< Genèse 10 >

1 Or ce sont ici les générations des enfants de Noé, Sem, Cam et Japheth; auxquels naquirent des enfants après le déluge.
Nayi mbiri ya ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti. Ana atatuwa anabereka ana awo chitatha chigumula.
2 Les enfants de Japheth sont Gomer, Magog, Madaï, Javan, Tubal, Mésech, et Tiras.
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
3 Et les enfants de Gomer, Askénaz, Riphath, et Thogarma.
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.
4 Et les enfants de Javan, Elisa, Tarsis, Kittim, et Dodanim.
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
5 De ceux-là furent divisées les Iles des nations par leurs terres, chacun selon sa langue, selon leurs familles, entre leurs nations.
(Amenewa ndiwo makolo a anthu okhala mʼmphepete mwa nyanja. Awa ndi ana a Yafeti monga mwa mafuko a mu mitundu yawo, uliwonse ndi chiyankhulo chake).
6 Et les enfants de Cam sont Cus, Mitsraïm, Put, et Canaan.
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani.
7 Et les enfants de Cus: Séba, Havila, Sabtah, Rahma, et Sebtéca. Et les enfants de Rahma, Séba, et Dédan.
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka. Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
8 Cus engendra aussi Nimrod, qui commença d'être puissant sur la terre.
Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
9 Il fut un puissant chasseur devant l'Eternel; c'est pourquoi l'on a dit: Comme Nimrod, le puissant chasseur devant l'Eternel.
Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”
10 Et le commencement de son règne fut Babel, Erec, Accad, et Calné au pays de Sinhar.
Malo oyambirira a ufumu wake anali Babeli, Ereki, Akadi ndi Kaline. Malo onsewa anali mʼdziko la Sinara.
11 De ce pays-là sortit Assur, et il bâtit Ninive, et les rues de la ville, et Calah,
Atachoka mʼdziko limeneli anapita ku Asiriya kumene anakamanga Ninive, Rehoboti-Iri, Kala,
12 Et Résen, entre Ninive et Calah, qui est une grande ville.
ndi Reseni, mzinda waukulu umene uli pakati pa Ninive ndi Kala.
13 Mitsraïm engendra Ludim, Hanamim, Léhabim, Naphtuhim.
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
14 Pathrusim, Chasluhim, desquels sont issus les Philistins, et Caphtorim.
Apaturusi, Akasilu ndi Akafitori (kumene kunachokera Afilisti).
15 Et Canaan engendra Sidon, son fils aîné, et Heth,
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba, Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti;
16 Les Jébusiens, les Amorrhéens, les Guirgasiens,
Ayebusi, Aamori, Agirigasi;
17 Les Héviens, les Harkiens, et les Siniens,
Ahivi, Aariki, Asini,
18 Les Arvadiens, les Tsémariens, et les Hamathiens. Et ensuite les familles des Cananéens se sont dispersées.
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati. Pambuyo pake, mafuko a Akanaani anafalikira ponseponse,
19 Et les limites des Cananéens furent depuis Sidon, quand on vient vers Guérar, jusqu'à Gaza, en tirant vers Sodome et Gomorrhe, Adma, et Tséboïm, jusqu'à Lésa.
mpaka ku malire a Kanaani. Malirewo anachokera ku Sidoni kulowa cha ku Gerari mpaka ku Gaza, ndi kulowa ku Sodomu, Gomora, Adima ndi Zeboimu mpaka ku Lasa.
20 Ce sont là les enfants de Cam selon leurs familles [et leurs] langues, en leurs pays, et en [leurs] nations.
Amenewa ndiwo ana aamuna a Hamu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe amakhala ndi mitundu yawo.
21 Et il naquit des enfants à Sem, père de tous les enfants d'Héber, et frère de Japheth, [qui était] le plus grand.
Semu amene anali mkulu wake wa Yafeti nayenso anabereka nakhala kholo la Eberi.
22 Et les enfants de Sem sont Hélam, Assur, Arpacsad, Lud, et Aram.
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.
23 Et les enfants d'Aram, Hus, Hul, Guéther et Mas.
Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
24 Et Arpacsad engendra Sélah, et Sélah engendra Héber.
Aripakisadi anabereka Sela, ndipo Selayo anabereka Eberi.
25 Et à Héber naquirent deux fils: le nom de l'un fut Péleg, parce qu'en son temps la terre fut partagée; et le nom de son frère fut Joktan.
A Eberi anabereka ana aamuna awiri: Wina anamutcha Pelegi chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
26 Et Joktan engendra Almodad, Séleph, Hatsarmaveth, et Jérah.
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
27 Hadoram, Uzal, Dikla,
Hadoramu, Uzali, Dikila,
28 Hobal, Abimaël, Séba,
Obali, Abimaeli, Seba,
29 Ophir, Havila, et Jobab. Tous ceux-là sont les enfants de Joktan.
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
30 Et leur demeure était depuis Mésa, quand on vient en Séphar, montagne d'Orient.
Chigawo chimene ankakhala chinayambira ku Mesa mpaka ku Seferi, ku dera la mapiri chakummawa.
31 Ce sont là les enfants de Sem, selon leurs familles [et] leurs langues, en leurs pays, et en [leurs] nations.
Amenewa ndiwo ana a Semu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe ankakhala ndi mitundu yawo.
32 Telles sont les familles des enfants de Noé, selon leurs lignées en leurs nations; et de ceux-là ont été divisées les nations sur la terre après le déluge.
Amenewa ndiwo mafuko a ana aamuna a Nowa monga mwa mibado ya mitundu yawo. Mitundu yonse ya anthu inatuluka mwa iwowa ndi kufalikira pa dziko lonse lapansi chitatha chigumula chija.

< Genèse 10 >