< Marcos 1 >

1 Daytoy ti nangrugian iti ebanghelio maipanggep kenni Jesu-Cristo, nga Anak ti Dios.
Chiyambi cha Uthenga Wabwino wa Yesu Khristu, Mwana wa Mulungu,
2 Kas naisurat idiay libro ni propeta Isaias a kunana, “Kitaem, ibaonko ti mensaherok nga umun-una ngem sika, a mangisagana iti dalanmo.
monga zalembedwera mʼbuku la mneneri Yesaya: “Ine ndidzatuma mthenga wanga patsogolo panu, amene adzakonza njira yanu,”
3 Ti makintimek iti daydiay umaw-awag nga adda idiay let-ang, 'Isaganayo ti dalan ti Apo, pagbalinenyo a nalinteg dagiti pagnaanna.'”
“Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’”
4 Immay ni Juan a nangbautisar idiay let-ang ken nangikasaba iti pannakabautisar iti panagbabawi para iti pannakapakawan dagiti basbasol.
Ndipo Yohane anabwera mʼmadera a mʼchipululu nabatiza, ndi kulalikira za ubatizo wa kutembenuka mtima ndi wa chikhululukiro cha machimo.
5 Ti entero a pagilian iti Judea ken amin a tattao idiay Jerusalem ket rimmuarda a napan kenkuana. Binautisaranna amin ida idiay Karayan Jordan, ket impudnoda dagiti basbasolda.
Madera onse a ku Yudeya ndi anthu onse a ku Yerusalemu anatuluka napita kwa iye. Akavomereza machimo awo, amawabatiza mu mtsinje wa Yorodani.
6 Nakakawes ni Juan iti kagay a naaramid manipud iti buok ti kamelyo, nakabarikes iti lalat, ken nangnangan isuna iti dudun ken diro.
Yohane amavala zovala zopangidwa ndi ubweya wangamira, ndi lamba wachikopa mʼchiwuno mwake, ndipo amadya dzombe ndi uchi wamthengo.
7 isuna ket kinunana, “Adda iti sumaruno kaniak a nabilbileg ngem siak, ket saanak a maikari nga agrukob a mangwarwar iti tali dagiti sandaliasna.
Ndipo uthenga wake unali uwu: “Pambuyo panga pakubwera wina wondiposa ine mphamvu. Ine si woyenera kuwerama ndi kumasula zingwe za nsapato zake.
8 Bautisarankayo babaen iti danum, ngem bautisarannakayo babaen ti Espiritu Santo.”
Ine ndikubatizani ndi madzi, koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.”
9 Napasamak kadagidiay nga al-aldaw a simmangpet ni Jesus manipud Nazaret iti Galilea, ket binautisaran isuna ni Juan idiay Karayan Jordan.
Pa nthawi imeneyo Yesu anabwera kuchokera ku Nazareti wa ku Galileya ndipo anabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani.
10 Apaman a rimmuar ni Jesus manipud iti danum, nakitana a nalukatan ti langit ken ti Espiritu ket bumabbaba kenkuana a kasla kalapati.
Pamene Yesu ankatuluka mʼmadzi, anaona kumwamba kukutsekuka ndipo Mzimu Woyera akutsikira pa Iye ngati nkhunda.
11 Ket adda timek a nagsao sadi langit, “Sika ti Anakko a dungdungwek. Maay-ayoak unay kenka.”
Ndipo Mawu anamveka kuchokera kumwamba: “Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa; ndipo ndikondwera nawe.”
12 Ket dagus nga inturong isuna ti Espiritu a rumuar a mapan idiay let-ang.
Nthawi yomweyo Mzimu Woyera anamutumiza Iye ku chipululu,
13 Adda isuna idiay let-ang iti uppat a pulo nga aldaw, ket sinulsulisog isuna ni Satanas. Adda isuna iti ayan dagiti atap nga ayup, ket pinagserbian isuna dagiti anghel.
ndipo anali mʼchipululumo masiku makumi anayi, akuyesedwa ndi Satana. Anali pakati pa nyama zakuthengo; ndipo angelo anamutumikira.
14 Ita, kalpasan a natiliw ni Juan, dimteng ni Jesus idiay Galilea ket inwarwaragawagna ti ebanghelio ti Dios,
Yohane atamutsekera mʼndende, Yesu anapita ku Galileya nalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu nati,
15 a kinunkunana, “Ti tiempo ket natungpalen, ken ti pagarian ti Dios ket asidegen. Agbabawikayo ken mamatikayo iti ebanghelio.”
“Nthawi yafika, ufumu wa Mulungu wayandikira. Tembenukani mtima ndi kukhulupirira Uthenga Wabwino!”
