< Haggai 2 >

1 Hla rhih, hnin kul hnin khat dongkah BOEIPA ol he tonghma Haggai kut lamloh pai tih,
Pa tsiku la 21 la mwezi wachisanu ndi chiwiri, Yehova anayankhula kudzera mwa mneneri Hagai kuti:
2 Judah rhalboei Shealtiel capa Zerubbabel taengah khaw, khosoih puei Jehozadak capa Joshua taengah khaw, pilnam kah a meet taengah khaw thui laeh.
“Yankhula kwa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kwa anthu onse otsala. Afunse kuti,
3 “Hlamat vaengkah a thangpomnah dongah im aka hmu te nangmih khuiah unim aka sueng? Aka hmu rhoek nang te te metlam a om coeng? Te bang te na mik dongkah a hong bangla a om moenih a?
‘Kodi alipo amene watsala pakati panu amene anaona ulemerero wakale wa Nyumba iyi? Nanga tsopano ikuoneka motani kwa inu? Kodi sikuoneka ngati yopanda pake kwa inu?
4 Tedae Zerubbabel aw, BOEIPA kah olphong bangla thaahuel laeh. Khosoih puei Jehozadak capa Joshua thaahuel laeh. Khohmuen pilnam boeih loh thaahuel laeh. He tah BOEIPA kah olphong coeng ni. Nangmih taengah ka om coeng dongah saii uh laeh. He tah caempuei BOEIPA kah olphong ni.
Iwe Zerubabeli, limba mtima tsopano,’ akutero Yehova. ‘Limba mtima, iwe Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe. Limbani mtima, anthu nonse a mʼdziko,’ akutero Yehova, ‘ndipo gwirani ntchito. Pakuti ine ndili nanu,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
5 Ol he Egypt lamloh na lo vaengah ni nangmih taengah kang khueh coeng. Ka mueihla he na khui ah a om dongah rhih boeh.
‘Izi ndi zimene ndinapangana nanu pamene munkatuluka ku Igupto. Ndipo Mzimu wanga uli pakati panu. Musachite mantha.’
6 Caempuei BOEIPA loh he ni a thui. Vai khaw bet a om bal phoeiah tah vaan neh diklai khaw, tuitunli neh lanhak khaw ka hinghuen ni.
“Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Pakapita nthawi pangʼono ndidzagwedezanso thambo ndi dziko lapansi, nyanja ndi mtunda.
7 Namtom boeih te ka hinghuen vetih namtom boeih te sahnaih la ha pai uh ni. Te vaengah he im he thangpomnah ka bae sak ni tila caempuei BOEIPA loh a thui.
Ndidzagwedeza mitundu yonse ya anthu, ndipo chimene mitundu yonse ya anthu imachifuna chidzabwera, ndipo ndidzaza Nyumba ino ndi ulemerero,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
8 Cak he kamah kah tih sui khaw kamah kah ni. He tah caempuei BOEIPA kah olphong ni.
‘Siliva yense ndi wanga, golide yense ndi wanganso,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
9 “He im thangpomnah tah lamhma lakah khaw lamhnuk ah a len om ni,” tila caempuei BOEIPA loh a thui. Te dongah he hmuen ah ngaimongnah ka paek ni. He tah caempuei BOEIPA kah olphong ni.
‘Ulemerero wa nyumba iyi udzaposa ulemerero wa nyumba yoyamba ija,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse. ‘Ndipo pamalo pano ndidzakhazikitsapo mtendere,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.”
10 Darius kah a kum bae, hla ko, hin kul hnin li vaengah BOEIPA ol te tonghma Haggai taengla pai tih,
Chaka chachiwiri cha Dariyo, pa tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chinayi, Yehova anayankhula ndi mneneri Hagai kuti:
11 Caempuei BOEIPA loh he ni a thui. “Khosoih te olkhueng dawt laeh,” a ti nah.
“Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Funsa ansembe za zimene lamulo likunena:
12 Te dongah, “Hlang loh a himbai cun khuiah hmuencim maeh a phueih tih a hmoi neh buh khaw, andam khaw, misurtui khaw, situi khaw, caak te khat khat khaw, a ben te a ciim a?” a ti nah. Te vaengah khosoih rhoek loh a doo tih, “Cim mahpawh,” a ti uh.
Ngati munthu wakulunga nyama yopatulika mu mkanjo wake, ndipo mkanjowo nʼkukhudza buledi kapena msuzi, kapena vinyo, mafuta kapena chakudya cha mtundu wina uliwonse, kodi zimenezo zimasanduka zopatulika?’” Ansembe anayankha kuti, “Ayi.”
