Aionian Verses

and to arise: rise all son: child his and all daughter his to/for to be sorry: comfort him and to refuse to/for to be sorry: comfort and to say for to go down to(wards) son: child my mourning hell: Sheol [to] and to weep [obj] him father his (Sheol h7585)
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
and to say not to go down son: child my with you for brother: male-sibling his to die and he/she/it to/for alone him to remain and to encounter: chanced him harm in/on/with way: journey which to go: continue in/on/with her and to go down [obj] greyheaded my in/on/with sorrow hell: Sheol [to] (Sheol h7585)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)
and to take: take also [obj] this from from with face: before my and to meet him harm and to go down [obj] greyheaded my in/on/with distress: evil hell: Sheol [to] (Sheol h7585)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol h7585)
and to be like/as to see: see he for nothing [the] youth and to die and to go down servant/slave your [obj] greyheaded servant/slave your father our in/on/with sorrow hell: Sheol [to] (Sheol h7585)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol h7585)
and if creation to create LORD and to open [the] land: soil [obj] lip her and to swallow up [obj] them and [obj] all which to/for them and to go down alive hell: Sheol [to] and to know for to spurn [the] human [the] these [obj] LORD (Sheol h7585)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
and to go down they(masc.) and all which to/for them alive hell: Sheol [to] and to cover upon them [the] land: soil and to perish from midst [the] assembly (Sheol h7585)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
for fire to kindle in/on/with face: anger my and to burn till hell: Sheol lower and to eat land: country/planet and crops her and to kindle foundation mountain: mount (Sheol h7585)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
LORD to die and to live to go down hell: Sheol and to ascend: establish (Sheol h7585)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol h7585)
cord hell: Sheol to turn: surround me to meet me snare death (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
and to make: do like/as wisdom your and not to go down greyheaded his in/on/with peace hell: Sheol (Sheol h7585)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
and now not to clear him for man wise you(m. s.) and to know [obj] which to make: do to/for him and to go down [obj] greyheaded his in/on/with blood hell: Sheol (Sheol h7585)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol h7585)
to end: expend cloud and to go: went so to go down hell: Sheol not to ascend: rise (Sheol h7585)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
height heaven what? to work deep from hell: Sheol what? to know (Sheol h7585)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
who? to give: if only! in/on/with hell: Sheol to treasure me to hide me till to return: turn back face: anger your to set: appoint to/for me statute: portion and to remember me (Sheol h7585)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol h7585)
if to await hell: Sheol house: home my in/on/with darkness to spread bed my (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
alone: pole hell: Sheol to go down if: surely no unitedness upon dust to descend (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
(to end: finish *QK) in/on/with good day their and in/on/with moment hell: Sheol to descend (Sheol h7585)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
dryness also heat to plunder water snow hell: Sheol to sin (Sheol h7585)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol h7585)
naked hell: Sheol before him and nothing covering to/for Abaddon (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
for nothing in/on/with death memorial your in/on/with hell: Sheol who? to give thanks to/for you (Sheol h7585)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
to return: return wicked to/for hell: Sheol [to] all nation forgetful God (Sheol h7585)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
for not to leave: forsake soul my to/for hell: Sheol not to give: allow pious your to/for to see: see Pit: hell (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
cord hell: Sheol to turn: surround me to meet me snare death (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
LORD to ascend: establish from hell: Sheol soul my to live me (from to go down I *QK) pit (Sheol h7585)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
LORD not be ashamed for to call: call to you be ashamed wicked to silence: silent to/for hell: Sheol (Sheol h7585)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
like/as flock to/for hell: Sheol to appoint death to pasture them and to rule in/on/with them upright to/for morning (and rock their *QK) to/for to become old hell: Sheol from elevation to/for him (Sheol h7585)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
surely God to ransom soul my from hand: power hell: Sheol for to take: recieve me (Selah) (Sheol h7585)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
(to deceive death *QK) upon them to go down hell: Sheol alive for bad: evil in/on/with sojourning their in/on/with entrails: inner parts their (Sheol h7585)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
for kindness your great: large upon me and to rescue soul my from hell: Sheol lower (Sheol h7585)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
for to satisfy in/on/with distress: harm soul my and life my to/for hell: Sheol to touch (Sheol h7585)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
who? great man to live and not to see: see death to escape soul his from hand: power hell: Sheol (Selah) (Sheol h7585)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol h7585)
to surround me cord death and terror hell: Sheol to find me distress and sorrow to find (Sheol h7585)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
if to ascend heaven there you(m. s.) and to lay hell: Sheol look! you (Sheol h7585)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol h7585)
like to cleave and to break up/open in/on/with land: country/planet to scatter bone our to/for lip hell: Sheol (Sheol h7585)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
to swallow up them like/as hell: Sheol alive and unblemished: complete like/as to go down pit (Sheol h7585)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
foot her to go down death hell: Sheol step her to grasp (Sheol h7585)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol h7585)
way: journey hell: Sheol house: home her to go down to(wards) chamber death (Sheol h7585)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
and not to know for shade there in/on/with unfathomable hell: Sheol to call: call to her (Sheol h7585)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
hell: Sheol and Abaddon before LORD also for heart son: child man (Sheol h7585)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
way life to/for above [to] to/for be prudent because to turn aside: depart from hell: Sheol beneath (Sheol h7585)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
you(m. s.) in/on/with tribe: staff to smite him and soul his from hell: Sheol to rescue (Sheol h7585)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
hell: Sheol (and destruction his *QK) not to satisfy and eye [the] man not to satisfy (Sheol h7585)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
hell: Sheol and coercion womb land: country/planet not to satisfy water and fire not to say substance (Sheol h7585)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
all which to find hand your to/for to make: do in/on/with strength your to make: do for nothing deed: work and explanation and knowledge and wisdom in/on/with hell: Sheol which you(m. s.) to go: went there [to] (Sheol h7585)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol h7585)
to set: make me like/as signet upon heart your like/as signet upon arm your for strong like/as death love severe like/as hell: Sheol jealousy flash her flash fire flame LORD (Sheol h7585)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
to/for so to enlarge hell: Sheol soul: appetite her and to open lip her to/for without statute: allotment and to go down glory her and crowd her and roar her and exultant in/on/with her (Sheol h7585)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol h7585)