16 Iti ilalabasna iti igid ti baybay ti Galilea, nakitana da Simon ken ni Andres a kabsat a lalaki ni Simon a mangiwaywayat iti iket idiay baybay, ta mangngalapda.
Pamene Yesu ankayenda mʼmbali mwa nyanja ya Galileya, anaona Simoni ndi mʼbale wake Andreya akuponya khoka mʼnyanja, popeza anali asodzi.
17 Kinuna ni Jesus kadakuada, “Surotendak, ket pagbalinenkayo a mangngalap iti tattao.”
Yesu anati, “Bwerani, tsateni Ine, ndipo ndidzakusandutsani asodzi a anthu.”
18 Ket dagus nga imbatida dagiti iketda ket simmurotda kenkuana.
Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.
19 Apaman a nakaadayo bassit ni Jesus, nakitana ni Santiago nga anak ni Zebedeo ken ni Juan a kabsatna a lalaki; addada iti bangka nga agtartarimaan kadagiti iket.
Atapita patsogolo pangʼono, anaona Yakobo ndi mʼbale wake Yohane ana a Zebedayo, ali mʼbwato akukonza makoka awo.
20 Dagus nga inayabanna isuda ket pinanawanda ti amada a ni Zebedeo nga adda iti bangka a kaduana dagiti babayadan nga adipen, ket sinurotda isuna.
Mosataya nthawi anawayitana, ndipo anasiya abambo awo Zebedayo ndi anyamata aganyu ali mʼbwatomo, namutsata Iye.
21 Ket dimtengda idiay Capernaum, ket iti Aldaw a Panaginana, napan a dagus ni Jesus iti sinagoga ket nagisuro.
Iwo anapita ku Kaperenawo, ndipo tsiku la Sabata litafika, Yesu analowa mʼsunagoge nayamba kuphunzitsa.
22 Nasdaawda iti panagisurona, ta nagisuro isuna kadakuada a kas maysa nga addaan iti turay a saan ket a kas kadagiti eskriba.
Anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake, chifukwa anawaphunzitsa ngati munthu amene anali ndi ulamuliro, osati ngati aphunzitsi amalamulo.
23 Nairana nga adda idiay sinagogada ti maysa a lalaki nga addaan iti narugit nga espiritu ket impukkawna,
Pomwepo munthu wina mʼsunagogemo amene anali wogwidwa ndi mzimu woyipa anafuwula kuti,
24 “Ania iti pakibianganmi kenka, Jesus ti Nazaret? Immayka kadi a mangdadael kadakami? Ammok no siasinoka. Sika ti Nasantoan ti Dios!”
“Mukufuna chiyani kwa ife, Yesu wa ku Nazareti? Kodi mwabwera kudzatiwononga? Ndikudziwa kuti ndinu ndani, ndinu Woyerayo wa Mulungu!”
25 Tinubngar ni Jesus ti demonio a kinunana, “Agulimekka ket rummuarka kenkuana!”
Yesu anadzudzula chiwandacho mwamphamvu nati, “Khala chete! Tuluka mwa iye!”
26 Ket intumba ti dakes nga espiritu ti lalaki ken agik-ikkis a rimmuar manipud kenkuana.
Mzimu woyipawo unamugwedeza mwamphamvu ndipo unatuluka mwa iye ukufuwula.
27 Ket nasdaaw amin dagiti tattao, isu a sinaludsodda iti tumunggal maysa, “Ania daytoy? Maysa a baro a sursuro nga addaan turay! Bilinenna pay uray dagiti narugit nga espiritu, ket agtulnogda kenkuana.”
Anthu anadabwa kwambiri kotero kuti anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Ichi nʼchiyani? Chiphunzitso chatsopano ndi ulamuliro! Iye akulamula, ngakhale mizimu yoyipa ikumumvera.”
28 Ket dagus a rimuar ti damag maipanggep kenkuana iti sadinoman, iti entero a rehion ti Galilea.
Mbiri yake inafalikira kudera lonse la Galileya mofulumira.
29 Kalpasan a pimmanawda iti sinagoga, napanda a dagus iti balay da Simon ken Andres, kaduada da Santiago ken Juan.
Atangochoka mu sunagoge, Yesu pamodzi ndi Yakobo ndi Yohane anakalowa mʼnyumba ya Simoni ndi Andreya.
30 Ita ti katugangan a babai ni Simon ket agsaksakit ket nakaidda gapu iti gurigor. Dagus nga imbagada ken ni Jesus ti maipanggep kenkuana.
Mpongozi wa Simoni anali chigonere akudwala malungo, ndipo anamuwuza Yesu za iye.
31 Immay ngarud isuna, iniggamanna dagiti imana, ket binangonna isuna; pinanawan isuna iti gurigor, ket nangrugi isuna a nagserbi kadakuada.
