< Esther 10 >

1 Forsothe kyng Assuerus made tributarye ech lond, and alle the ilis of the see;
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 whos strengthe and empire and dignyte and hiynesse, by which he enhaunside Mardochee, ben writun in the bookis of Medeis and of Persis;
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 and how Mardochee of the kyn of Jewis was the secounde fro king Assuerus, and was greet anentis Jewis, and acceptable to the puple of hise britheren, and he souyte goodis to his puple, and spak tho thingis, that perteyneden to the pees of his seed.
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.

< Esther 10 >