< Luka 8 >

1 Te a poeng phoeiah amah loh khopuei boeih neh vangca patoeng a hil. Te vaengah Pathen ram te a hoe tih a olthangthen a thui. A hnukbang hlainit loh anih te a pueiuh.
Zitatha izi, Yesu anayendayenda kuchoka mzinda wina kupita wina ndiponso mudzi wina kupita wina, akulalikira Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu. Ophunzira ake khumi ndi awiri aja anali naye,
2 Mueihla thae, vawtthoeknah lamkah aka hoeih tangtae la aka om huta hlangvang rhoek, a khui lamkah rhaithae parhih loh a nong tak Magdala la a khue Mary,
komanso akazi ena amene anachiritsidwa ku mizimu yoyipa ndi matenda: Mariya, wotchedwa Magadalena, amene mwa iye munatuluka ziwanda zisanu ndi ziwiri;
3 Herod buhtaem Chuza yuu Joanna, Susanna neh a tloe rhoek khaw muep lo uh tih amih loh Jesuh khaw a hnukbang rhoek te khaw a khuehtawn neh a bongyong uh.
Yohana mkazi wa Kuza, woyangʼanira mʼnyumba ya Herode; Suzana; ndi ena ambiri analinso. Akazi awa ankawathandiza ndi chuma chawo.
4 Khopuei takuem kah hlangping te muep capit uh tih a taengla ha pawk uh.
Anthu ambiri ankasonkhana, ndipo pamene anthu ankabwera kwa Yesu kuchokera ku midzi, Iye anawawuza fanizo ili,
5 Te vaengah nuettahnah neh, “Cangti aka tuh tah a cangtii tuh hamla cet. Tedae a tuh vaengah a ngen tah long taengah tla. Te dongah a taelh uh tih vaan kah vaa loh a kueh.
“Mlimi anapita kukafesa mbewu zake. Akufesa mbewuzo, zina zinagwa mʼmbali mwa njira; zinapondedwa, ndipo mbalame zamlengalenga zinadya.
6 A tloe rhoek tah lungpang soah tla dae, laiyuem a om pawt dongah a poe neh pahoi koh.
Zina zinagwa pa thanthwe, ndipo pamene zinamera, zinafota chifukwa panalibe chinyezi.
7 A tloe rhoek tah hling puem ah tla tih, a rhoeng vaengah hling loh a thing.
Mbewu zina zinagwera pakati pa minga, zinakulira pamodzi ndi mingazo ndipo zinalepheretsa mmerawo kukula.
8 A tloe te lai then dongah tla tih, a poe vaengah a vuei yakhat lam khaw thoeng,” a ti. Te phoeiah te, “Yaak nah hna aka khueh loh ya saeh,” a ti nah tih a doek.
Mbewu zina zinagwera pa nthaka yabwino. Zinamera ndipo zinabala mowirikiza 100 kuposa zimene zinafesedwa zija.” Atanena izi, anafuwula kuti, “Amene ali ndi makutu, amve.”
9 Te dongah nuettahnah loh metla a om te a hnukbang rhoek loh amah a dawt uh.
Ophunzira ake anamufunsa tanthauzo lake la fanizolo.
10 Te dongah, “Pathen ram kah olhuep he ming hamla nangmih m'paek coeng. Te phoeiah a hmuh uh vaengah a hmat uh pawt ham, a yaak uh dae a hmuhming uh pawt ham ni nuettahnah neh ka hlihloeh sak.
Iye anati, “Kudziwa zinsinsi za ufumu wa Mulungu kwapatsidwa kwa inu, koma kwa ena ndimawayankhula mʼmafanizo kuti, “ngakhale akuona, asapenye; ngakhale akumva, asazindikire.”
11 Nuettahnah tah he tlam ni a om. Cangtii tah Pathen kah olka ni.
“Tanthauzo la fanizoli ndi ili: Mbewu ndi mawu a Mulungu.
12 A yaak uh vaengah amih a khang ham te tangnah boel saeh tila, rhaithae te ha pawk tih a thinko kah olka a rhawt pah rhoek tah, long taengkah rhoek la om uh.
