< Genesis 5 >

1 This is the book of the lineage of Adam. In the day that God created man, he made him to the likeness of God.
Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi: Pamene Mulungu analenga munthu, anamulenga mʼchifaniziro cha Mulungu.
2 He created them, male and female; and he blessed them. And he called their name Adam, in the day when they were created.
Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”
3 Then Adam lived for one hundred and thirty years. And then he conceived a son in his own image and likeness, and he called his name Seth.
Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti.
4 And after he conceived Seth, the days of Adam that passed were eight hundred years. And he conceived sons and daughters.
Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
5 And all the time that passed while Adam lived was nine hundred and thirty years, and then he died.
Zaka zonse za Adamu zinali 930 ndipo anamwalira.
6 Seth likewise lived for one hundred and five years, and then he conceived Enos.
Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi.
7 And after he conceived Enos, Seth lived for eight hundred and seven years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
8 And all the days of Seth that passed were nine hundred and twelve years, and then he died.
Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.
9 In truth, Enos lived ninety years, and then he conceived Cainan.
Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.
10 After his birth, he lived eight hundred and fifteen years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
11 And all the days of Enos that passed were nine hundred and five years, and then he died.
Zaka zonse za Enosi pamodzi zinali 905 ndipo anamwalira.
12 Likewise, Cainan lived seventy years, and then he conceived Mahalalel.
Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.
13 And after he conceived Mahalalel, Cainan lived for eight hundred and forty years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Mahalaleli, Kenani anakhala ndi moyo zaka zina 840 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
14 And all the days of Cainan that passed were nine hundred and ten years, and then he died.
Zaka zonse za Kenani zinali 910, ndipo anamwalira.
15 And Mahalalel lived sixty-five years, and then he conceived Jared.
Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi.
16 And after he conceived Jared, Mahalalel lived for eight hundred and thirty years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Yaredi, Mahalaleli anakhala ndi moyo zaka zina 830 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
17 And all the days of Mahalalel that passed were eight hundred and ninety-five years, and then he died.
Zaka zonse za Mahalaleli zinali 895 ndipo anamwalira.
18 And Jared lived for one hundred and sixty-two years, and then he conceived Enoch.
Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki.
19 And after he conceived Enoch, Jared lived for eight hundred years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Enoki, Yaredi anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
20 And all the days of Jared that passed were nine hundred and sixty-two years, and then he died.
Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.
21 Now Enoch lived for sixty-five years, and then he conceived Methuselah.
Pamene Enoki anali ndi zaka 65, anabereka Metusela.
22 And Enoch walked with God. And after he conceived Methuselah, he lived for three hundred years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
23 And all the days of Enoch that passed were three hundred and sixty-five years.
Zaka zonse za Enoki zinali 365.
24 And he walked with God, and then he was seen no more, because God took him.
Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.
25 Likewise, Methuselah lived for one hundred and eighty-seven years, and then he conceived Lamech.
Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki.
26 And after he conceived Lamech, Methuselah lived for seven hundred and eighty-two years, and he conceived sons and daughters.
Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
27 And all the days of Methuselah that passed were nine hundred and sixty-nine years, and then he died.
Zaka zonse za Metusela zinali 969, ndipo anamwalira.
28 Then Lamech lived for one hundred and eighty-two years, and he conceived a son.
Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.
29 And he called his name Noah, saying, “This one will console us from the works and hardships of our hands, in the land that the Lord has cursed.”
Ndipo anamutcha Nowa ndipo anati, “Iyeyu adzatipumulitsa ku ntchito zathu zolemetsazi, zolima nthaka imene Yehova anayitemberera.”
30 And after he conceived Noah, Lamech lived for five hundred and ninety-five years, and he conceived sons and daughters.
Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
31 And all the days of Lamech that passed were seven hundred and seventy-seven years, and then he died.
Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.
32 In truth, when Noah was five hundred years old, he conceived Shem, Ham, and Japheth.
Pamene Nowa anali ndi zaka 500, anabereka Semu, Hamu ndi Yafeti.

< Genesis 5 >