< Psalms 136 >

1 Give thanks to the LORD, for he is good, for his loving kindness endures forever.
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
2 Give thanks to the God of gods, for his loving kindness endures forever.
Yamikani Mulungu wa milungu.
3 Give thanks to the Lord of lords, for his loving kindness endures forever;
Yamikani Ambuye wa ambuye,
4 to him who alone does great wonders, for his loving kindness endures forever;
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
5 to him who by understanding made the heavens, for his loving kindness endures forever;
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
6 to him who spread out the earth above the waters, for his loving kindness endures forever;
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
7 to him who made the great lights, for his loving kindness endures forever;
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
8 the sun to rule by day, for his loving kindness endures forever;
Dzuwa lilamulire usana,
9 the moon and stars to rule by night, for his loving kindness endures forever;
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 to him who struck down the Egyptian firstborn, for his loving kindness endures forever;
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 and brought out Israel from among them, for his loving kindness endures forever;
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 with a strong hand, and with an outstretched arm, for his loving kindness endures forever;
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 to him who divided the Red Sea apart, for his loving kindness endures forever;
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 and made Israel to pass through the middle of it, for his loving kindness endures forever;
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 but overthrew Pharaoh and his army in the Red Sea, for his loving kindness endures forever;
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 to him who led his people through the wilderness, for his loving kindness endures forever;
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 to him who struck great kings, for his loving kindness endures forever;
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 and killed mighty kings, for his loving kindness endures forever;
Napha mafumu amphamvu,
19 Sihon king of the Amorites, for his loving kindness endures forever;
Siloni mfumu ya Aamori,
20 Og king of Bashan, for his loving kindness endures forever;
Ogi mfumu ya Basani,
21 and gave their land as an inheritance, for his loving kindness endures forever;
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 even a heritage to Israel his servant, for his loving kindness endures forever;
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 who remembered us in our low estate, for his loving kindness endures forever;
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 and has delivered us from our adversaries, for his loving kindness endures forever;
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 who gives food to every creature, for his loving kindness endures forever.
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 Oh give thanks to the God of heaven, for his loving kindness endures forever.
Yamikani Mulungu wakumwamba,

< Psalms 136 >