Mbewu za mʼmbali mwa njira ndi anthu amene amamva mawu, ndipo kenaka mdierekezi amabwera ndi kuchotsa mawuwo mʼmitima mwawo kuti asakhulupirire ndi kupulumutsidwa.
13 Lungpang sokah rhoek te tah olka te a yaak uh vaengah omngaihnah neh a doeuh. Tedae te rhoek te a yung om pawh. Amih loh a tue kolkalh ham a tangnah uh tih noemcainah tue vaengah tah nong uh.
Mbewu za pa thanthwe ndi anthu amene amalandira mawu mwachimwemwe pamene akumva, koma mawuwo sazika mizu. Iwo amakhulupirira kwa kanthawi, koma pa nthawi ya mayesero, amagwa.
14 Hling puem kah aka tla rhoek, amih khaw aka ya tangtae rhoek ni. Tedae a pongpa vaengah mawntangnah, khuehtawn neh khosaknah omthenbawn loh a thing tih tak pawh.
Mbewu zimene zinagwa pakati pa minga zikuyimira anthu amene amamva mawu, koma akamayenda mʼnjira zawo amatsamwitsidwa ndi zodandaulitsa za moyo uno, chuma ndi zosangalatsa, ndipo iwo samakhwima.
15 Lai then dongkah rhoek, amih rhoek tah thinko then neh a then la aka om rhoek ni. Te dongah ol a yaak uh te a dueh uh tih uehnah neh thaihtak uh.
Koma mbewu za pa nthaka yabwino zikuyimira anthu amene ali ndi mtima woona ndi wabwino, amene amamva mawu nawasunga, ndipo amalimbikira mpaka amabala zipatso.
16 Hmaiim a tok te hnopai neh aka dah, thingkong hmuiah aka det he a om moenih. Tedae aka kun rhoek te vangnah hmuh sak ham hmaitung soah ni a khueh.
“Palibe amayatsa nyale ndi kuyibisa mu mtsuko kapena kuyika pansi pa bedi. Koma mʼmalo mwake, amayika pa choyikapo chake, kuti anthu olowamo aone kuwala.
17 A huephael la aka om te mingpha la a om mueh moenih. A huep te khaw mingpha mueh pawt tih mingpha la a pawk mueh moenih.
Pakuti palibe kanthu kobisika kamene sikadzawululika, ndipo palibe kanthu kophimbika kamene sikadzadziwika kapena kuonetsedwa poyera.
18 Te dongah metla na yaak uh khaw hmuminguh. Aka khueh te tah a a taengla a paek ni. Tedae aka khueh pawt te tah a taengah a khueh la a ngai te khaw a loh pah ni,” a ti nah.
Choncho ganizirani mozama. Iye amene ali nazo adzapatsidwa zambiri, iye amene alibe, ngakhale chimene akuganiza kuti ali nacho adzalandidwa.”
19 Jesuh te a manu neh a mana rhoek loh a paan. Tedae hlangping dongah anih te hum uh thai pawh.
Tsopano amayi ndi abale a Yesu anabwera kudzamuona Iye, koma analephera kuti afike pafupi ndi Iye chifukwa cha gulu la anthu.
20 Te dongah amah te, “Na nu neh na mana rhoek loh nang hmuh ham la a ngaih uh tih poeng ah pai uh,” tila a puen pah.
Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunja, akufuna kukuonani.”
21 Tedae Jesuh loh amih te a doo tih, “Pathen kah olka a yaak tih aka saii rhoek tah ka manu neh ka manuca la om uh,” a ti nah.
Yesu anayankha kuti, “Amayi ndi abale anga ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kumachita zimene mawuwo akunena.”
22 Hnin at vaengah Jesuh tah a hnukbang neh lawng khuila kun. Te phoeiah amih te, “Tuili kah rhalvangan la kat uh sih,” a ti nah tih kat uh.
Tsiku lina Yesu anati kwa ophunzira ake, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina la nyanja.” Ndipo analowa mʼbwato nanyamuka.
23 A hlaikan uh vaengah Jesuh tah vik ip. Te vaengah hlipuei khohli loh tuili la ha pawk tih dalh a muelh coeng dongah khopo uh.
