< Psalms 136 >

1 Alleluia. Confess to the Lord, for he is good: for his mercy is eternal.
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
2 Confess to the God of gods, for his mercy is eternal.
Yamikani Mulungu wa milungu.
3 Confess to the Lord of lords, for his mercy is eternal.
Yamikani Ambuye wa ambuye,
4 He alone performs great miracles, for his mercy is eternal.
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
5 He made the heavens with understanding, for his mercy is eternal.
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
6 He established the earth above the waters, for his mercy is eternal.
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
7 He made the great lights, for his mercy is eternal:
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
8 the sun to rule the day, for his mercy is eternal:
Dzuwa lilamulire usana,
9 the moon and the stars to rule the night, for his mercy is eternal.
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 He struck Egypt along with their first-born, for his mercy is eternal.
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 He led Israel away from their midst, for his mercy is eternal:
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 with a powerful hand and an outstretched arm, for his mercy is eternal.
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 He divided the Red Sea into separate parts, for his mercy is eternal.
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 And he led out Israel through the middle of it, for his mercy is eternal.
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 And he shook off Pharaoh and his army in the Red Sea, for his mercy is eternal.
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 He led his people through the desert, for his mercy is eternal.
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 He has struck great kings, for his mercy is eternal.
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 And he has slaughtered strong kings, for his mercy is eternal:
Napha mafumu amphamvu,
19 Sihon, king of the Amorites, for his mercy is eternal:
Siloni mfumu ya Aamori,
20 and Og, king of Bashan, for his mercy is eternal.
Ogi mfumu ya Basani,
21 And he granted their land as an inheritance, for his mercy is eternal:
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 as an inheritance for his servant Israel, for his mercy is eternal.
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 For he was mindful of us in our humiliation, for his mercy is eternal.
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 And he redeemed us from our enemies, for his mercy is eternal.
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 He gives food to all flesh, for his mercy is eternal.
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 Confess to the God of heaven, for his mercy is eternal. Confess to the Lord of lords, for his mercy is eternal.
Yamikani Mulungu wakumwamba,

< Psalms 136 >