< Micah 1 >

1 The word of the Lord, which was maad to `Mychee of Morasti, in the daies of Joathan, Achas, Ezechie, kyngis of Juda; which word he sai on Samarie, and Jerusalem.
Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu.
2 Here ye, alle puplis, and the erthe perseyue, and plentee therof, and be the Lord God to you in to a witnesse, the Lord fro his hooli temple.
Tamverani, inu anthu a mitundu yonse, mvetsera iwe dziko lapansi ndi okhala mʼmenemo, pakuti Ambuye Yehova achitira umboni wokutsutsani, Ambuye akuyankhula ali mʼnyumba yake yopatulika.
3 For lo! the Lord schal go out of his place, and schal come doun, and schal trede on hiy thingis of erthe.
Taonani! Yehova akubwera kuchokera ku malo ake; Iye akutsika ndipo akuponda pa malo okwera a dziko lapansi.
4 And mounteyns schulen be waastid vndur hym, and valeis schulen be kit, as wex fro the face of fier, as watirs that rennen in to a pit.
Mapiri akusungunuka pansi pake, ndipo zigwa zikugawikana ngati phula pa moto, ngati madzi ochokera mʼphiri.
5 In the grete trespas of Jacob is al this thing, and in the synnes of the hous of Israel. Which is the greet trespas of Jacob? whether not Samarie? and whiche ben the hiy thingis of Juda? whether not Jerusalem?
Zonsezi ndi chifukwa cha cholakwa cha Yakobo, chifukwa cha machimo a nyumba ya Israeli. Kodi cholakwa cha Yakobo nʼchiyani? Kodi si Samariya? Kodi malo achipembedzo a Yuda ndi ati? Kodi si Yerusalemu?
6 And Y schal put Samarie as an heep of stoonys in the feeld, whanne a vynyerd is plauntid; and Y schal drawe awei the stoonys therof in to a valei, and Y schal schewe the foundementis therof.
“Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja, malo odzalamo mphesa. Miyala yake ndidzayitaya ku chigwa ndipo ndidzafukula maziko ake.
7 And alle `grauun ymagis therof schulen be betun togidere, and alle hiris therof schulen be brent in fier; and Y schal putte alle idols therof in to perdicioun; for of hiris of an hoore tho ben gaderid, and `til to hire of an hoore tho schulen turne ayen.
Mafano ake onse ndidzawaphwanyaphwanya; mphatso zake zonse ndidzazitentha ndi moto; ndidzawononga zifanizo zonse za milungu yake. Popeza analandira mphatso zake kuchokera ku malipiro a akazi achiwerewere, mphatsozonso zidzagwiritsidwa ntchito ndi ena ngati malipiro a akazi achiwerewere.”
8 On this thing Y schal weile and yelle, Y schal go spuylid and nakid; Y schal make weilyng of dragouns, and mournyng as of ostrigis.
Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni; ndidzayenda wopanda nsapato ndi wamaliseche. Ndidzafuwula ngati nkhandwe ndi kulira ngati kadzidzi.
9 For wounde therof is dispeirid; for it cam til to Juda, it touchide the yate of my puple, til to Jerusalem.
Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika; chafika ku Yuda. Chafika pa chipata chenicheni cha anthu anga, mpaka mu Yerusalemu mwenimwenimo.
10 In Geth nyle ye telle, bi teeris wepe ye not; in the hous of dust with dust togidere sprynge you.
Musanene zimenezi ku Gati; musalire nʼkomwe. Mugubuduzike mu fumbi ku Beti-Leafura.
11 And ye a fair dwellyng passe, which is confoundid with yuel fame; it is not goon out, which dwellith in the goyng out; a niy hous schal take of you weilyng, which stood to it silf.
Inu anthu okhala ku Safiro, muzipita ku ukapolo muli amaliseche ndi amanyazi. Iwo amene akukhala ku Zanaani sadzatuluka. Beti-Ezeli akulira mwachisoni; chitetezo chake chakuchokerani.
12 For it is maad sijk to good, which dwellith in bitternessis. For yuel cam doun fro the Lord in to the yate of Jerusalem, noise of foure horsid cart,
Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu, akuyembekezera thandizo, chifukwa Yehova wabweretsa tsoka, lafika mpaka pa chipata cha Yerusalemu.
13 of drede to the puple dwellynge at Lachis. It is the bigynnyng of synne of the douyter of Sion, for the grete trespassis of Israel ben foundun in thee.
Inu anthu okhala ku Lakisi mangani akavalo ku magaleta. Inu amene munayamba kuchimwitsa mwana wamkazi wa Ziyoni, pakuti zolakwa za Israeli zinapezeka pakati panu.
14 Therfor he schal yyue werriours on the eritage of Geth, on housis of leesyng in to deseit to kyngis of Israel.
Chifukwa chake perekani mphatso zolawirana ndi a ku Moreseti Gati. Mzinda wa Akizibu udzaonetsa kunama kwa mafumu a Israeli.
15 Yit Y schal brynge an eir to thee, that dwellist in Maresa; the glorie of Israel schal come til to Odolla.
Ndidzabweretsa mgonjetsi kudzalimbana ndi inu okhala mu Maresa. Ulemerero wa Israeli udzafika ku Adulamu.
16 Be thou maad ballid, and be thou clippid on the sones of thi delices; alarge thi ballidnesse as an egle, for thei ben lad caitif fro thee.
Metani mipala mitu yanu kuonetsa kuti mukulirira ana anu amene mumawakonda; mudzichititse dazi ngati dembo, pakuti anawo adzatengedwa pakati panu kupita ku ukapolo.

< Micah 1 >