< Mark 15 >

1 Very early in the morning the chief priests met together with [the rest of] the Jewish council, [in order to decide how to accuse Jesus before the Roman governor. Their guards] tied Jesus’ hands [again]. They took him to [the house of] Pilate, [the governor, and they started to accuse him, saying] “[Jesus is claiming that he is a king!]!”
Mmamawa, akulu a ansembe pamodzi ndi akuluakulu, aphunzitsi amalamulo ndi olamulira onse anamanga fundo. Anamumanga Yesu, namutenga ndi kukamupereka kwa Pilato.
2 Pilate asked Jesus, “Do you [claim to be] the king of the Jews?” Jesus answered him, “You yourself have said so.”
Pilato anafunsa kuti, “Kodi Iwe ndi Mfumu ya Ayuda?” Yesu anayankha kuti, “Mwatero ndinu.”
3 Then the chief priests claimed that Jesus had done many bad things.
Akulu a ansembe anamunenera zinthu zambiri.
4 So Pilate asked him again, “Don’t you have anything to say? Listen to how many bad things they are saying that you [have done]!”
Ndipo Pilato anamufunsanso Iye kuti, “Kodi Iwe suyankhapo kanthu? Tamva zinthu zambiri akukunenerazi.”
5 But [even though Jesus was not guilty], he did not say anything more. The result was that Pilate was very much surprised.
Koma Yesu sanayankhebe, ndipo Pilato anadabwa.
6 It was the governor’s custom [each year] during the [Passover] celebration to release [one person who was in prison. He customarily released] whichever prisoner the people requested.
Pa nthawi ya Phwando, panali chizolowezi chomasula munthu wamʼndende amene anthu amupempha.
7 [At that time] there was a man called Barabbas who had been {whom [the soldiers had]} [put in prison with some other men]. Those men had murdered [some soldiers] when they rebelled [against the Roman government].
Munthu wotchedwa Baraba anali mʼndende pamodzi ndi anthu owukira amene anapha anthu pa nthawi ya chipolowe.
8 A crowd approached [Pilate] and asked him [to release someone], just like he customarily did for them [during the Passover celebration].
Gulu la anthu linabwera kwa Pilato ndi kumufunsa kuti awachitire zimene amachita nthawi zonse.
9 Pilate answered them, “Would you like me to release for you the [man whom you] Jewish [people say is your] king?”
“Kodi mukufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?” Pilato anafunsa,
10 [He asked this] because he realized what the chief priests were wanting to do. They were accusing Jesus because they were jealous of him [because many people were becoming his disciples].
podziwa kuti akulu a ansembe anamupereka Yesu kwa iye chifukwa cha nsanje.
11 But the chief priests urged the crowd [to request] that Pilate release Barabbas for them instead [of Jesus].
Koma akulu a ansembe anasonkhezera anthu kuti Pilato amasule Baraba mʼmalo mwa Yesu.
12 Pilate said to them again, “[If I release Barabbas], what do you want me to do with the man whom [some of] you Jews say is [your] king?”
Pilato anawafunsa kuti, “Kodi nanga ndichite chiyani ndi uyu amene mukumutcha mfumu ya Ayuda?”
13 Then they shouted again, “[Command that your soldiers] crucify him!”
Anafuwula kuti, “Mpachikeni!”
14 Then Pilate said to them, “Why? What crime has he committed?” But they shouted even louder, “[Command your soldiers to] crucify him!”
Pilato anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani? Wapalamula mlandu wotani?” Koma anafuwula kwambiri, “Mpachikeni!”
15 So, because Pilate wanted to please the crowd, he released Barabbas for them. Then, after [his soldiers] had whipped Jesus with leather straps into which they had fastened metal pieces, [Pilate told the soldiers to take him away] in order that he would be crucified {they would crucify him}.
Pilato pofuna kuwakondweretsa anthuwo, anawamasulira Baraba. Analamula kuti Yesu akwapulidwe mwankhanza, ndipo anamupereka kuti akapachikidwe.
16 The soldiers took Jesus into the [courtyard of the] palace [where Pilate lived]. That place was the government headquarters. Then they summoned the whole (cohort/group of soldiers) [who were on duty there].
Asilikali anamutenga Yesu ndi kupita naye mʼkati mwa nyumba yaufumu (dera lokhalako asilikali a mfumu) ndipo anasonkhanitsa gulu lonse la asilikali.
17 [After the soldiers gathered together], they put a purple robe on Jesus. Then they placed on his head a crown that they made from [branches of] thornbushes. [They did those things in order to ridicule him by pretending that he was a king].
Anamuveka Iye mwinjiro wofiira, kenaka analuka chipewa cha minga ndi kuyika pa mutu pake.
