< Psalms 146 >

1 Alleluya.
Tamandani Yehova. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.
2 Mi soule, herie thou the Lord; Y schal herie the Lord in my lijf, Y schal synge to my God as longe as Y schal be. Nile ye triste in princis;
Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.
3 nether in the sones of men, in whiche is noon helthe.
Musamadalire mafumu, anthu osakhalitsa, amene sangathe kupulumutsa.
4 The spirit of hym schal go out, and he schal turne ayen in to his erthe; in that dai alle the thouytis of hem schulen perische.
Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi; zimene ankafuna kuchita zimatha tsiku lomwelo.
5 He is blessid, of whom the God of Jacob is his helpere, his hope is in his Lord God, that made heuene and erthe;
Wodala ndi amene thandizo lake ndi Mulungu wa Yakobo.
6 the see, and alle thingis that ben in tho.
Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo; Yehova, amene ndi wokhulupirika kwamuyaya.
7 Which kepith treuthe in to the world, makith dom to hem that suffren wrong; yyueth mete to hem that ben hungri. The Lord vnbyndith feterid men;
Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa ndipo amapereka chakudya kwa anthu anjala. Yehova amamasula amʼndende,
8 the Lord liytneth blynde men. The Lord reisith men hurtlid doun; the Lord loueth iust men.
Yehova amatsekula maso anthu osaona, Yehova amadzutsa onse amene awerama pansi, Yehova amakonda anthu olungama.
9 The Lord kepith comelyngis, he schal take vp a modirles child, and widewe; and he schal distrie the weies of synners.
Yehova amasamalira alendo ndipo amathandiza ana ndi akazi amasiye, koma amasokoneza njira za anthu oyipa.
10 The Lord schal regne in to the worldis; Syon, thi God schal regne in generacioun and in to generacioun.
Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya, Mulungu wako iwe Ziyoni, pa mibado yonse. Tamandani Yehova.

< Psalms 146 >