< Psalms 133 >

1 [A Song of Ascents. By David.] See how good and how pleasant it is for brothers to live together in unity.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2 It is like the precious oil on the head, that ran down on the beard, even Aaron's beard; that came down on the edge of his robes;
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3 like the dew of Hermon, that comes down on the hills of Zion: for there Jehovah gives the blessing, even life forevermore.
Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.

< Psalms 133 >