< 1 Pedro 5 >

1 Bagbagaak dagiti panglakayenyo, Siak, maysa a panglakayen a padayo ken maysa a saksi iti panagsagsagaba ni Cristo, ken maysa met a makipagpaset iti dayag a maiparangarangto.
Ine ndikupempha akulu a mpingo amene ali pakati panu, monga inenso mkulu mnzawo, mboni ya zowawa za Khristu ndiponso amene ndidzalandira nawo ulemerero umene uti udzaonetsedwe.
2 Bagbagaankayo ngarud a panglakayen, aywananyo dagiti arban ti Dios nga adda kadakayo. Kitaenyo ida, saan a gapu ta kasapulan nga aramidenyo, ngem gapu ta isu ti tarigagayyo mayannurot iti pagayatan ti Dios. Kitaenyo ida, saan a para iti kinaagum iti kuarta, ngem sipapalubos.
Wetani gulu la Mulungu limene lili mʼmanja mwanu, muziliyangʼanira. Muzichita osati mowumirizidwa, koma mwakufuna kwanu, monga momwe Mulungu akufunira kuti mutero. Musachite chifukwa chadyera la ndalama, koma ndi mtima ofuna kutumikira.
3 Saankayo nga agtignay a kas apo kadagiti tattao nga adda iti panangaywanyo, ngem agbalinkayo koma a pagulidanan kadagiti arban.
Musakhale ngati mafumu pa amene mukuwayangʼanira, koma mukhale chitsanzo kwa gululo.
4 Inton maiparangarang ti Katan-okan a Pastor, awatenyonto iti saan nga agkupkupas a nadayag a korona.
Ndipo Mʼbusa wamkulu akadzaonekera, mudzalandira chipewa cha ulemerero chosafota.
5 Kasta met, dakayo nga agtutubo a lallaki, agpaituraykayo kadagiti natataengan ngem kadakayo. Aminkayo, kawesanyo dagiti bagbagiyo iti kinapakumbaba ken agserbikayo iti tunggal maysa, ta busoren ti Dios ti natangsit, ngem paraburanna dagiti napakumbaba.
Momwemonso, inu anyamata gonjerani amene ndi akulu. Inu nonse mukhale odzichepetsa kuti mutumikirane, chifukwa, “Mulungu amatsutsana nawo odzikuza, koma amapereka chisomo kwa odzichepetsa.”
6 Ipakumbabayo ngarud dagiti bagbagiyo iti mannakabalin nga ima ti Dios tapno itag-aynakayonto inton dumteng iti maitutop a tiempo.
Choncho, mudzichepetse pamaso pa Mulungu wamphamvu, kuti pa nthawi yake adzakukwezeni.
7 Ikamangyo amin a pakariribukanyo kenkuana, gapu ta maseknan isuna kadakayo.
Tayani pa Iye nkhawa zanu zonse chifukwa ndiye amakusamalani.
8 Agparbengkayo, agsiputkayo. Ti kalabanyo, ti diablo, ket kasla agngerngernger a leon a magmagna iti aglawlaw, nga agsapsapul iti alun-onenna.
Khalani odziretsa ndi atcheru. Mdani wanu mdierekezi amayendayenda monga mkango wobangula kufunafuna wina kuti amumeze.
9 Agtakderkayo a maibusor kenkuana. Papigsaenyo ti pammatiyo. Ammoyo nga uray dagiti kakabsatyo nga adda ditoy lubong ket agib-ibtur iti isu met laeng a panagsagsagaba.
Mukaneni iye, ndipo mukhazikike mʼchikhulupiriro, chifukwa mukudziwa kuti abale anzanu pa dziko lonse lapansi nawonso akumva zowawa zomwezi.
10 Kalpasan nga agsagabakayo iti apagbiit, ti Dios iti amin a parabur, a nangayab kadakayo iti agnanayon a gloriana kenni Cristo, ket palaingennakayonto, patibkerennakayonto, ken papigsaennakayonto. (aiōnios g166)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
11 Maited koma kenkuana ti panagturay iti agnanayon ken awan patinggana. Amen. (aiōn g165)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
12 Ibilangko ni Silvano a kas napudno a kabsat, ken nagsuratak kadakayo iti ababa babaen kenkuana. Bagbagaankayo ken paneknekak kadakayo a ti insuratko ket isu ti pudno a parabur ti Dios. Agtakderkayo iti daytoy.
Mothandizidwa ndi Sila, amene ndi mʼbale wokhulupirika, ndakulemberani mwachidule kukulimbikitsani ndi kuchita umboni kuti ichi ndi chisomo choona cha Mulungu.
13 Isuna nga adda idiay Babilonia, a napili a kas kadakayo, kablaawandakayo, ken ni Marcos, nga anakko, kablaawannakayo.
Imani mwamphamvu mʼchisomochi. Mlongo wanu amene ali ku Babuloni, wosankhidwa pamodzi nanu akupereka moni, nayenso Marko, mwana wanga, akupereka moni.
14 Agkikinnablaawkayo a buyogen iti agek ni ayat. Kapia koma kadakayo amin nga adda ken Cristo.
Mupatsane moni ndi mpsopsono wachikondi. Mtendere ukhale ndi inu nonse amene muli mwa Khristu.

< 1 Pedro 5 >