18 Then they greeted him [like they would greet a king, in order to ridicule him], saying, “Hooray for the King [who rules] the Jews!”
Ndipo anayamba kunena kwa lye kuti, “Ulemu kwa inu Mfumu ya Ayuda!”
19 They repeatedly struck his head with a reed and spat on him. By kneeling down, they [pretended to honor] him.
Ndipo anamugogoda pa mutu mobwerezabwereza ndi ndodo ndi kumulavulira. Anamugwadira ndi kumulambira Iye.
20 When they had finished ridiculing him, they pulled off the purple robe. They put his own clothes on him, and then they led him outside [of the city] in order to nail him to a cross.
Ndipo anamuchita chipongwe, anamuvula mwinjiro wofiira uja ndi kumuveka zovala zake. Kenaka anamutenga kuti akamupachike.
21 [After Jesus carried his cross a short distance], a man named Simon from Cyrene [city came along]. He was the father of Alexander and Rufus. He was passing by while he was returning [home] from outside [the city. The soldiers] compelled Simon to carry the cross [for Jesus].
Munthu wina ochokera ku Kurene, Simoni, abambo a Alekisanda ndi Rufasi amadutsa kuchokera ku dziko la kwawo, ndipo anamuwumiriza kuti anyamule mtanda.
22 They brought them both to a place that they [call] Golgotha. That name means, ‘a place [like] a skull’.
Anafika naye Yesu pa malo otchedwa Gologota (kutanthauza kuti, malo a bade)
23 Then they tried to give Jesus wine that was {that they} mixed with [medicine called] myrrh. [They wanted him to drink it so that he would not feel so much pain when they crucified him]. But he did not drink it.
Kenaka anamupatsa Iye vinyo wosakaniza ndi mure, koma Iye sanamwe.
24 [Some] of the [soldiers took his clothes]. Then they nailed him to a cross. Afterwards, they divided his clothes among themselves by gambling with [something like] dice. They did this [in order to determine] which [piece of clothing] each one would get.
Ndipo anamupachika Iye. Anachita maere ogawana zovala zake kuti aone chimene aliyense angatenge.
25 It was nine o’clock in the morning when they crucified him.
Linali ora lachitatu mmawa pamene anamupachika Yesu.
26 They [attached to the cross above Jesus’ head] a sign on which it had been written {someone had written} the reason why [they were nailing him to the cross]. [But all] that it said was, “The King of the Jews.”
Chikwangwani cholembedwapo mlandu wake chinali choti: mfumu ya ayuda.
27 They also nailed to crosses two men who were bandits. They nailed one to a cross at the right side [of Jesus] and one to a cross at the left side [of Jesus].
Achifwamba awiri anapachikidwanso pamodzi ndi Iye, wina kumanja kwake ndi wina kumanzere kwake.
(Ndipo malemba anakwaniritsidwa amene amati, “Iye anayikidwa mʼgulu la anthu oyipa).”
29 The people who were passing by insulted him by shaking their heads as [if here were an evil man]. They said, “Aha! You said that you would destroy the Temple and then you would build it again within three days.
Amene amadutsa pafupi anamunenera mawu amwano, akupukusa mitu yawo ndi kuti, “Haa! Iwe amene udzawononga Nyumba ya Mulungu ndi kuyimanganso masiku atatu,
30 [If you could do that, then] rescue yourself by coming down from the cross!”
tsika kuchoka pa mtandapo ndipo udzipulumutse wekha!”
31 The chief priests, along with the men who taught the [Jewish] laws, also [wanted to] make fun of Jesus. So they said to each other, “He [claims to have] saved others [from their sicknesses] [IRO] but he cannot save himself!
Chimodzimodzinso akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo anamunyoza Iye pakati pawo. Iwo anati, “Anapulumutsa ena, koma sangathe kudzipulumutsa yekha!
32 He said, ‘I am the Messiah, I am the King who [rules the people of] Israel.’ [If his words are true], he should come down now from the cross! Then we will believe [him]!” The [two] men who were crucified beside him also insulted him.
Musiyeni Khristu, Mfumu ya Aisraeli, atsike tsopano kuchoka pa mtanda, kuti ife tione ndi kukhulupirira.” Iwonso amene anapachikidwa naye pamodzi anamulalatira.
33 At noon the whole land became dark, [and it stayed dark] until three o’clock in the afternoon.
Pa ora lachisanu ndi chimodzi masana mdima unabwera pa dziko lonse mpaka pa ora lachisanu ndi chinayi masana.
34 At three o’clock Jesus shouted loudly, “Eloi, Eloi, lama sabachthani?” That means, “My God, my God, why have you deserted me?”
Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakitani?” Kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?”
35 When some of the people who were standing there heard [the word ‘Eloi’, misunderstanding it], they said, “Listen! He is calling for [the prophet] Elijah!”
Ena amene anali pafupi atamva izi anati, “Tamverani, akuyitana Eliya.”
36 One of them ran and filled a sponge with sour wine. He placed it on [the tip of] a reed, and then he [held it] up for [Jesus] to suck out [the wine that was in] it. [While he was doing that, someone] said, “Wait! Let’s see whether Elijah will come to take him down [from the cross]!”
Munthu wina anathamanga, natenga chinkhupule atachiviyika mu vinyo wosasa, anachizika ku mtengo, ndi kumupatsa Yesu kuti amwe. Munthuyo anati, “Musiyeni yekha tsopano. Tiyeni tione ngati Eliya angabwere kudzamutsitsa.”
37 And then, after Jesus shouted loudly, he stopped breathing [and died].
Ndi mawu ofuwula, Yesu anapuma komaliza.
38 [At that moment] the [heavy thick] curtain that closed off [the most holy place in] the Temple split into two pieces from top to bottom. [That showed that ordinary people could now go into the presence of God].
Chinsalu chotchinga cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati kuyambira pamwamba mpaka pansi.
39 The officer who supervised the soldiers [who nailed Jesus to the cross] was standing in front of Jesus. When he saw how Jesus died, he exclaimed, “Truly, this man was the man who was also God!”
Ndipo Kenturiyo, amene anayima patsogolo pa Yesu, atamva kulira kwake ndi kuona mmene anafera anati, “Zoonadi, uyu anali Mwana wa Mulungu.”
40 There were also some women there, watching these events from a distance. They had accompanied Jesus when he was in Galilee [district], and they had provided what he needed. They had come with him to Jerusalem. Among those women was Mary from Magdala [town]. There was [another] Mary, who was the mother of the younger James and of Joses. There was also Salome.
Amayi ena anali patali kuonerera. Pakati pawo panali Mariya Magadalena, Mariya amayi a Yakobo wamngʼono ndi Yose ndi Salome.
Amayi awa ankamutsatira Iye mu Galileya ndi kumutumikira Iye pa zosowa zake. Amayi enanso ambiri amene anabwera naye ku Yerusalemu analinso pomwepo.
42 When evening was near, [a man named] Joseph from Arimathea [town came there]. He was a member of the [Jewish] council, one whom everyone respected. He was also one of those who had been waiting expectantly for the [time when] God [would send] his king to begin to rule. [He knew that, according to Jewish law, people’s bodies had to be buried] {[someone had to bury people’s bodies]} [on the day they died. He also realized that] it was the day when [people] prepared [things for] ([the Jewish day of rest/the Sabbath]), [and that the Sabbath would start when the sun set]. So he became courageous and went to Pilate and asked Pilate [to permit him to take] the body of Jesus [down from the cross and bury it immediately].
Linali Tsiku Lokonzekera (kunena kuti, tsiku lomwe limatsatizana ndi Sabata). Choncho madzulo atayandikira,
Yosefe wa ku Arimateyu, mkulu wolamulira odziwika bwino, amene amadikirira ufumu wa Mulungu, anapita kwa Pilato molimba mtima ndi kukapempha mtembo wa Yesu.
44 Pilate was surprised [when he heard that] Jesus was already dead. So he summoned the officer who was in charge of the soldiers [who crucified Jesus], and he asked him if [Jesus] had already died.
Pilato anadabwa pakumva kuti anali atamwalira kale. Anayitana Kenturiyo, namufunsa ngati Yesu anali atamwalira kale.
45 When the officer told [Pilate that Jesus was dead], Pilate allowed Joseph [to take away] the body.
Atawuzidwa ndi Kenturiyo kuti zinali motero, anapereka mtembowo kwa Yosefe.
46 After Joseph bought a linen cloth, he [and others] took [Jesus’ body down from the cross]. They wrapped it in the linen cloth and laid it in a tomb that [previously] had been dug out of the rock [cliff]. Then they rolled a [huge flat] stone in front of the entrance to the tomb.
Choncho Yosefe anagula nsalu yabafuta, natsitsa thupi, ndipo analikulunga mʼnsalu, naliyika mʼmanda amene anawagoba pa mwala. Kenaka anagubuduza mwala umene anatseka nawo mandawo.
47 Mary [from] Magdala and Mary the mother of Joses were watching where Jesus’ [body] was placed {where they placed Jesus’ [body]}.
Mariya Magadalena ndi Mariya amayi a Yose anaona kumene anamuyika Yesu.

< Mark 15 >