Ndipo Yesu anapita kwa iye, namugwira dzanja namuthandiza kudzuka. Malungo anachoka ndipo anayamba kuwatumikira.
32 Iti dayta a rabii, kalpasan a limnek ti init, impanda kenkuana dagiti amin a masaksakit wenno linuganan dagiti demonio.
Madzulo omwewo dzuwa litalowa anthu anabweretsa kwa Yesu anthu onse odwala ndi ogwidwa ndi ziwanda.
33 Nagguummong ti entero a siudad iti ruangan.
Anthu onse a mʼmudzimo anasonkhana pa khomo,
34 Pinaimbagna ti adu nga agsagsagaba iti nadumaduma a kita ti sakit, ken pinaksiatna ti adu a demonio, ngem saanna nga impalubos nga agsao dagiti demonio gapu ta am-ammoda isuna.
Yesu anachiritsa ambiri amene anali ndi matenda osiyanasiyana, komanso anatulutsa ziwanda zambiri, ndipo sanalole kuti ziwandazo ziyankhule chifukwa zinkamudziwa Iye.
35 Bimmangon isuna iti nakasapsapa unay kabayatan a nasipnget pay laeng; pimmanaw ket rimuar a napan iti saan a matagtagitao a lugar, ket idiay a nagkararag.
Mmamawa, kukanali kamdima, Yesu anadzuka, nachoka pa nyumbapo kupita kumalo kwa yekha, kumene anakapemphera.
36 Biniruk isuna da Simon ken dagiti kakadduana.
Simoni ndi anzake anapita kokamufunafuna Iye,
37 Nasarakanda isuna, ket kinunada kenkuana, “Tunggal maysa ket sapsapulendaka.”
ndipo atamupeza, anamuwuza kuti, “Aliyense akukufunani!”
38 Kinunana, “Mapantayo iti sabali a lugar, kadagiti ili iti aglaw-law, tapno mangasabaak met sadiay. Dayta ti makagapu nga immayak ditoy.
Yesu anayakha kuti, “Tiyeni tipite kwina ku midzi ya pafupi kuti ndikalalikirenso kumeneko. Ichi ndi chifukwa chimene ndinabwerera.”
39 Napan isuna iti amin a paset ti Galilea, nangasaba isuna kadagiti sinagogada ken pinaksiatna dagiti demonio.
Potero anayendayenda mu Galileya, kulalikira mʼmasunagoge awo ndi kutulutsa ziwanda.
40 Maysa nga agketong ti napan kenkuana; agpakpakaasi kenkuana; nagparintumeng ket kinunana kenkuana, “No pagayatam, mabalinnak a pagbalinen a nadalus.”
Munthu wakhate anabwera kwa Iye, nagwada, namupempha kuti, “Ngati mukufuna, mukhoza kundiyeretsa.”
41 Natignay ni Jesus ket naasi, inggaw-atna ti imana ken sinagidna isuna, kinunana kenkuana, “Sipapalubosak. Agbalinka a nadalus.”
Yesu pomva naye chifundo, anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo nati, “Ndikufuna, yeretsedwa!”
42 Dagus a pimmanaw ti ketong kenkuana, ket nadalusan isuna.
Nthawi yomweyo khate linachoka ndipo anachiritsidwa.
43 Siiinget a binallaagan isuna ni Jesus ken pinapanawna a dagus,
Nthawi yomweyo Yesu anamuwuza kuti apite koma anamuchenjeza kuti,
44 kinuna ni Jesus kenkuana, “Siguraduem nga awan ti ibagam iti siasinoman, ngem mapanka, iparangmo ti bagim iti padi, ken idatonmo dagiti banbanag a maipaay iti pannakadalusmo kas iti imbilin ni Moises, kas pammaneknek kadakuada.”
“Wonetsetsa kuti usawuze aliyense za zimenezi. Koma pita, kadzionetse wekha kwa wansembe ndi kukapereka nsembe zimene Mose analamulira zotsimikizira kuyeretsedwa kwanu, ngati umboni kwa iwo.”
45 Ngem rimmuar isuna ken inrugina nga imbaga iti amin, ket nagwaras ti damag, isu a saanen a makaapan ni Jesus a siwayawaya iti uray ania nga ili. Nagigian ngarud isuna kadagiti di matagtagitao a disso ket immay kenkuana dagiti tattao manipud iti sadinoman.
Mʼmalo mwake anapita nayamba kuyankhula momasuka, nafalitsa mbiriyo. Zotsatira zake, Yesu sanathe kulowa mʼmudzi moonekera, koma anakhala kunja kumalo kopanda anthu. Komabe anthu amabwera kwa Iye kuchokera kulikonse.

< Marcos 1 >