< Tingtoeng 71 >

1 BOEIPA nang dongah ka ying tih, kumhal ah yah m'poh sak boeh.
Mwa Inu Yehova ine ndathawiramo; musalole kuti ndichititsidwe manyazi.
2 Na duengnah neh, kai na huul tih nan hlawt. Te dongah na hna te kai taengla han hooi lamtah, kai n'khang lah.
Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu, mutchere khutu lanu ndi kundipulumutsa.
3 Caeh taitu vaengkah ham, kai taengah lungpang khuirhung la ha om lah. Namah te ka thaelpang neh ka rhalvong la na om dongah, kai khang ham khaw na uen.
Mukhale thanthwe langa lothawirapo, kumene ine nditha kupita nthawi zonse; lamulani kuti ndipulumuke, pakuti Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa.
4 Ka Pathen aw, halang kut lamloh, aka phayoe tih aka muen kah kutpha lamloh, kai n'hlawt lah.
Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa, kuchoka mʼdzanja la oyipa ndi anthu ankhanza.
5 Ka Boeipa Yahovah namah tah, ka ngaiuepnah neh, ka camoe lamkah ka pangtungnah ni.
Pakuti Inu mwakhala chiyembekezo changa, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, chilimbikitso changa kuyambira ndili mwana.
6 Bungko khui lamkah nang dongah ka hangdang coeng. Namah loh a nu ko khui lamkah kai nan poh. Namah te kai kah koehnah la na om yoeyah.
Kuyambira pamene ndinabadwa, ndakhala ndikudalira Inu; Inu munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga, ndipo ndidzakupembedzani nthawi zonse.
7 Hlang tom taengah mikdairhueng bangla ka om cakhaw namah te ka hlipyingnah sarhi la na om.
Ine ndakhala chinthu chodabwitsa kwa anthu ambiri koma Inu ndinu wonditchinjiriza wamphamvu.
8 Namah kah boeimangnah rhangneh namah koehnah te hnin takuem ka ka ah baetawt.
Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse.
9 Ka patong tue vaengah kai m'voei boeh. Ka thadueng a bawt vaengah kai nan hnoo mahpawh.
Musanditaye pamene ndakalamba; musandisiye pamene mphamvu zanga zatha.
10 Ka thunkha rhoek loh kai taengah cal uh tih ka hinglu dawn ham tun caai uh.
Pakuti adani anga ayankhula motsutsana nane; iwo amene amadikira kuti andiphe amapangana pamodzi.
11 “Anih he Pathen loh a hnoo coeng dongah hloem uh sih lamtah tu uh sih. Anih aka huul ham khaw hlang a om moenih,” a ti uh.
Iwo amati, “Mulungu wamusiya; mutsatireni ndi kumugwira, pakuti palibe amene adzamupulumutse.”
12 Pathen aw kai taeng lamkah lakhla tak boeh. Kai bomkung ham ka Pathen nang ha tawn rhoe ha tawn uh laeh.
Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu, bwerani msanga, Inu Mulungu wanga; thandizeni.
13 Ka hinglu aka khingkhoek rhoek te yahpok uh saeh lamtah hmata uh saeh. Kai kah yoethae aka hue rhoe te kokhahnah neh mingthae loh thing uh saeh.
Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi, iwo amene akufuna kundipweteka avale chitonzo ndi manyazi.
14 Tedae kai loh ka ngaiuep yoeyah vetih namah koehnah te boeih ka khoep ni.
Koma ine ndidzakhala ndi chiyembekezo mwa Inu nthawi zonse, ndidzakutamandani mowirikizawirikiza.
15 Nan khangnah te taenah ham ka ming pawt cakhaw na duengnah te ka ka loh hnin takuem a tae bitni.
Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu, za chipulumutso chanu tsiku lonse, ngakhale sindikudziwa muyeso wake.
16 Ka Boeipa Yahovah kah thayung thamal khuila ka lo vetih, namah bueng dongah ni na duengnah ka thoelh eh.
Ndidzabwera ndi kulengeza za machitidwe amphamvu zanu Inu Ambuye Wamphamvuzonse. Ndidzalengeza chilungamo chanu, chanu chokha.
17 Pathen aw, ka camoe lamkah kai nan cang puei dongah tahae duela namah kah khobaerhambae te ka doek.
Kuyambira ubwana wanga, Inu Mulungu mwakhala mukundiphunzitsa, ndipo mpaka lero ine ndikulengeza za ntchito zanu zodabwitsa
18 Pathen aw, thawnpuei taengah na bantha, hmailong kah aka lo ham boeih taengah na thayung thamal ka doek hlanhil tah patong sampok la ka om cakhaw kai nan hnoo mahpawh.
Ngakhale pamene ndakalamba ndipo imvi zili mbuu musanditaye Inu Mulungu, mpaka nditalengeza mphamvu zanu kwa mibado yonse yakutsogolo.
19 Tedae Pathen na duengnah loh a sang duela a puet. Pathen loh duelhduelh na saii te, namah bangla ulae aka om?
Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba. Ndani wofanana nanu Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu?
20 Kai he citcai neh yoethaenah muep nan hmuh khaw nan hmuh sak dae koep nan hing khaw nan hing sak vetih diklai laedil lamkah koep nan lat bal ni.
Ngakhale mwandionetsa mavuto ambiri owawa, mudzabwezeretsanso moyo wanga; kuchokera kunsi kwa dziko lapansi, mudzandiukitsanso.
21 Ka lennah nan pueh vetih kai nan hloep bal ni.
Inu mudzachulukitsa ulemu wanga ndi kunditonthozanso.
22 Kai khaw ka Pathen namah kah uepomnah te thangpa toembael neh kan uem vetih Israel kah a cim namah te rhotoeng neh ka tingtoeng ni.
Ndidzakutamandani ndi zeze chifukwa cha kukhulupirika kwanu Mulungu, ndidzayimba matamando kwa Inu ndi pangwe, Inu Woyera wa Israeli.
23 Ka hinglu he na lat coeng dongah nang te kan tingtoeng vaengah ka hmui ka lai neh ka tamhoe ni.
Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe pamene ndidzayimba matamando kwa Inu amene mwandiwombola.
24 Kai kah yoethae aka hue rhoek loh yah a poh uh tih a hmai a tal uh coeng dongah ka lai long khaw hnin takuem nang kah duengnah te a thuep ni.
Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo tsiku lonse, pakuti iwo amene amafuna kundipweteka achititsidwa manyazi ndi kusokonezedwa.

< Tingtoeng 71 >