< Psalms 100 >

1 A Psalme of Praise. Sing ye loude vnto the Lord, all the earth.
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Serue the Lord with gladnes: come before him with ioyfulnes.
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3 Knowe ye that euen the Lord is God: hee hath made vs, and not we our selues: we are his people, and the sheepe of his pasture.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4 Enter into his gates with prayse, and into his courts with reioycing: prayse him and blesse his Name.
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5 For the Lord is good: his mercy is euerlasting, and his trueth is from generation to generation.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

< Psalms 100 >