< Mateo 5 >

1 Idi nakita ni Jesus dagiti adu a tattao, simmang-at isuna iti bantay. Idi nagtugaw isuna, immay dagiti adalanna kenkuana.
Iye ataona anthu ambiri, anakwera pa phiri nakhala pansi. Ndipo ophunzira ake anabwera kwa Iye,
2 Nagsao ket sinuroanna ida, a kunana,
ndipo anayamba kuwaphunzitsa kuti,
3 “Nabendisionan dagiti napanglaw iti espiritu, ta kukuada ti pagarian ti langit.
“Odala ndi amene ali osauka mu mzimu, chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo.
4 Nabendisionan dagiti agladladingit, ta maliwliwadanto.
Odala ndi amene ali achisoni, chifukwa adzatonthozedwa.
5 Nabendisionan dagiti naemma, ta tawidendanto ti daga.
Odala ndi amene ali ofatsa, chifukwa adzalandira dziko lapansi.
6 Nabendisionan dagiti mabisin ken mawaw iti kinalinteg, ta mapunnodanto.
Odala ndi amene akumva njala ndi ludzu la chilungamo, chifukwa adzakhutitsidwa.
7 Nabendisionan dagiti manangngaasi, ta magun-oddanto ti asi.
Odala ndi amene ali ndi chifundo, chifukwa adzawachitira chifundo.
8 Nabendisionan dagiti nasin-aw ti pusona, ta makitadanto ti Dios.
Odala ndi amene ali oyera mtima, chifukwa adzaona Mulungu.
9 Nabendisionan dagiti mamagkappia, ta maawagandanto nga annak ti Dios.
Ndi odala amene amabweretsa mtendere, chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu.
10 Nabendisionan dagiti maparparigat gapu iti kinalinteg, ta kukuadanto ti pagarian ti langit.
Odala ndi amene akuzunzidwa chifukwa cha chilungamo, pakuti ufumu wakumwamba ndi wawo.”
11 Nabendisionankayo no laisendakayo ken parigatendakayo dagiti tattao, wenno isawangda amin a kita ti dakes a banbanag maibusor kadakayo gapu kaniak.
“Inu ndinu odala anthu akamakunyozani, kukuzunzani, kukunenerani zoyipa zilizonse ndi kukunamizirani chifukwa cha Ine.
12 Agrag-o ken agragsakkayo la unay, ta naindaklan ti gunggonayo sadi langit. Ta iti kastoy a wagas a pinarigat dagiti tattao dagiti profeta a nagbiag sakbay kadakayo.
Sangalalani, kondwerani chifukwa mphotho yanu ndi yayikulu kumwamba, chifukwa moterenso ndi mmene anazunzira aneneri inu musanabadwe.
13 Dakayo ti asin ti daga. Ngem no napukawen ti raman ti asin, kasano a pagbalinen manen a naapgad? Saanen a pulos a nasayaat para iti aniaman a banag, malaksid nga ibelleng iti ruar ket mapayatpayatan dagiti tattao.
“Inu ndinu mchere wa dziko lapansi. Koma ngati mcherewo usukuluka, adzawukometsanso ndi chiyani? Ulibenso ntchito koma kungowutaya kunja, anthu nawuponda.
14 Dakayo ti silaw ti lubong. Ti siudad a nabangon iti rabaw ti turod ket saan a mailemmeng.
“Inu ndinu kuwunika kwa dziko lapansi. Mzinda wa pa phiri sungathe kubisika.
15 Kasta met nga awan ti tao a mangsindi iti pagsilawan sana ikabil iti sirok ti maysa a basket, ngem ikabilna ketdi iti nairanta a pagsilawan, ket aglawag para iti tumunggal maysa nga adda iti balay.
Anthu sayatsa nyale ndikuyivundikira ndi mbiya, mʼmalo mwake amayika poonekera ndipo imawunikira onse mʼnyumbamo.
16 Pagraniagenyo dagiti silawyo iti imatang dagiti tattao iti wagas a makitada dagiti nasayaat nga aramidyo ket dayawenda ti Dios Ama nga adda sadi langit.
Momwemonso kuwunika kwanu kuwale pamaso pa anthu kuti aone ntchito zanu zabwino ndi kulemekeza Atate anu akumwamba.
17 Saanyo a panunoten nga immayak a mangdadael iti linteg wenno dagiti profeta. Saanak nga immay tapno dadaelen ida, ngem tapno tungpalen dagitoy.
“Musaganize kuti ndinadza kudzathetsa malamulo kapena zonena za aneneri; sindinabwere kudzathetsa koma kukwaniritsa.
18 Ta pudno, ibagak kadakayo nga agingga a mapukaw ti langit ken daga, awan ti uray maysa a kur-it wenno tolnek a mapukaw manipud iti linteg, agingga a matungpal amin a banbanag.
Ine ndikukuwuzani zoonadi kuti, kufikira kutha kwa thambo ndi dziko lapansi, chilichonse chimene chinalembedwa mʼmalamulo, ngakhale kalemba kakangʼonongʼono, chidzakwaniritsidwa.