Akuwoloka, Iye anagona tulo. Namondwe wamkulu anayamba pa nyanja, ndipo bwatolo linayamba kudzaza ndi madzi ndipo anali pa chiopsezo chachikulu.
24 Te dongah Jesuh te a paan uh tih a haeng uh. Te phoeiah, “Boeipa, Boeipa, m'poci uh coeng he,” a ti nauh. Tedae a haeng vaengah khohli neh tui dongkah tuiphu te khaw a toel hatah khohli khaw paa tih suepduem la koep om.
Ophunzira anapita ndi kukamudzutsa Iye, nati, “Ambuye, Ambuye, ife tikumira!” Anadzuka ndipo anadzudzula mphepo ndi madzi owindukawo. Namondwe anasiya, ndipo panali bata.
25 Te phoeiah amih te, “Nangmih kah tangnah te ta?” a ti nah. Tedae a rhih uh tih a ngai a hmang uh dongah amamih te, “Unim he, khohli neh tui khaw a voek tih a ngai pah he,” a ti uh.
Iye anafunsa ophunzira ake kuti, “Chikhulupiriro chanu chili kuti?” Koma pogwidwa ndi mantha ndi kudabwa anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndi ndani? Iye alamulira ngakhale mphepo ndi madzi, ndipo zimumvera Iye.”
26 Te phoeiah Galilee imdan ah aka om Gerasenes kho te a pha uh.
Iwo anawolokera ku chigawo cha Gerasa chimene chili tsidya lina la nyanja kuchokera ku Galileya.
27 Lan so a pha vaengah khopuei lamkah rhaithae aka khueh hlang pakhat loh a doe. Kum te yet ah himbai bai voel pawh, im ah pawt tih phuel ah naeh.
Yesu ataponda pa mtunda, anakumana ndi munthu wogwidwa ndi ziwanda wochokera mu mzindawo. Kwa nthawi yayitali munthuyu sanavale zovala kapena kukhala mʼnyumba, koma amakhala ku manda.
28 Jesuh te a hmuh vaengah pang tih a bakop thil. Te phoeiah ol ue la, “Kai taeng neh nang taengah balae aka om?, Khohni Pathen capa Jesuh aw. Kai nan phaep pawt ham ni nang kan hloep,” a ti nah.
Iye ataona Yesu, anakuwa nagwa pa mapazi ake akufuwula kwambiri kuti, “Mukufuna chiyani ndi ine, Yesu Mwana wa Mulungu Wammwambamwamba? Ndikupemphani Inu, musandizunze ine!”
29 Te dongah hlang khui lamkah a coe hamla rhalawt mueihla te a toel. Te vaengah anih a paco te a tue khaw yet coeng. Thirhui neh a pael tih hloong nen khaw a khoh uh coeng. Tedae rhaithae loh khosoek la a vai vaengah tah hloong te khaw a dueng.
Pakuti Yesu analamula mzimu woyipawo kuti utuluke mwa munthuyo. Kawirikawiri umamugwira iye, ndipo ngakhale anali womangidwa ndi unyolo dzanja ndi mwendo ndi kuti ankamuyangʼanira, koma amadula maunyolo akewo ndipo ziwanda zimamutengera kumalo a yekha.
30 Te phoeiah anih te Jesuh loh, “Na ming ulae? tila a dawt. Anih te rhaithae a yet loh a kun thil dongah, “caempuei caempa,” a ti nah.
Yesu anamufunsa kuti, “Dzina lako ndani?” Iye anayankha kuti, “Legiyo,” chifukwa ziwanda zambiri zinalowa mwa iye.
31 Te phoeiah amih te tangrhom dung khuiah cungpung saeh tila olpaek pawt ham Jesuh te a hloep uh. (Abyssos g12)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
32 Te vaengah tlang ah aka luem ok hui te muep tapkhoeh om. Te dongah amih te ok khuila kun sak ham a bih uh tih a kun sak.
Gulu lalikulu la nkhumba limadya pamenepo mʼmbali mwa phiri. Ziwandazo zinamupempha Yesu kuti azilole kuti zikalowe mu nkhumbazo ndipo Iye anazilola.
