< Psalmi 82 >

1 Psalam. Asafov. Bog ustaje u skupštini “bogova”, usred “bogova” sud održava.
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
2 “Dokle ćete sudit' krivo, ić' na ruku bezbožnima?
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
3 Štitite slaba i sirotu, vratite pravicu jadniku i siromahu!
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
4 Izbavite potlačenog i ubogog: istrgnite ga iz ruku bezbožnih!”
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
5 Ne shvaćaju nit' razumiju, po mraku hodaju: poljuljani su svi temelji zemlje.
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
6 Rekoh doduše: “Vi ste bogovi i svi ste sinovi Višnjega!
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
7 Ali ćete k'o svi ljudi umrijeti, past ćete kao svatko od velikih!”
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
8 Ustani, Bože, i sudi zemlju, jer si s pravom gospodar svih naroda.
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.

< Psalmi 82 >