19 Ngarud, siasinoman a mangsalungasing iti kababaan kadagitoy a bilbilin ken mangisuro kadagitoy iti dadduma tapno aramidenda met ket maawaganto a kababaan idiay pagarian ti langit. Ngem siasinoman a mangtungpal kadagitoy ken mangisuro kadagitoy ket maawaganto a natan-ok idiay pagarian ti langit.
Chifukwa chake aliyense amene aphwanya limodzi la malamulowa ngakhale lalingʼonongʼono ndi kuphunzitsa ena kuti achite chimodzimodzi, adzakhala wotsirizira mu ufumu wakumwamba, koma aliyense amene achita ndi kuphunzitsa malamulo awa adzakhala wamkulu mu ufumu wakumwamba.
20 Ta ibagak kadakayo a makastrekkayo iti pagarian ti langit no maartapan ti kinalintegyo ti kinalinteg dagiti eskriba ken dagiti Pariseo.
Chifukwa chake ndikuwuzani kuti ngati chilungamo chanu sichiposa cha Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo, zoonadi, simudzalowa mu ufumu wakumwamba.
21 Nangngeganyo a naibaga kadakuada idi un-unana a tiempo, 'Saanka a pumatay,' ken, 'Siasinoman a pumatay ket agpeggadto iti pannakaukom.'
“Munamva kuti kunanenedwa kwa anthu kale kuti, ‘Usaphe ndipo kuti aliyense amene apha munthu adzaweruzidwa.’
22 Ngem ibagak kadakayo a tunggal maysa a makaunget iti kabsatna ket agpeggadto iti pannakaukom. Ken siasinoman a mangibaga iti kabsatna, 'Awan serserbim a tao!' ket agpeggadto iti konseho. Ket siasinoman a mangibaga iti, 'Sika a maag!' ket agpeggadto iti apuy ti impierno. (Geenna g1067)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
23 Ngarud no mangidatagka iti sagutmo idiay altar ket idiay nalagipmo a ti kabsatmo ket addaan iti sakit ti nakem kenka,
“Nʼchifukwa chake, pamene ukupereka chopereka chako pa guwa lansembe ndipo nthawi yomweyo ukumbukira kuti mʼbale wako ali nawe chifukwa,
24 ibatim ti sagutmo iti sango ti altar, ket mapanka iti dalanmo. Makikappiaka pay nga umuna iti kabsatmo, ket kalpasanna mapanka ket idatagnmo ti sagutmo.
usiye choperekacho pa guwa lansembepo, choyamba pita kayanjane ndi mʼbale wako; ukatero bwera kudzapereka chopereka chakocho.
25 Makikinnaawatanka a dagus iti nangidarum kenka kabayatan a kaduam isuna iti dalan a mapan iti pangukoman, wenno saan ti nangidarum kenka ket ipaimanaka iti ukom, ket ti ukom ipaimanaka iti opisial, ket mabalin a maibaludka iti pagbaludan.
“Fulumira kuyanjana ndi mnzako amene unamulakwira nthawi ya milandu isanafike chifukwa angakupereke kwa oweruza amene angakupereke kwa mlonda ndipo mlondayo angakutsekere mʼndende.
26 Pudno, ibagak kadakayo, saankanto a makarruar manipud sadiay agingga a mabayadam amin a binulodmo.
Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti sudzatuluka mʼndende mpaka utalipira zonse.
27 Nangngegyo a naibaga, 'Saanka a makikamalala.'
“Munamva kuti kunanenedwa kuti, ‘Usachite chigololo.’
28 Ngem ibagak kadakayo a siasinoman a kumita iti babai nga addaan panaggartem kenkuana ket nakikamalalan kenkuana iti pusona.
Koma Ine ndikuwuzani kuti aliyense woyangʼana mkazi momusirira wachita naye kale chigololo mu mtima mwake.
29 No ti makannawan a matam ti makagapu a maitublakka, suatem ken ibellengmo iti adayo manipud kenka. Ta nasaysayaat para kenka a mapukaw ti maysa a paset ti bagim ngem maitapuak ta sibubukel a bagim iti impierno. (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
30 Ket no ti makannawan nga imam ti makagapu a maitublakka, putdem ken ibellengmo iti adayo manipud kenka. Ta nasaysayaat para kenka a mapukaw ti maysa a paset ti bagim ngem ti itapuaknaka ti Dios ti entero a bagim iti impierno. (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
31 Naibaga pay, 'Siasinoman a mangpapanaw iti asawana a babai, ikkanna koma iti kasuratan ti panagsina.'
“Ananena kuti, ‘Aliyense wosudzula mkazi wake ayenera amupatse kalata ya chisudzulo.’
32 Ngem ibagak kadakayo a siasinoman a mangisina iti asawana a babai, malaksid no gapu iti kinaderrep, pagbalinenna isuna a mannakikamalala. Ken ti siasinoman a mangasawa kenkuana kalpasan a naisina ket makikamkamalala.
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene asudzula mkazi wake pa chifukwa china chilichonse osati chifukwa cha chiwerewere, akumuchititsa mkaziyo chigololo ndipo aliyense wokwatira mkaziyo, akuchitanso chigololo.