33 Te daengah rhaithae rhoek tah hlang lamloh cet uh tih ok khuila kun uh. Tedae ok hui tah laengpoeng ah tuili khuila cu tih buek uh.
Ziwanda zija zitatuluka mwa munthuyo, zinakalowa mwa nkhumbazo, ndipo gulu lonselo linathamangira ku mtsetse ndi kukalowa mʼnyanja ndi kumira.
34 Aka thoeng hno te ok vuelh rhoek loh a hmuh uh vaengah rhaelrham uh tih khopuei neh lohma lam khaw puen uh.
Oweta nkhumbazo ataona zimene zinachitikazo, anathamanga ndi kukanena izi mu mzinda ndi ku madera a ku midzi.
35 Te dongah aka om hno te sawt hamla cet uh tih Jesuh te a paan uh. Te vaengah a khui lamkah rhaithae rhoek loh a nong tak hlang khaw ana yol uh tih Jesuh kho kungah samthing la a ngol te a hmuh uh hatah a rhih uh.
Ndipo anthu anapita kukaona zimene zinachitika. Atafika kwa Yesu, anapeza munthu amene anatulutsidwa ziwanda uja atakhala pa mapazi a Yesu, atavala ndipo ali ndi nzeru zake; ndipo iwo anachita mantha.
36 Te dongah rhaithae aka kaem loh a khang te aka hmuh rhoek loh amih taengah patoeng puen uh.
Amene anaona izi anawuza anthu mmene munthu wogwidwa ndi ziwandayo anachiritsidwira.
37 Tedae rhihnah loh mat a nan uh dongah Gerasenes pingpang kah rhaengpuei boeih loh Jesuh te amih taeng lamkah nong sak ham la a hloep uh. Jesuh khaw lawng khuila kun tih mael.
Kenaka anthu onse a ku chigawo cha Gerasa anamupempha Yesu kuti achoke kwa iwo, chifukwa anadzazidwa ndi mantha. Choncho Iye analowa mʼbwato nachoka.
38 A khui lamkah rhaithae loh a nong tak hlang long khaw Jesuh neh amah taengah om hamla a bih.
Munthu amene anatulutsidwa ziwanda uja, anapempha Yesu kuti apite nawo, koma Yesu anamubweza nati,
39 Tedae anih te a tueih tih, “Namah im la bal lamtah, Pathen loh nang ham a saii te thui pah,” a ti nah. Te dongah kho tom la cet tih Jesuh loh anih ham a saii te a hoe.
“Bwerera kwanu kafotokoze zimene Mulungu wakuchitira.” Ndipo munthuyo anachoka ndi kukanena ku mzinda wonsewo zimene Yesu anamuchitira iye.
40 Jesuh aka lamso la boeih a om uh dongah a mael vaengah anih te hlangping loh a doe.
Yesu atabwerera, gulu lalikulu la anthu linamulandira, chifukwa onse ankamuyembekezera.
41 Te vaengah Jairus aka ming nah hlang pakhat te pakcak ha pawk. Anih tah tunim kah boei la om dae, Jesuh kho taengah bakop tih a im ah pah sak ham a cael.
Nthawi yomweyo munthu wotchedwa Yairo, woweruza wa mu sunagoge, anabwera ndi kugwa pa mapazi a Yesu, namupempha Iye kuti apite ku nyumba kwake,
42 A canu khueh duen, kum hlainit tluk te duek. Tedae a caeh vaegah Jesuh te hlangping loh a thing.
chifukwa mwana wake yekhayo wamkazi, kamtsikana ka zaka khumi ndi ziwiri, kanali pafupi kufa. Pamene Yesu ankapita gulu la anthu linkamupanikiza.
43 Te phoeiah kum hlainit ah thii buk aka khueh huta om. Anih loh a khosaknah te siboei taengah boeih a hnonah coeng dae coeng thai pawt tih hoeih pawh.
Ndipo pomwepo panali mayi wina amene ankataya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri, koma panalibe wina akanamuchiritsa.