to ask to/for you sign: miraculous from from with LORD God your be deep hell: Sheol or to exult to/for above [to] (Sheol h7585)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol h7585)
hell: Sheol from underneath: under to tremble to/for you to/for to encounter: meet to come (in): come you to rouse to/for you shade all goat land: country/planet to arise: raise from throne their all king nation (Sheol h7585)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
to go down hell: Sheol pride your sound harp your underneath: under you to lay worm and covering your worm (Sheol h7585)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
surely to(wards) hell: Sheol to go down to(wards) flank pit (Sheol h7585)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
for to say to cut: make(covenant) covenant with death and with hell: Sheol to make seer (whip *QK) to overflow for (to pass *QK) not to come (in): come us for to set: make lie refuge our and in/on/with deception to hide (Sheol h7585)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
and to atone covenant your with death and vision your with hell: Sheol not to arise: establish whip to overflow for to pass and to be to/for him to/for trampling (Sheol h7585)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
I to say in/on/with quiet day my to go: went in/on/with gate hell: Sheol to reckon: put remainder year my (Sheol h7585)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol h7585)
for not hell: Sheol to give thanks you death to boast: praise you not to await to go down pit to(wards) truth: faithful your (Sheol h7585)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol h7585)
and to travel to/for king in/on/with oil and to multiply perfumery your and to send: depart envoy your till from distant and to abase till hell: Sheol (Sheol h7585)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
thus to say Lord YHWH/God in/on/with day to go down he hell: Sheol [to] to mourn to cover upon him [obj] abyss and to withhold river her and to restrain water many and be dark upon him Lebanon and all tree [the] land: country upon him fainting (Sheol h7585)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol h7585)
from voice: sound carcass his to shake nation in/on/with to go down I [obj] him hell: Sheol [to] with to go down pit and to be sorry: comfort in/on/with land: country/planet lower all tree Eden best and pleasant Lebanon all to drink water (Sheol h7585)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol h7585)
also they(masc.) with him to go down hell: Sheol [to] to(wards) slain: killed sword and arm his to dwell in/on/with shadow his in/on/with midst nation (Sheol h7585)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol h7585)
to speak: speak to/for him leader mighty man from midst hell: Sheol with to help him to go down to lie down: lay down [the] uncircumcised slain: killed sword (Sheol h7585)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol h7585)
and not to lie down: be dead with mighty man to fall: fall from uncircumcised which to go down hell: Sheol in/on/with article/utensil battle their and to give: put [obj] sword their underneath: under head their and to be iniquity: crime their upon bone their for terror mighty man in/on/with land: country/planet alive (Sheol h7585)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol h7585)
from hand: power hell: Sheol to ransom them from death to redeem: redeem them where? pestilence your death where? destruction your hell: Sheol repentance to hide from eye my (Sheol h7585)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
if to dig in/on/with hell: Sheol from there hand: power my to take: take them and if to ascend: rise [the] heaven from there to go down them (Sheol h7585)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol h7585)
and to say to call: call to from distress to/for me to(wards) LORD and to answer me from belly: abdomen hell: Sheol to cry to hear: hear voice my (Sheol h7585)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
and also for [the] wine to act treacherously great man proud and not to dwell which to enlarge like/as hell: Sheol soul: appetite his and he/she/it like/as death and not to satisfy and to gather to(wards) him all [the] nation and to gather to(wards) him all [the] people (Sheol h7585)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol h7585)
I/we then to say you that/since: that all the/this/who to anger the/this/who brother it/s/he (in vain *KO) liable for to be the/this/who judgment which then if to say the/this/who brother it/s/he fool liable for to be the/this/who council which then if to say foolish liable for to be toward the/this/who hell: Gehenna the/this/who fire (Geenna g1067)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
if then the/this/who eye you the/this/who right to cause to stumble you to take out/select it/s/he and to throw: throw away from you be profitable for you in order that/to to destroy one the/this/who member you and not all the/this/who body you to throw: throw toward hell: Gehenna (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
and if the/this/who right you hand to cause to stumble you to prevent it/s/he and to throw: throw away from you be profitable for you in order that/to to destroy one the/this/who member you and not all the/this/who body you toward hell: Gehenna (to go away *N+KO) (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
and not (to fear *N+kO) away from the/this/who to kill the/this/who body the/this/who then soul not be able to kill (to fear *N+kO) then more: rather the/this/who be able and (the/this/who *o) soul and (the/this/who *o) body to destroy in/on/among hell: Gehenna (Geenna g1067)
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna g1067)
and you Capernaum (not *N+KO) until (the/this/who *k) heaven (to lift up *N+kO) until hell: Hades (to come/go down *N+kO) that/since: since if in/on/among Sodom (to be *N+kO) the/this/who power the/this/who to be in/on/among you (to stay *N+kO) if until the/this/who today (Hadēs g86)
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
and which (if *N+kO) to say word according to the/this/who son the/this/who a human to release: forgive it/s/he which then if to say according to the/this/who spirit/breath: spirit the/this/who holy no to release: forgive it/s/he neither in/on/among this/he/she/it the/this/who (now *O) an age: age neither in/on/among the/this/who to ensue (aiōn g165)
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
the/this/who then toward the/this/who a thorn to sow this/he/she/it to be the/this/who the/this/who word to hear and the/this/who concern the/this/who an age: age (this/he/she/it *ko) and the/this/who deceit the/this/who riches to choke the/this/who word and unfruitful to be (aiōn g165)
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn g165)
the/this/who then enemy the/this/who to sow it/s/he to be the/this/who devilish/the Devil the/this/who then harvest consummation (the/this/who *k) an age: age to be the/this/who then reaper angel to be (aiōn g165)
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn g165)
just as therefore/then to collect the/this/who weed and fire (to burn *NK+o) thus(-ly) to be in/on/among the/this/who consummation the/this/who an age: age (this/he/she/it *k) (aiōn g165)
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn g165)
thus(-ly) to be in/on/among the/this/who consummation the/this/who an age: age to go out the/this/who angel and to separate the/this/who evil/bad out from midst the/this/who just (aiōn g165)
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn g165)
I/we and then you to say that/since: that you to be Peter and upon/to/against this/he/she/it the/this/who rock to build me the/this/who assembly and gate hell: Hades no to prevail it/s/he (Hadēs g86)
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs g86)
if then the/this/who hand you or the/this/who foot you to cause to stumble you to prevent (it/s/he *N+KO) and to throw: throw away from you good you to be to enter toward the/this/who life crippled or lame or two hand or two foot to have/be to throw: throw toward the/this/who fire the/this/who eternal (aiōnios g166)
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios g166)
and if the/this/who eye you to cause to stumble you to take out/select it/s/he and to throw: throw away from you good you to be one-eyed toward the/this/who life to enter or two eye to have/be to throw: throw toward the/this/who hell: Gehenna the/this/who fire (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna g1067)
