< Dagiti Proverbio 4 >

1 Annakko, denggenyo ti annuroten ti maysa nga ama, ken ipangagyo tapno maammoanyo ti kayat a sawen ti pannakaawat.
Ananu, mverani malangizo a abambo anu; tcherani khutu kuti mupeze nzeru zodziwira zinthu.
2 Ik-ikkankayo iti nasasayaat a sursuro; saanyo a laksiden ti pannursurok.
Zimene ndikukuphunzitsani ndi zabwino. Choncho musasiye malangizo anga.
3 Idi maysaak nga ubing ti amak, ti nalupoy ken kakaisuna nga anak ti inak,
Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga; mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
4 sinurwannak ket kinunana kaniak, “Ipapusom koma dagiti sasaok: tungpalem dagiti bilinko ket agbiagka.
Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti, “Ugwiritse mawu anga pa mtima pako, usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.
5 Gun-odem ti kinasirib ken pannakaawat; saanmo a lipaten ken saanmo a laksiden dagiti sasaok;
Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu; usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.
6 saanmo a panpanawan ti kinasirib ket bantayannakanto; ayatem isuna ket saluadannakanto.
Usasiye nzeru ndipo idzakusunga. Uziyikonda ndipo idzakuteteza.
7 Ti kinasirib ti kapapatgan a banag, isu a gun-odem ti kinasirib ket busbusem dagiti amin a kukuam tapno maalam ti pannakaawat.
Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru. Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.
8 Ipategmo ti kinasirib ket itag-aynaka; padayawannaka inton arakupem isuna.
Uyilemekeze nzeruyo ndipo idzakukweza; ikumbatire nzeruyo ndipo idzakupatsa ulemu.
9 Mangikabil isuna iti balangat ti pammadayaw dita ulom; ikkannaka iti napintas a korona.”
Idzayika sangamutu yokongola yamaluwa pamutu pako; idzakupatsa chipewa chaufumu chaulemu.”
10 Dumngegka anakko, ken ipangagmo dagiti sasaok, ket maaddaankanto iti adu a tawen iti panagbiagmo.
Mwana wanga, umvere ndi kuvomereza zimene ndikunena, ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka.
11 Iturturongka iti dalan ti kinasirib; idaldalanka kadagiti nalinteg a pagnaan.
Ndakuphunzitsa njira yake ya nzeru. Ndakutsogolera mʼnjira zolungama.
12 Inton magnaka, awanto ti agserra iti dalanmo ket no agtarayka, saankanto a maitublak.
Pamene ukuyenda, mapazi ako sadzawombana; ukamadzathamanga, sudzapunthwa.
13 Petpetam ti disiplina, saanmo nga ib-ibbatan; bantayam, ta isu ti biagmo.
Ugwiritse zimene ndikukuphunzitsazi osazitaya ayi. Uwasamale bwino pakuti moyo wako wagona pamenepa.
14 Saanmo a suroten ti wagas dagiti nadangkes ken saanmo nga ar-aramiden ti wagas dagiti agar-aramid iti dakes.
Usayende mʼnjira za anthu oyipa kapena kuyenda mʼnjira ya anthu ochimwa.
15 Liklikam daytoy, saanka a mapmapan iti daytoy; liklikam daytoy ket magnaka iti sabali a dalan.
Pewa njira zawo, usayende mʼmenemo; uzilambalala nʼkumangopita.
16 Ta saanda a makaturog agingga a makaaramidda iti dakes ken saanda a makaturog agingga nga adda maipatublakda.
Pakuti iwo sagona mpaka atachita zoyipa; tulo salipeza mpaka atapunthwitsa munthu wina.
17 Ta kankanenda ti tinapay ti kinadangkes ken in-inumenda ti arak ti kinaranggas.
Paja chakudya chawo ndicho kuchita zoyipa basi ndipo chakumwa chawo ndi chiwawa.
18 Ngem ti dalan ti agar-aramid iti umno ket kas iti panagbannawag a lumawlawag; rumanraniag agingga nga umay ti naan-anay a kinaraniag ti aldaw.
Koma njira ya anthu olungama ili ngati kuwala kwa mʼbandakucha kumene kumanka kuwalirawalira mpaka dzuwa litafika pa mutu.
19 Ti dalan dagiti nadangkes ket kasla sipnget - saanda nga ammo no ania iti pakaitibtibkulanda.
Koma njira ya anthu oyipa ili ngati mdima wandiweyani; iwo sadziwa chomwe chimawapunthwitsa.
20 Anakko, ipangagmo dagiti sasaok; denggem dagiti ibagbagak.
Mwana wanga, mvetsetsa zimene ndikunena; tchera khutu ku mawu anga.
21 Saanmo nga ik-ikkaten kadagitoy ti panagkitam; salimetmetam dagitoy dita pusom.
Usayiwale malangizo angawa, koma uwasunge mu mtima mwako.
22 Ta dagiti sasaok ket biag kadagiti mangsapul kadagitoy ken salun-at iti entero a bagida.
Pakuti amapatsa moyo kwa aliyense amene awapeza ndipo amachiritsa thupi lake lonse.
23 Pagtalinaedem a natalged ti pusom ken ikagumaam daytoy a bantayan, ta manipud iti daytoy ket agayus ti ubbog ti biag.
Ndipotu mtima wako uziwuyangʼanira bwino ndithu pakuti ndiwo magwero a moyo.
24 Ikkatem ti panagul-ulbodmo ken ibellengmo dagiti dakes a panagsarsaritam.
Usiyiretu kuyankhula zokhotakhota; ndipo ulekeretu kuyankhula zinthu zonyansa.
25 Arigna nga ikitam a deretso dagiti matam ken iti sangoanam laeng ti kitkitam.
Maso ako ayangʼane patsogolo; uziyangʼana kutsogolo molunjika.
26 Agaramidka iti nasimpa a pagnaan dagiti sakam; ket natalgedto dagiti amin a dalanmo.
Uzilingalira bwino kumene kupita mapazi ako ndipo njira zako zonse zidzakhala zosakayikitsa.
27 Saanka a sumiasi a mapan iti kannawan wenno kannigid; iyadayom ti sakam iti dakes.
Usapatukire kumanja kapena kumanzere; usapite kumene kuli zoyipa.

< Dagiti Proverbio 4 >