44 A hnuk lamloh a paan tih a himbai dongkah salaw te a taek pah. Te dongah a thii buk te dup a ngol pah.
Iye anafika kumbuyo kwake ndi kukhudza mothera mwa chovala chake, ndipo nthawi yomweyo magazi ake analeka kutuluka.
45 Tedae Jesuh loh, “Ulae kai aka taek te,” a ti nah. Boeih basa uh tih Peter loh, “Boeipa, hlangping loh nang te ng'et tih n'nen te ta,” a ti nah.
Yesu anafunsa kuti, “Wandikhudza ndani?” Onse atakana, Petro anati, “Anthu akukupanikizani ndi kukukankhani.”
46 Te vaengah Jesuh loh, “Khat khat loh kai n'taek, kai lamkah ka thaomnah a caeh te ka ming,” a ti nah.
Koma Yesu anati, “Wina wandikhudza; ndikudziwa chifukwa mphamvu yachoka mwa Ine.”
47 A phah tloel te huta loh a hmuh vaengah a birhih doela a paan tih a taengah a bakuep pah. Anih a taek vaengah a paelnaehnah te khaw, metla a hoeih pahoi te khaw pilnam boeih taengah puen.
Ndipo mayiyo podziwa kuti sanathe kuchoka wosadziwika, anabwera akunjenjemera ndipo anagwa pa mapazi a Yesu. Pamaso pa anthu onse, anafotokoza chifukwa chimene anamukhudzira Iye ndi mmene iye anachiritsidwira nthawi yomweyo.
48 Te dongah anih te, “Ka canu, na tangnah loh namah ng'khang coeng, ngaimong la cet laeh,” a ti nah.
Kenaka anati kwa iye, “Mwana wamkazi, chikhulupiriro chako chakuchiritsa. Pita mu mtendere.”
49 A thui pueng ah tamtaeng taeng lamkah hlang pakhat ha pawk tih, “Na canu duek coeng, saya te toehoeih boeh,” a ti nah.
Pamene Yesu ankayankhulabe, munthu wina anabwera kuchokera ku nyumba ya Yairo, woweruza wa ku sunagoge uja. Iye anati, “Mwana wanu wa mkazi wamwalira, musawavutitsenso Aphunzitsiwa.”
50 Jesuh loh a yaak vaengah, “Rhih boeh, dawk tangnah lamtah daem bitni,” a ti nah.
Atamva zimenezi, Yesu anati kwa Yairo, “Usachite mantha, ingokhulupirira basi ndipo adzachiritsidwa.”
51 A pha vaengah Peter, Johan neh James, camoe kah manu a napa pawt atah pakhat khaw amah taengah im khuila kun sak pawh.
Iye atafika ku nyumba ya Yairo, sanalole wina aliyense kulowa kupatula Petro, Yohane, ndi Yakobo ndi abambo ndi amayi a mwanayo.
52 Te vaengah boeih rhap uh tih camoe te a rhaengsae uh. Tedae Jesuh loh, “Rhap uh boeh, a duek moenih, aka ip ni he,” a ti nah.
Pa nthawiyi nʼkuti anthu onse akubuma ndi kumulirira iye. Yesu anati, “Lekani kulira, sanafe koma wagona tulo.”
53 Tedae a duek te a ming uh dongah Jesuh te a nueih thiluh.
Iwo anamuseka podziwa kuti anali atamwalira.
54 Tedae Jesuh loh a kut a tuuk pah phoeiah a khue tih, “Camoe thoo laeh,” a ti nah.
Koma Iye anamugwira dzanja lake ndipo anati, “Mwana wanga, dzuka!”
55 Te dongah a mueihla ha mael tih pahoi thoo. Te phoeiah anih te a caak a paek ham a uen.
Mzimu wake unabwerera, ndipo nthawi yomweyo anayimirira. Kenaka Yesu anawawuza kuti amupatse chakudya.
56 Te vaengah a manu napa tah limlum rhoi. Tedae aka om hno te thui pawt ham amih te a uen.
Makolo ake anadabwa, koma Iye anawalamulira kuti asawuze wina aliyense zimene zinachitikazo.

< Luka 8 >