and look! one to come near/agree it/s/he to say teacher (good *K) which? good to do/make: do in order that/to (to have/be *N+kO) life eternal (aiōnios g166)
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios g166)
and all (who/which *N+kO) to release: leave home or brother or sister or father or mother or (woman: wife or *KO) child or field because of the/this/who name (me *NK+o) (a hundred times *NK+O) to take and life eternal to inherit (aiōnios g166)
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios g166)
and to perceive: see fig tree one upon/to/against the/this/who road to come/go upon/to/against it/s/he and none to find/meet in/on/among it/s/he if: not not leaf alone and to say it/s/he (no *o) never again out from you fruit to be toward the/this/who an age: eternity and to dry instantly the/this/who fig tree (aiōn g165)
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
woe! you scribe and Pharisee hypocrite that/since: since to take/go around the/this/who sea and the/this/who dried up/withered to do/make: do one proselyte and when(-ever) to be to do/make: do it/s/he son hell: Gehenna double you (Geenna g1067)
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna g1067)
snake offspring snake how! to flee away from the/this/who judgment the/this/who hell: Gehenna (Geenna g1067)
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna g1067)
to sit then it/s/he upon/to/against the/this/who mountain the/this/who Olivet to come near/agree it/s/he the/this/who disciple according to one's own/private to say to say me when? this/he/she/it to be and which? the/this/who sign the/this/who you coming and (the/this/who *k) consummation the/this/who an age: age (aiōn g165)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
then to say and the/this/who out from left/south to travel away from I/we the/this/who to curse toward the/this/who fire the/this/who eternal the/this/who to make ready the/this/who devilish/the Devil and the/this/who angel it/s/he (aiōnios g166)
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
and to go away this/he/she/it toward punishment eternal the/this/who then just toward life eternal (aiōnios g166)
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
to teach it/s/he to keep: observe all just as/how much to order you and look! I/we with/after you to be all the/this/who day until the/this/who consummation the/this/who an age: age (amen *KO) (aiōn g165)
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn g165)
which then if to blaspheme toward the/this/who spirit/breath: spirit the/this/who holy no to have/be forgiveness toward the/this/who an age: eternity but liable for to be eternal (sin *N+KO) (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
and the/this/who concern the/this/who (an age: age *NK+O) (this/he/she/it *k) and the/this/who deceit the/this/who riches and the/this/who about the/this/who remaining desire to enter to choke the/this/who word and unfruitful to be (aiōn g165)
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
and if (to cause to stumble *NK+o) you the/this/who hand you to cut off it/s/he good to be (you *N+kO) crippled to enter toward the/this/who life or the/this/who two hand to have/be to go away toward the/this/who hell: Gehenna toward the/this/who fire the/this/who unquenchable (Geenna g1067)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
and if the/this/who foot you to cause to stumble you to cut off it/s/he good to be (you *N+kO) to enter toward the/this/who life lame or the/this/who two foot to have/be to throw: throw toward the/this/who hell: Gehenna (toward the/this/who fire the/this/who unquenchable *KO) (Geenna g1067)
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
and if the/this/who eye you to cause to stumble you to expel it/s/he good (you *N+kO) to be one-eyed to enter toward the/this/who kingdom the/this/who God or two eye to have/be to throw: throw toward the/this/who hell: Gehenna (the/this/who fire *K) (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
and to depart it/s/he toward road to hasten one and to kneel it/s/he to question it/s/he teacher good which? to do/make: do in order that/to life eternal to inherit (aiōnios g166)
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
if not to take a hundred times now in/on/among the/this/who time/right time this/he/she/it home and brother and sister and (mother *NK+o) and child and field with/after persecution and in/on/among the/this/who an age: age the/this/who to come/go life eternal (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn g165, aiōnios g166)
and to answer (the/this/who Jesus *k) to say it/s/he never again toward the/this/who an age: eternity out from you nothing fruit to eat and to hear the/this/who disciple it/s/he (aiōn g165)
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn g165)
and to reign upon/to/against the/this/who house: household Jacob toward the/this/who an age: eternity and the/this/who kingdom it/s/he no to be goal/tax (aiōn g165)
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn g165)
as/just as to speak to/with the/this/who father me the/this/who Abraham and the/this/who seed: offspring it/s/he toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn g165)
as/just as to speak through/because of mouth the/this/who holy (the/this/who *k) away from an age: age prophet it/s/he (aiōn g165)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn g165)
and (to plead/comfort *N+kO) it/s/he in order that/to not to command it/s/he toward the/this/who abyss to go away (Abyssos g12)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
and you Capernaum (not *N+kO) until (the/this/who *k) heaven (to lift up *N+kO) until (the/this/who *no) hell: Hades (to come/go down *N+kO) (Hadēs g86)
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
and look! lawyer one to arise to test/tempt it/s/he (and *ko) to say teacher which? to do/make: do life eternal to inherit (aiōnios g166)
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
to show then you which? to fear to fear the/this/who with/after the/this/who to kill to have/be authority to throw in toward the/this/who hell: Gehenna yes to say you this/he/she/it to fear (Geenna g1067)
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
and to praise the/this/who lord: master the/this/who manager the/this/who unrighteousness that/since: since shrewdly to do/make: do that/since: since the/this/who son the/this/who an age: age this/he/she/it thoughtful above/for the/this/who son the/this/who light toward the/this/who generation the/this/who themself to be (aiōn g165)
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
and I/we you to say themself to do/make: do friendly/friend out from the/this/who wealth the/this/who unrighteousness in order that/to when(-ever) (to fail *N+KO) to receive you toward the/this/who eternal tent (aiōnios g166)
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
and in/on/among the/this/who hell: Hades to lift up the/this/who eye it/s/he be already in/on/among torment to see: see (the/this/who *k) Abraham away from from afar and Lazarus in/on/among the/this/who bosom it/s/he (Hadēs g86)
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
and to question one it/s/he ruler to say teacher good which? to do/make: do life eternal to inherit (aiōnios g166)
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
which (not! *N+kO) not (to get back *NK+o) many times more in/on/among the/this/who time/right time this/he/she/it and in/on/among the/this/who an age: age the/this/who to come/go life eternal (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
and (to answer *k) to say it/s/he the/this/who Jesus the/this/who son the/this/who an age: age this/he/she/it to marry and (to give in marriage *N+kO) (aiōn g165)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn g165)
the/this/who then to consider worthy the/this/who an age: age that to obtain/happen and the/this/who resurrection the/this/who out from dead neither to marry neither (to give in marriage *N+k+o) (aiōn g165)
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn g165)
in order that/to all the/this/who to trust (in) (in/on/among it/s/he *N+kO) (not to destroy but *K) to have/be life eternal (aiōnios g166)
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
thus(-ly) for to love the/this/who God the/this/who world so the/this/who son (it/s/he *ko) the/this/who unique to give in order that/to all the/this/who to trust (in) toward it/s/he not to destroy but to have/be life eternal (aiōnios g166)
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
