< Salme 131 >

1 (Sang til Festrejserne. Af David.) Herre, mit hjerte er ikke hovmodigt, mine øjne er ikke stolte, jeg sysler ikke med store Ting, med Ting, der er mig for høje.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 Nej, jeg har lullet og tysset min Sjæl; som afvant Barn hos sin Moder har min Sjæl det hos HERREN.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Israel, bi på HERREN fra nu og til evig Tid!
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Salme 131 >