< Psalms 82 >

1 — A Psalm of Asaph. God hath stood in the company of God, In the midst God doth judge.
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
2 Till when do ye judge perversely? And the face of the wicked lift up? (Selah)
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
3 Judge ye the weak and fatherless, The afflicted and the poor declare righteous.
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
4 Let the weak and needy escape, From the hand of the wicked deliver them.
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
5 They knew not, nor do they understand, In darkness they walk habitually, Moved are all the foundations of earth.
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
6 I — I have said, 'Gods ye [are], And sons of the Most High — all of you,
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
7 But as man ye die, and as one of the heads ye fall,
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
8 Rise, O God, judge the earth, For Thou hast inheritance among all the nations!
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.

< Psalms 82 >