< Job 25 >

1 Nu nam Bildad van Sjóeach het woord, en sprak:
Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 Hem is de macht en de schrik, Hem, die vrede gebiedt in zijn hoge hemel!
“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
3 Zijn soms zijn legioenen te tellen, Tegen wien staan zijn troepen niet op!
Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
4 Hoe kan dan een mens tegen God in zijn recht zijn, Of rein, die uit een vrouw is geboren?
Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
5 Zie, zelfs de maan is niet helder, De sterren zijn niet rein in zijn ogen:
Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
6 Hoeveel minder een mens, een aas, Een mensenkind, een worm!
nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”

< Job 25 >