< Psaumes 133 >

1 Cantique des degrés. Voyez aujourd'hui qu'il est doux, qu'il est aimable d'avoir des frères, d'habiter dans l'union.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2 C'est comme de la myrrhe sur la tête, comme celle qui descendit sur la barbe d'Aaron, et de là sur la frange de son vêtement;
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3 Ou comme la rosée d'Hermon, qui descend sur les montagnes de Sion; parce que là le Seigneur a voulu que fussent la bénédiction et la vie dans tous les siècles.
Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.

< Psaumes 133 >