< Psalm 128 >

1 Ein Stufenlied. - Heil jedem, der den Herren fürchtet und der auf seinen Pfaden wandelt!
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake.
2 Wenn du von deiner Hände Arbeit lebst, wohl dir! Es geht dir gut.
Udzadya chipatso cha ntchito yako; madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3 Gleich einem Weinstock, früchtereich, dein Weib im Innern deines Hauses und deine Söhne Ölbaumsprossen um deinen Tisch herum!
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka mʼkati mwa nyumba yako; ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi kuzungulira tebulo lako.
4 Seht! Also wird der Mann gesegnet, der fürchtet Gott, den Herrn.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
5 So segne dich der Herr von Sion aus! Erlabe dich am Glück Jerusalems dein Leben lang!
Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni masiku onse a moyo wako; uwone zokoma za Yerusalemu,
6 Und schau die Kinder deiner Kinder! Heil über Israel!
ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako. Mtendere ukhale ndi Israeli.

< Psalm 128 >