the/this/who to trust (in) toward the/this/who son to have/be life eternal the/this/who then to disobey the/this/who son no to appear life but the/this/who wrath the/this/who God to stay upon/to/against it/s/he (aiōnios g166)
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios g166)
which then if to drink out from the/this/who water which I/we to give it/s/he no not (to thirst *N+kO) toward the/this/who an age: eternity but the/this/who water which to give it/s/he to be in/on/among it/s/he flow water to spring toward life eternal (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
(and *k) the/this/who to reap wage to take and to assemble fruit toward life eternal in order that/to (and *k) the/this/who to sow together to rejoice and the/this/who to reap (aiōnios g166)
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
amen amen to say you that/since: that the/this/who the/this/who word me to hear and to trust (in) the/this/who to send me to have/be life eternal and toward judgment no to come/go but to depart out from the/this/who death toward the/this/who life (aiōnios g166)
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios g166)
to look for/into the/this/who a writing that/since: since you to think in/on/among it/s/he life eternal to have/be and that to be the/this/who to testify about I/we (aiōnios g166)
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios g166)
to work not the/this/who eating the/this/who to destroy but the/this/who eating the/this/who to stay toward life eternal which the/this/who son the/this/who a human you to give this/he/she/it for the/this/who father to seal the/this/who God (aiōnios g166)
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios g166)
this/he/she/it (for *N+kO) to be the/this/who will/desire the/this/who (father *N+KO) (me *N+kO) in order that/to all the/this/who to see/experience the/this/who son and to trust (in) toward it/s/he to have/be life eternal and to arise it/s/he I/we (in/on/among *n) the/this/who last/least day (aiōnios g166)
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios g166)
amen amen to say you the/this/who to trust (in) (toward I/we *KO) to have/be life eternal (aiōnios g166)
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios g166)
I/we to be the/this/who bread the/this/who to live the/this/who out from the/this/who heaven to come/go down if one to eat out from this/he/she/it the/this/who bread (to live *N+kO) toward the/this/who an age: eternity and the/this/who bread then which I/we to give the/this/who flesh me to be (which I/we to give *K) above/for the/this/who the/this/who world life (aiōn g165)
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn g165)
the/this/who to eat me the/this/who flesh and to drink me the/this/who blood to have/be life eternal I/we and to arise it/s/he the/this/who last/least day (aiōnios g166)
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios g166)
this/he/she/it to be the/this/who bread the/this/who out from (the/this/who *k) heaven to come/go down no as/just as to eat the/this/who father (you *K) (the/this/who *k) (manna *K) and to die the/this/who to eat this/he/she/it the/this/who bread (to live *N+kO) toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn g165)
to answer (therefore/then *K) it/s/he Simon Peter lord: God to/with which? to go away declaration life eternal to have/be (aiōnios g166)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios g166)
the/this/who then slave no to stay in/on/among the/this/who home toward the/this/who an age: eternity the/this/who (then *o) son to stay toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn g165)
amen amen to say you if one the/this/who I/we word (the/this/who *k) to keep: observe death no not to see/experience toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn g165)
to say therefore/then it/s/he the/this/who Jew now to know that/since: that demon to have/be Abraham to die and the/this/who prophet and you to say if one the/this/who word me to keep: observe no not (to taste *N+kO) death toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn g165)
out from the/this/who an age: age no to hear that/since: that to open one eye blind to beget (aiōn g165)
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
I/we and to give it/s/he life eternal and no not to destroy toward the/this/who an age: eternity and no to seize one it/s/he out from the/this/who hand me (aiōn g165, aiōnios g166)
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn g165, aiōnios g166)
and all the/this/who to live and to trust (in) toward I/we no not to die toward the/this/who an age: eternity to trust (in) this/he/she/it (aiōn g165)
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn g165)
the/this/who to love the/this/who soul: life it/s/he (to destroy *N+kO) it/s/he and the/this/who to hate the/this/who soul: life it/s/he in/on/among the/this/who world this/he/she/it toward life eternal to keep/guard: protect it/s/he (aiōnios g166)
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
to answer (therefore/then *NO) it/s/he the/this/who crowd me to hear out from the/this/who law that/since: that the/this/who Christ to stay toward the/this/who an age: eternity and how! to say you that/since: that be necessary to lift up the/this/who son the/this/who a human which? to be this/he/she/it the/this/who son the/this/who a human (aiōn g165)
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
and to know that/since: that the/this/who commandment it/s/he life eternal to be which therefore/then I/we to speak as/just as to say me the/this/who father thus(-ly) to speak (aiōnios g166)
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
to say it/s/he Peter no not to wash me the/this/who foot toward the/this/who an age: eternity to answer (the/this/who *k) Jesus it/s/he if not to wash you no to have/be part with/after I/we (aiōn g165)
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
I/we and to ask the/this/who father and another counsellor to give you in order that/to with/after you toward the/this/who an age: eternity (to be *N+kO) (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
as/just as to give it/s/he authority all flesh in order that/to all which to give it/s/he (to give *NK+o) it/s/he life eternal (aiōnios g166)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
this/he/she/it then to be the/this/who eternal life in order that/to to know you the/this/who alone true God and which to send Jesus Christ (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
that/since: since no to leave behind the/this/who soul me toward (hell: Hades *N+kO) nor to give the/this/who sacred you to perceive: see decay (Hadēs g86)
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs g86)
to foresee to speak about the/this/who resurrection the/this/who Christ that/since: that (neither to leave behind *N+kO) (the/this/who soul it/s/he *K) toward (hell: Hades neither *N+kO) the/this/who flesh it/s/he to perceive: see decay (Hadēs g86)
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs g86)
which be necessary heaven on the other hand to receive until time restoration all which to speak the/this/who God through/because of mouth (all *K) the/this/who holy away from an age: eternity it/s/he prophet (aiōn g165)
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn g165)
to preach boldly (and/both *N+kO) the/this/who Paul and the/this/who Barnabas to say you to be necessary first to speak the/this/who word the/this/who God since (then *ko) to reject it/s/he and no worthy to judge themself the/this/who eternal life look! to turn toward the/this/who Gentiles (aiōnios g166)
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios g166)
to hear then the/this/who Gentiles (to rejoice *NK+o) and to glorify the/this/who word the/this/who (lord: God *NK+O) and to trust (in) just as/how much to be to appoint toward life eternal (aiōnios g166)
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios g166)
acquainted with away from an age: eternity (to be the/this/who God all the/this/who work it/s/he *K) (aiōn g165)
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
the/this/who for invisible it/s/he away from creation world the/this/who workmanship to understand to perceive the/this/who and/both eternal it/s/he power and divinity toward the/this/who to exist it/s/he inexcusable (aïdios g126)
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios g126)
