< Salme 11 >

1 (Til sangmesteren. Af David.) Jeg tager min Tilflugt til HERREN! Hvor kan I sige til min Sjæl: "Fly som en Fugl til Bjergene!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mwa Yehova ine ndimathawiramo. Nanga mungathe bwanji kunena kwa ine kuti, “Thawira ku phiri lako ngati mbalame.
2 Thi se, de gudløse spænder Buen, lægger Pilen til Rette på Strengen for i Mørke at ramme de oprigtige af Hjertet.
Pakuti taona oyipa akunga mauta awo; ayika bwino mivi yawo pa zingwe za uta, pobisala pawo kuti alase olungama mtima.
3 Når selv Grundpillerne styrter, hvad gør den retfærdige da?"
Tsono ngati maziko awonongeka, olungama angachite chiyani?”
4 HERREN er i sin hellige Hal, i Himlen er HERRENs Trone; på Jorderig skuer hans Øjne ned, hans Blik ransager Menneskens Børn;
Yehova ali mʼNyumba yake yoyera; Yehova ali pa mpando wake waufumu kumwamba. Iye amayangʼanitsitsa ana a anthu; maso ake amawayesa.
5 retfærdige og gudløse ransager HERREN; dem, der elsker Uret, hader hans Sjæl;
Yehova amayesa olungama, koma moyo wake umadana ndi oyipa, amene amakonda zachiwawa.
6 over gudløse sender han Regn af Gløder og Svovl, et Stormvejr er deres tilmålte Bæger.
Iye adzakhuthulira pa oyipa makala amoto ndi sulufule woyaka; mphepo yotentha idzakhala yowayenera.
7 Thi retfærdig er HERREN, han elsker at øve Retfærd, de oprigtige skuer hans Åsyn!
Pakuti Yehova ndi wolungama, Iye amakonda chilungamo; ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake.

< Salme 11 >