< Zsoltárok 53 >

1 Az éneklőmesternek a mahalathra, Dávid tanítása. Ezt mondta a balgatag az ő szívében: Nincs Isten. Megromlottak és útálatos hamisságot cselekedtek, nincs a ki jót cselekedjék.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide. Chitsiru chimati mu mtima mwake, “Kulibe Mulungu.” Iwo ndi oyipa ndipo njira zawo ndi zonyansa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino.
2 Isten letekint a mennyből az emberek fiaira, hogy meglássa, ha van-é értelmes, Istent kereső?
Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano pa ana a anthu kuti aone ngati alipo wina wanzeru, wofunafuna Mulungu.
3 Mindnyájan elhajlottak, és valamennyien megromlottak, nincsen a ki jót cselekedjék, nincsen csak egy is.
Aliyense wabwerera, iwo onse pamodzi akhala oyipa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino, ngakhale mmodzi.
4 Avagy nincs értelem a hamisságnak cselekvőiben, a kik az én népemet megeszik, mintha kenyeret ennének, a kik az Istent segítségül nem hívják?
Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi; anthu amene amadya anthu anga monga mmene anthu amadyera buledi, ndipo sapemphera kwa Mulungu?
5 Ott félnek nagy félelemmel, a hol nincsen félelem; mert az Isten elszéleszti azoknak tetemeit, a kik tábort járnak ellened; megszégyeníted azokat, mert az Isten megveti őket.
Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu pamene panalibe kanthu kochititsa mantha. Mulungu anamwazamwaza mafupa a anthu amene anakuthirani nkhondo; inuyo munawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawanyoza.
6 Oh, vajha eljönne Sionból Izráelnek a szabadítás! Mikor az Úr visszahozza az ő népének foglyait, örül majd Jákób és vigad Izráel!
Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni! Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake, lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale!

< Zsoltárok 53 >