who/which to exchange the/this/who truth the/this/who God in/on/among the/this/who lie and to worship and to minister the/this/who creation from/with/beside the/this/who to create which to be praiseworthy toward the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
the/this/who on the other hand according to perseverance work good glory and honor and incorruptibility to seek life eternal (aiōnios g166)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
in order that/to just as to reign the/this/who sin in/on/among the/this/who death thus(-ly) and the/this/who grace to reign through/because of righteousness toward life eternal through/because of Jesus Christ the/this/who lord: God me (aiōnios g166)
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios g166)
now then to set free away from the/this/who sin to enslave then the/this/who God to have/be the/this/who fruit you toward holiness the/this/who then goal/tax life eternal (aiōnios g166)
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
the/this/who for compensation the/this/who sin death the/this/who then gift the/this/who God life eternal in/on/among Christ Jesus the/this/who lord: God me (aiōnios g166)
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios g166)
which the/this/who father and out from which the/this/who Christ the/this/who according to flesh the/this/who to be upon/to/against all God praiseworthy toward the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
or which? to come/go down toward the/this/who abyss this/he/she/it to be Christ out from dead to lead (Abyssos g12)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
to confine for the/this/who God the/this/who all toward disobedience in order that/to the/this/who all to have mercy (eleēsē g1653)
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
that/since: since out from it/s/he and through/because of it/s/he and toward it/s/he the/this/who all it/s/he the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
and not (to conform to *NK+o) the/this/who an age: age this/he/she/it but (to transform *NK+o) the/this/who renewal the/this/who mind (you *k) toward the/this/who to test you which? the/this/who will/desire the/this/who God the/this/who good and well-pleasing and perfect (aiōn g165)
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn g165)
the/this/who then be able you to establish according to the/this/who gospel me and the/this/who preaching Jesus Christ according to revelation mystery time eternal be silent (aiōnios g166)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
to reveal then now through/because of and/both a writing prophetic according to command the/this/who eternal God toward obedience faith toward all the/this/who Gentiles to make known (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
alone wise God through/because of Jesus Christ which the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity amen (to/with Roman to write away from Corinth through/because of Phoebe the/this/who servant the/this/who in/on/among Cenchreae assembly *K) (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)
where? wise where? scribe where? debater the/this/who an age: age this/he/she/it not! be foolish the/this/who God the/this/who wisdom the/this/who world (this/he/she/it *k) (aiōn g165)
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn g165)
wisdom then to speak in/on/among the/this/who perfect wisdom then no the/this/who an age: age this/he/she/it nor the/this/who ruler the/this/who an age: age this/he/she/it the/this/who to abate (aiōn g165)
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn g165)
but to speak God wisdom in/on/among mystery the/this/who to conceal which to predestine the/this/who God before the/this/who an age: age toward glory me (aiōn g165)
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn g165)
which none the/this/who ruler the/this/who an age: age this/he/she/it to know if for to know no if the/this/who lord: God the/this/who glory to crucify (aiōn g165)
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn g165)
nothing themself to deceive if one to think wise to exist in/on/among you in/on/among the/this/who an age: age this/he/she/it foolish to be in order that/to to be wise (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
for if food to cause to stumble the/this/who brother me no not to eat meat toward the/this/who an age: eternity in order that/to not the/this/who brother me to cause to stumble (aiōn g165)
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn g165)
this/he/she/it then (all *K) (figuratively to happen *N+kO) that to write then to/with admonition me toward which the/this/who goal/tax the/this/who an age: age (to come to *N+kO) (aiōn g165)
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn g165)
where? you death the/this/who victory where? you (hell: Hades *N+KO) the/this/who sting (Hadēs g86)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
in/on/among which the/this/who God the/this/who an age: age this/he/she/it to blind the/this/who mind/thought the/this/who unbelieving toward the/this/who not to see (it/s/he *k) the/this/who light the/this/who gospel the/this/who glory the/this/who Christ which to be image the/this/who God (aiōn g165)
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn g165)
the/this/who for momentary light the/this/who pressure me according to surpassing toward surpassing eternal burden glory to workout/produce me (aiōnios g166)
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios g166)
not to watch out me the/this/who to see but the/this/who not to see the/this/who for to see temporary the/this/who then not to see eternal (aiōnios g166)
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios g166)
to know for that/since: that if the/this/who earthly me home the/this/who tent to destroy/lodge building out from God to have/be home not man-made eternal in/on/among the/this/who heaven (aiōnios g166)
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios g166)
as/just as to write to scatter to give the/this/who poor the/this/who righteousness it/s/he to stay toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
the/this/who God and father the/this/who lord: God (me *k) Jesus (Christ *K) to know the/this/who to be praiseworthy toward the/this/who an age: eternity that/since: that no to lie (aiōn g165)
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
the/this/who to give themself (above/for *NK+o) the/this/who sin me that to take out/select me out from the/this/who an age: age the/this/who be present evil/bad according to the/this/who will/desire the/this/who God and father me (aiōn g165)
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
which the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
that/since: since the/this/who to sow toward the/this/who flesh themself out from the/this/who flesh to reap corruption the/this/who then to sow toward the/this/who spirit/breath: spirit out from the/this/who spirit/breath: spirit to reap life eternal (aiōnios g166)
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios g166)
above all beginning and authority and power and lordship and all name to name no alone in/on/among the/this/who an age: age this/he/she/it but and in/on/among the/this/who to ensue (aiōn g165)
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
in/on/among which once/when to walk according to the/this/who an age: age the/this/who world this/he/she/it according to the/this/who ruler the/this/who authority the/this/who air the/this/who spirit/breath: spirit the/this/who now be active in/on/among the/this/who son the/this/who disobedience (aiōn g165)
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn g165)
in order that/to to show in/on/among the/this/who an age: age the/this/who to arrive/invade (the/this/who to surpass riches *N+kO) the/this/who grace it/s/he in/on/among kindness upon/to/against me in/on/among Christ Jesus (aiōn g165)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn g165)
and to illuminate all which? the/this/who (management *N+KO) the/this/who mystery the/this/who to conceal away from the/this/who an age: age in/on/among the/this/who God the/this/who the/this/who all to create (through/because of Jesus Christ *K) (aiōn g165)
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn g165)
according to purpose the/this/who an age: eternity which to do/make: do in/on/among (the/this/who *no) Christ Jesus the/this/who lord: God me (aiōn g165)
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn g165)
it/s/he the/this/who glory in/on/among the/this/who assembly (and *no) in/on/among Christ Jesus toward all the/this/who generation the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
