< Psalm 122 >

1 Wallfahrtslieder. Von David. Ich freute mich, als man zu mir sprach: “Laßt uns zum Tempel Jahwes gehn!”
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
2 Unsere Füße stehen in deinen Thoren, Jerusalem!
Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
3 Jerusalem, du wiedergebaute, wie eine Stadt, die allzumal zusammengefügt ist,
Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
4 wohin die Stämme hinaufziehen, die Stämme Jahs, nach dem Gesetz für Israel, um dem Namen Jahwes zu danken.
Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
5 Denn dort stehen Gerichtssessel, Sessel des Hauses Davids.
Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
6 Erbittet Frieden für Jerusalem: Mögen Ruhe haben, die dich lieben.
Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
7 Friede sei in deinen Bollwerken, Ruhe in deinen Palästen.
Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
8 Um meiner Brüder und Freunde willen laßt mich sprechen: Friede sei in dir!
Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
9 Um des Tempels Jahwes, unseres Gottes, willen will ich dein Bestes suchen.
Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.

< Psalm 122 >