33 Nangngeganyo manen a naibaga kadagiti adda idi un-unana a tiempo, 'Diyo sapataan iti inuulbod ti kariyo, ngem tungpalenyo ti inkariyo iti Apo.'
“Munamvanso kuti kunanenedwa kwa anthu akale kuti, ‘Musaphwanye lonjezo; koma sungani malonjezo anu amene mwachita kwa Yehova.’
34 Ngem ibagak kadakayo, saankayo nga agsapata uray pay babaen iti langit, ta isu ti trono ti Dios;
Koma ndikuwuzani kuti musalumbire ndi pangʼono pomwe kutchula kumwamba chifukwa kuli mpando waufumu wa Mulungu.
35 wenno babaen iti daga, ta isu ti pagbatayan dagiti sakana; wenno babaen iti Jerusalem, ta isu ti siudad ti naindaklan nga Ari.
Kapena kutchula dziko lapansi, chifukwa ndi chopondapo mapazi ake; kapena kutchula Yerusalemu, chifukwa ndi mzinda wa mfumu yayikulu.
36 Saanyo nga iraman ti uloyo iti panagkariyo, ta saankayo a makaaramid iti maysa a buok a puraw wenno nangisit.
Ndipo musalumbire ndi mutu wanu chifukwa simungathe kuyeretsa ngakhale kudetsa tsitsi limodzi.
37 Ngem kastoy koma ti kunayo, 'Wen, no wen,' wenno 'Saan, no saan.' Ta aniaman a banag a nalablabes ngem iti daytoy ket nagtaud iti daydiay a managdakdakes.
Koma ‘Inde’ wanu akhaledi ‘Inde’ kapena ‘Ayi’ wanu akhaledi ‘Ayi,’ chilichonse choposera apa, chichokera kwa woyipayo.
38 Nangngegyo a naibaga, 'Mata para iti mata, ken ngipen para iti ngipen.'
“Munamva kuti, ‘Diso kulipira diso ndi dzino kulipira dzino.’
39 Ngem ibagak kadakayo, saanyo a kalabanen ti managdakdakes. Ngem ketdi, siasinoman a mangtungpa iti makannawan a pingpingmo, itayam pay ti bangir a pingpingmo.
Koma ndikuwuzani kuti musamukanize munthu woyipa, akakumenya patsaya mupatseni tsaya linalo.
40 Ket no adda agtarigagay a mangidarum kenka idiay pangukoman ken alaenna ti kawesmo, palubosam dayta a tao nga alaenna pay ti kagaymo.
Ndipo ngati wina afuna kukuzenga mlandu kuti akulande malaya ako, umupatsenso mkanjo wako.
41 Ket siasinoman a mangpilit kenka a mangdaliasat iti maysa a milia, kumuyogka kenkuana iti dua.
Ngati wina akukakamiza kuti uyende naye mtunda umodzi, iwe uyende naye mitunda iwiri.
42 Mangtedka iti siasinoman nga agdawat kenka, ken saanmo a tallikudan ti siasinoman nga agtarigagay nga agbulod kenka.
Wina akakupempha kanthu umupatse, ndipo wofuna kubwereka usamukanize.
43 Nangngegyo a naibaga, 'Ayatem ti kaarrubam ken guraem ti kabusormo.'
“Munamva kuti, ‘Konda mnansi wako ndi kudana ndi mdani wako.’
44 Ngem ibagak kadakayo, ayatenyo dagiti kabusoryo ken ikararaganyo dagiti mangparparigat kadakayo,
Koma Ine ndikuwuzani kuti, ‘Kondani adani anu ndi kuwapempherera okuzunzani
45 tapno agbalinkayo nga annak ti Amayo nga adda sadi langit. Ta inaramidna ti initna nga agraniag kadagiti dakes ken naimbag, ken mangmangted iti tudo kadagiti nalinteg ken saan a nalinteg.
kuti mukhale ana a Atate anu akumwamba, amene awalitsa dzuwa lake pa oyipa ndi pa abwino, nagwetsa mvula pa olungama ndi pa osalungama.’
46 Ta no ay-ayatenyo dagiti mangay-ayat kadakayo, ania ti magunggonayo? Saan kadi nga uray dagiti agsingsingir iti buis ket aramidenda ti kasta met laeng a banag?
Ngati mukonda amene akukondani inu, mudzapeza mphotho yanji? Kodi ngakhale amisonkho sachita chimodzimodzi?
47 Ket no dagiti laeng kakabsatyo ti kablaawanyo, ania ti ar-aramidenyo a nasaysayaat ngem kadagiti dadduma? Saan kadi nga uray dagiti Hentil ket aramidenda ti kasta met laeng a banag?
Ndipo ngati inu mupatsa moni abale anu okhaokha mukuchita chiyani choposa ena? Kodi ngakhale akunja sachita chimodzimodzi?
48 Ngarud, masapul nga awan ti pagkuranganyo, kas iti Amayo nga adda sadi langit nga awan pagkuranganna.
Nʼchifukwa chake, inu khalani angwiro monga Atate anu akumwamba ali wangwiro.”

< Mateo 5 >