that/since: since no to be me the/this/who struggle to/with blood and flesh but to/with the/this/who beginning to/with the/this/who authority to/with the/this/who world power the/this/who darkness (the/this/who *k) (an age: age *K) this/he/she/it to/with the/this/who spiritual the/this/who evil in/on/among the/this/who heavenly (aiōn g165)
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn g165)
the/this/who then God and father me the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
the/this/who mystery the/this/who to conceal away from the/this/who an age: age and away from the/this/who generation (now *N+kO) then to reveal the/this/who holy: saint it/s/he (aiōn g165)
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn g165)
who/which condemnation to pay destructive eternal away from face the/this/who lord: God and away from the/this/who glory the/this/who strength it/s/he (aiōnios g166)
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
it/s/he then the/this/who lord: God me Jesus Christ and the/this/who God (the/this/who *N+KO) father me the/this/who to love me and to give encouragement eternal and hope good in/on/among grace (aiōnios g166)
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios g166)
but through/because of this/he/she/it to have mercy in order that/to in/on/among I/we first: best to show Christ Jesus the/this/who (all *N+KO) patience to/with example the/this/who to ensue to trust (in) upon/to/against it/s/he toward life eternal (aiōnios g166)
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios g166)
the/this/who then king the/this/who an age: eternity incorruptible invisible alone (wise *K) God honor and glory toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
to struggle the/this/who good fight the/this/who faith to catch the/this/who eternal life toward which (and *k) to call: call and to confess/profess the/this/who good confession before much witness (aiōnios g166)
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
the/this/who alone to have/be immortality light to dwell unapproachable which to perceive: see none a human nor to perceive: see be able which honor and power eternal amen (aiōnios g166)
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
the/this/who rich in/on/among the/this/who now an age: age to order not be arrogant nor to hope/expect upon/to/against riches uncertainty but (upon/to/against *N+kO) (the/this/who *k) God (the/this/who to live *K) the/this/who to furnish occasion me all richly toward enjoyment (aiōn g165)
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
the/this/who to save me and to call: call calling holy no according to the/this/who work me but according to one's own/private purpose and grace the/this/who to give me in/on/among Christ Jesus before time eternal (aiōnios g166)
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
through/because of this/he/she/it all to remain/endure through/because of the/this/who select in order that/to and it/s/he salvation to obtain/happen the/this/who in/on/among Christ Jesus with/after glory eternal (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
Demas for me (to leave behind *NK+o) to love the/this/who now an age: age and to travel toward Thessalonica Crescens toward Galatia Titus toward Dalmatia (aiōn g165)
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn g165)
(and *k) to rescue me the/this/who lord: God away from all work evil/bad and to save toward the/this/who kingdom it/s/he the/this/who heavenly which the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn g165)
upon/to/against hope life eternal which to profess the/this/who not a liar God before time eternal (aiōnios g166)
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
to instruct me in order that/to to deny the/this/who ungodlinessness and the/this/who earthly desire in self-control and rightly and piously to live in/on/among the/this/who now an age: age (aiōn g165)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
in order that/to to justify the/this/who that grace heir (to be *N+kO) according to hope life eternal (aiōnios g166)
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios g166)
perhaps for through/because of this/he/she/it to separate/leave to/with hour in order that/to eternal it/s/he to have in full (aiōnios g166)
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
upon/to/against (last/least *N+kO) the/this/who day this/he/she/it to speak me in/on/among son which to place heir all through/because of which and to do/make: do the/this/who an age: age (aiōn g165)
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
to/with then the/this/who son the/this/who throne you the/this/who God toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (and *no) the/this/who rod (the/this/who *no) righteousness rod the/this/who kingdom (you *NK+O) (aiōn g165)
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
as/just as and in/on/among other to say you priest toward the/this/who an age: eternity according to the/this/who order Melchizedek (aiōn g165)
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
and to perfect to be all the/this/who to obey it/s/he causer salvation eternal (aiōnios g166)
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios g166)
baptism (teaching *NK+o) laying on and/both hand resurrection and/both dead and judgment eternal (aiōnios g166)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios g166)
and good to taste God declaration power and/both to ensue an age: age (aiōn g165)
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn g165)
where(-ever) forerunner above/for me to enter Jesus according to the/this/who order Melchizedek high-priest to be toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn g165)
(to testify *N+kO) for that/since: that you priest toward the/this/who an age: eternity according to the/this/who order Melchizedek (aiōn g165)
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
the/this/who on the other hand for without oath to be priest to be the/this/who then with/after oath through/because of the/this/who to say to/with it/s/he to swear lord: God and no to repent you priest toward the/this/who an age: eternity (according to the/this/who order Melchizedek *K) (aiōn g165)
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn g165)
the/this/who then through/because of the/this/who to stay it/s/he toward the/this/who an age: eternity permanent to have/be the/this/who priesthood (aiōn g165)
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn g165)
the/this/who law for a human to appoint/conduct high-priest to have/be weakness: weak the/this/who word then the/this/who oath the/this/who with/after the/this/who law son toward the/this/who an age: eternity to perfect (aiōn g165)
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn g165)
nor through/because of blood he-goat and calf through/because of then the/this/who one's own/private blood to enter once/at once toward the/this/who Holy Place eternal redemption to find/meet (aiōnios g166)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
how much/many? more the/this/who blood the/this/who Christ which through/because of spirit/breath: spirit eternal themself to bring to blameless the/this/who God to clean the/this/who conscience (me *N+KO) away from dead work toward the/this/who to minister God to live (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
and through/because of this/he/she/it covenant new mediator to be that death to be toward redemption the/this/who upon/to/against the/this/who first covenant transgression the/this/who promise to take the/this/who to call: call the/this/who eternal inheritance (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
since be necessary it/s/he often to suffer away from beginning world (now *N+kO) then once upon/to/against consummation the/this/who an age: age toward nullification (the/this/who *no) sin through/because of the/this/who sacrifice it/s/he to reveal (aiōn g165)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
faith to understand to complete the/this/who an age: age declaration God toward the/this/who not out from to shine/appear (the/this/who to see *N+kO) to be (aiōn g165)
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn g165)
Jesus Christ yesterday and today the/this/who it/s/he and toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn g165)
the/this/who then God the/this/who peace the/this/who to lead out from dead the/this/who shepherd the/this/who sheep the/this/who great in/on/among blood covenant eternal the/this/who lord: God me Jesus (aiōnios g166)
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios g166)
to complete you in/on/among all (work *KO) good toward the/this/who to do/make: do the/this/who will/desire it/s/he to do/make: do in/on/among (me *N+KO) the/this/who well-pleasing before it/s/he through/because of Jesus Christ which the/this/who glory toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn g165)
and the/this/who tongue fire the/this/who world the/this/who unrighteousness (thus(-ly) *k) the/this/who tongue to appoint/conduct in/on/among the/this/who member me the/this/who to stain all the/this/who body and to kindle the/this/who course/wheel the/this/who origin and to kindle by/under: by the/this/who hell: Gehenna (Geenna g1067)
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna g1067)
to beget no out from seed perishable but incorruptible through/because of word to live God and to stay (toward the/this/who an age: eternity *K) (aiōn g165)
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn g165)
the/this/who then declaration lord: God to stay toward the/this/who an age: eternity this/he/she/it then to be the/this/who declaration the/this/who to speak good news toward you (aiōn g165)
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn g165)
if one to speak as/when oracles God if one to serve as/when out from strength (which *NK+o) to provide the/this/who God in order that/to in/on/among all to glorify the/this/who God through/because of Jesus Christ which to be the/this/who glory and the/this/who power toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
the/this/who then God all grace the/this/who to call: call (you *N+KO) toward the/this/who eternal it/s/he glory in/on/among Christ Jesus little/few to suffer it/s/he (to complete *N+kO) (you *k) (to establish to strengthen to found *N+kO) (aiōnios g166)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
it/s/he (the/this/who glory and *K) the/this/who power toward the/this/who an age: eternity (the/this/who *ko) (an age: eternity *KO) amen (aiōn g165)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
thus(-ly) for richly to supply you the/this/who entry toward the/this/who eternal kingdom the/this/who lord: God me and savior Jesus Christ (aiōnios g166)
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
if for the/this/who God angel to sin no to spare but (chain *NK+O) darkness hell: Tartarus to deliver toward judgment (to keep: guard *N+kO) (Tartaroō g5020)
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
to grow then in/on/among grace and knowledge the/this/who lord: God me and savior Jesus Christ it/s/he the/this/who glory and now and toward day an age: eternity amen (aiōn g165)
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
and the/this/who life to reveal and to see: see and to testify and to announce you the/this/who life the/this/who eternal who/which to be to/with the/this/who father and to reveal me (aiōnios g166)
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios g166)
and the/this/who world to pass and the/this/who desire it/s/he the/this/who then to do/make: do the/this/who will/desire the/this/who God to stay toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
and this/he/she/it to be the/this/who promise which it/s/he to profess me the/this/who life the/this/who eternal (aiōnios g166)
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
all the/this/who to hate the/this/who brother it/s/he murderer to be and to know that/since: that all murderer no to have/be life eternal in/on/among (it/s/he *NK+o) to stay (aiōnios g166)
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios g166)
and this/he/she/it to be the/this/who testimony that/since: that life eternal to give me the/this/who God and this/he/she/it the/this/who life in/on/among the/this/who son it/s/he to be (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
this/he/she/it to write you (the/this/who to trust (in) toward the/this/who name the/this/who son the/this/who God *K) in order that/to to know that/since: that life to have/be eternal (and in order that/to *K) (the/this/who *no) (to trust (in) *N+kO) toward the/this/who name the/this/who son the/this/who God (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
to know then that/since: that the/this/who son the/this/who God to come/be present and to give me mind in order that/to (to know *NK+o) the/this/who true and to be in/on/among the/this/who true in/on/among the/this/who son it/s/he Jesus Christ this/he/she/it to be the/this/who true God and (the/this/who *k) life eternal (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
through/because of the/this/who truth the/this/who to stay in/on/among me and with/after me to be toward the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
angel and/both the/this/who not to keep: observe the/this/who themself beginning but to leave the/this/who one's own/private dwelling toward judgment great day chain eternal by/under: under darkness to keep: guard (aïdios g126)
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios g126)
as/when Sodom and Gomorrah and the/this/who about it/s/he city the/this/who like way this/he/she/it to fornicate and to go away after flesh other to set before example fire eternal condemnation to undergo (aiōnios g166)
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios g166)
a wave wild sea to foam up the/this/who themself shame star wandering which the/this/who darkness the/this/who darkness toward (the/this/who *k) an age: eternity to keep: guard (aiōn g165)
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn g165)
themself in/on/among love God to keep: observe to wait for/welcome the/this/who mercy the/this/who lord: God me Jesus Christ toward life eternal (aiōnios g166)
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios g166)
alone (wise *K) God savior me (through/because of Jesus Christ the/this/who lord: God me *NO) glory (and *k) majesty power and authority (before all the/this/who an age: eternity *NO) and now and toward all the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
and to do/make: do me (kingdom *N+KO) (and *K) priest the/this/who God and father it/s/he it/s/he the/this/who glory and the/this/who power toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn g165)
and the/this/who to live and to be dead and look! to live to be toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (amen *K) and to have/be the/this/who key the/this/who death and the/this/who hell: Hades (aiōn g165, Hadēs g86)
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn g165, Hadēs g86)
and when(-ever) (to give *NK+o) the/this/who living thing glory and honor and thankfulness the/this/who to sit upon/to/against (the/this/who throne *N+kO) the/this/who to live toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn g165)
to collapse the/this/who twenty (and *k) four elder: Elder before the/this/who to sit upon/to/against the/this/who throne and (to worship *N+kO) the/this/who to live toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity and (to throw: throw *N+kO) the/this/who crown it/s/he before the/this/who throne to say (aiōn g165)
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn g165)
and all creature which (to be *k) in/on/among the/this/who heaven and (upon/to/against the/this/who earth: planet *N+kO) and under the/this/who earth: planet and upon/to/against the/this/who sea (which *k) (to be *ko) and the/this/who in/on/among it/s/he (all *N+kO) to hear to say the/this/who to sit upon/to/against (the/this/who throne *N+kO) and the/this/who lamb the/this/who praise and the/this/who honor and the/this/who glory and the/this/who power toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (amen *O) (aiōn g165)
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn g165)
and to perceive: see and look! horse green and the/this/who to sit above it/s/he name it/s/he the/this/who death and the/this/who hell: Hades (to follow *N+kO) with/after (it/s/he *NK+o) and to give (it/s/he *NK+O) authority upon/to/against the/this/who fourth the/this/who earth: planet to kill in/on/among sword and in/on/among hunger and in/on/among death and by/under: by the/this/who wild animal the/this/who earth: planet (Hadēs g86)
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs g86)
to say amen the/this/who praise and the/this/who glory and the/this/who wisdom and the/this/who thankfulness and the/this/who honor and the/this/who power and the/this/who strength the/this/who God me toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity amen (aiōn g165)
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn g165)
and the/this/who fifth angel to sound a trumpet and to perceive: see star out from the/this/who heaven to collapse toward the/this/who earth: planet and to give it/s/he the/this/who key the/this/who well/abyss the/this/who abyss (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
and to open the/this/who well/abyss the/this/who abyss and to ascend smoke out from the/this/who well/abyss as/when smoke furnace/oven (great *NK+o) and (to darken *N+kO) the/this/who sun and the/this/who air out from the/this/who smoke the/this/who well/abyss (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
(and *k) (to have/be *NK+o) upon/to/against it/s/he king the/this/who angel the/this/who abyss name it/s/he Hebrew Abaddon (and *NK+o) in/on/among the/this/who Greek name to have/be Apollyon (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
and to swear in/on/among the/this/who to live toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity which to create the/this/who heaven and the/this/who in/on/among it/s/he and the/this/who earth: planet and the/this/who in/on/among it/s/he and the/this/who sea and the/this/who in/on/among it/s/he that/since: that time no still to be (aiōn g165)
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn g165)
and when(-ever) to finish the/this/who testimony it/s/he the/this/who wild animal the/this/who to ascend out from the/this/who abyss to do/make: do with/after it/s/he war and to conquer it/s/he and to kill it/s/he (Abyssos g12)
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos g12)
and the/this/who seventh angel to sound a trumpet and to be voice/sound: voice great in/on/among the/this/who heaven (to say *N+kO) (to be *N+KO) (the/this/who *N+kO) (kingdom *N+KO) the/this/who world the/this/who lord: God me and the/this/who Christ it/s/he and to reign toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn g165)
and to perceive: see another angel to fly in/on/among midair to have/be gospel eternal to speak good news (upon/to/against *no) the/this/who (to sit *N+kO) upon/to/against the/this/who earth: planet and upon/to/against all Gentiles and tribe and tongue and a people (aiōnios g166)
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios g166)
and the/this/who smoke the/this/who torment it/s/he toward an age: eternity an age: eternity to ascend and no to have/be rest day and night the/this/who to worship the/this/who wild animal and the/this/who image it/s/he and if one to take the/this/who image/mark the/this/who name it/s/he (aiōn g165)
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn g165)
and one out from the/this/who four living thing to give the/this/who seven angel seven bowl golden be full the/this/who wrath the/this/who God the/this/who to live toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn g165)
the/this/who wild animal which to perceive: see to be and no to be and to ensue to ascend out from the/this/who abyss and toward destruction (to go *N+kO) and (to marvel *N+kO) the/this/who to dwell upon/to/against the/this/who earth: planet which no to write (the/this/who name *N+kO) upon/to/against the/this/who scroll the/this/who life away from beginning world (to see *N+kO) the/this/who wild animal (that/since: that *N+kO) to be and no to be (and *N+kO) (be present *N+KO) (Abyssos g12)
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos g12)
and secondly (to say *NK+o) hallelujah and the/this/who smoke it/s/he to ascend toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn g165)
and to arrest/catch the/this/who wild animal and with/after (it/s/he *N+kO) the/this/who false prophet the/this/who to do/make: do the/this/who sign before it/s/he in/on/among which to lead astray the/this/who to take the/this/who image/mark the/this/who wild animal and the/this/who to worship the/this/who image it/s/he to live to throw: throw the/this/who two toward the/this/who lake the/this/who fire (the/this/who to kindle/burn *N+kO) in/on/among (the/this/who *k) sulfur (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr g3041 g4442)
and to perceive: see angel to come/go down out from the/this/who heaven to have/be the/this/who key the/this/who abyss and chain great upon/to/against the/this/who hand it/s/he (Abyssos g12)
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos g12)
and to throw: throw it/s/he toward the/this/who abyss and to shut (it/s/he *k) and to seal above it/s/he in order that/to not (to lead astray *NK+o) still the/this/who Gentiles until to finish the/this/who thousand year (and *k) with/after this/he/she/it be necessary to loose it/s/he small time (Abyssos g12)
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos g12)
and the/this/who devilish/the Devil the/this/who to lead astray it/s/he to throw: throw toward the/this/who lake the/this/who fire and sulfur where(-ever) (and *no) the/this/who wild animal and the/this/who false prophet and to torture: torture day and night toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
and to give the/this/who sea the/this/who dead the/this/who in/on/among it/s/he and the/this/who death and the/this/who hell: Hades to give the/this/who dead the/this/who in/on/among it/s/he and to judge each according to the/this/who work it/s/he (Hadēs g86)
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs g86)
and the/this/who death and the/this/who hell: Hades to throw: throw toward the/this/who lake the/this/who fire this/he/she/it the/this/who death the/this/who secondly to be (the/this/who lake the/this/who fire *NO) (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
and if one no to find/meet in/on/among (the/this/who book *NK+o) the/this/who life to write to throw: throw toward the/this/who lake the/this/who fire (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr g3041 g4442)
(the/this/who *no) then timid and unbelieving (and sinful *O) and to abhor and murderer and sexual sinner and (sorcerer *N+kO) and idolater and all the/this/who false the/this/who part it/s/he in/on/among the/this/who lake the/this/who to kindle/burn fire and sulfur which to be the/this/who death the/this/who secondly (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
and night no to be (still *N+kO) and no to have/be need (light *no) lamp and (light *NK+o) sun that/since: since lord: God the/this/who God (to illuminate *N+kO) (upon/to/against *no) it/s/he and to reign toward the/this/who an age: eternity the/this/who an age: eternity (aiōn g165)
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn g165)
Questioned verse translations do not contain Aionian Glossary words, but may wrongly imply eternal or Hell
to withhold soul his from Pit: hell and living thing his from to pass in/on/with missile (questioned)
and be gracious him and to say to deliver him from to go down Pit: hell to find ransom (questioned)
to ransom (soul his *QK) from to pass in/on/with Pit: hell (and living thing his *QK) in/on/with light to see: enjoy (questioned)
to/for to return: return soul his from Pit: hell to/for to light in/on/with light [the] alive (questioned)
what? unjust-gain in/on/with blood my in/on/with to go down I to(wards) Pit: hell to give thanks you dust to tell truth: faithful your (questioned)
and to live still to/for perpetuity not to see: see [the] Pit: hell (questioned)
and you(m. s.) God to go down them to/for well Pit: hell human blood and deceit not to divide day their and I to trust in/on/with you (questioned)
[the] to redeem: redeem from Pit: hell life your [the] to crown you kindness and compassion (questioned)
behold to/for peace: well-being bitter to/for me to provoke and you(m. s.) to desire soul: life my from Pit: hell without for to throw after back your all sin my (questioned)
to hasten to march to/for to open and not to die to/for Pit: hell and not to lack food: bread his (questioned)
to/for Pit: hell to go down you and to die death slain: killed in/on/with heart sea (questioned)
to/for shape mountain: mount to go down [the] land: country/planet bar her about/through/for me to/for forever: enduring and to ascend: establish from Pit: hell life my LORD God my (questioned)
this/he/she/it to be flow waterless (and *no) (fog *N+kO) by/under: by storm to drive which the/this/who darkness the/this/who darkness (toward an age: eternity *K) to keep: guard (questioned)

ESC > Aionian Verses: 264, Questioned: 13
CHW > Aionian Verses: 264