13 Te phoeiah Haggai loh, “Hinglu rhalawt loh he he boeih a ben atah, a poeih nama?” a ti nah. Te vaengah khosoih rhoek a doo uh tih, “A poeih loella,” a ti uh.
Pamenepo Hagai anati, “Ngati munthu amene anayipitsidwa pokhudza mtembo akhudza chimodzi cha zinthu zimenezi, kodi chinthucho chimayipitsidwa?” Ansembe anayankha kuti, “Inde, chimayipitsidwa.”
14 Te phoeiah Haggai loh a doo tih, “Pilnam he khaw, namtom he khaw, ka mikhmuh ah te tlam ni a om. He tah BOEIPA kah olphong ni. Te dongah a kut dongkah bibi boeih neh a khuen uh long khaw amah la hnap a cuem moenih.
Pamenepo Hagai anati, “‘Ndi mmene zilili ndi anthu awa ndi dziko ili pamaso panga,’ akutero Yehova. ‘Chilichonse amachita ndiponso chilichonse chimene amapereka nʼchodetsedwa.
15 Tahae khohnin lamlong tah na thinko ah dueh uh mai laeh. BOEIPA bawkim kah lungto soah lungto a tlingtlawn hang hlan ah.
“‘Tsopano muganizire zimenezi kuyambira lero mpaka mʼtsogolo. Ganizirani momwe zinthu zinalili asanayambe kumanga nyumba ya Yehova.
16 A om vaengah a hlom pakul lo cakhaw parha ni a lo. Sum sawmnga la a duh va-am te khaw pakul ni a lo.
Pamene munthu ankayembekezera miyeso ya tirigu makumi awiri ankangopeza khumi yokha. Munthu akapita kuti akatunge miyeso makumi asanu ya vinyo mu mtsuko, ankangopeza miyeso makumi awiri yokha.
17 Namamih khaw, nangmih kut dongkah bitat boeih khaw, mawn neh, dung neh, rhael neh kang ngawn coeng. Tedae kai taengla na mael uh moenih. He tah BOEIPA kah olphong coeng ni.
Ndinawononga ntchito yonse ya manja anu ndi chinsikwi, chiwawu ndi matalala, komabe inu simunatembenukire kwa Ine,’ akutero Yehova
18 Tahae khohnin lamlong tah na thinko ah dueh uh laeh. BOEIPA bawkim a suen hnin lamloh a hlako hnin kul hnin li so hang te na thinko ah khueh uh laeh.
‘Kuyambira lero tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chinayi mpaka mʼtsogolo, chonde ganizirani bwino tsiku limene munayika maziko a nyumba ya Yehova. Ganizirani bwino.
19 Cangpup khuiah cangti khaw om dae nim? Misur neh thaibu khaw, tale neh olive thing khaw cuen pawh. Tahae khohnin lamlong tah yoethen kam paek pawn ni,” a ti nah.
Kodi mʼnkhokwe mwatsala mbewu? Mpaka lero, mpesa ndi mtengo wa mkuyu, makangadza ndi mtengo wa olivi sizinabereke zipatso. “‘Kuyambira lero mpaka mʼtsogolo ndidzakudalitsani.’”
20 Te kah hla hnin kul neh hnin li hnin ah tah BOEIPA ol he Haggai taengah a pabae la cet tih,
Yehova anayankhula ndi Hagai kachiwiri, pa tsiku la 24 la mwezi kuti:
21 “Judah rhalboei Zerubbabel taengah thui pah lamtah, 'Vaan neh diklai he ka hinghuen coeng.
“Uza Zerubabeli, bwanamkubwa wa Yuda, kuti ndidzagwedeza thambo ndi dziko lapansi.
22 Ram ngolkhoel te ka palet vetih namtom ram kah thaa te ka bawt sak ni. Leng neh a sokah aka ngol khaw ka palet ni. Te vaengah marhang neh a sokah aka ngol khaw, hlang khaw a manuca kah cunghang dongah kaeh uh ni.
Ndidzagwetsa mipando yaufumu ndi kuwononga mphamvu za maufumu achilendo. Ndidzagubuduza magaleta ndi okwerapo ake; akavalo ndi okwerapo ake adzagwa, aliyense adzaphedwa ndi lupanga la mʼbale wake.
23 He tah caempuei BOEIPA kah olphong ni. Te khohnin ah tah ka sal Shealtiel capa Zerubbabel nang te kan loh ni. He tah BOEIPA kah olphong ni. Nang te kan coelh coeng dongah nang te kutbuen la kan khueh ni. He tah caempuei BOEIPA kah olphong ni, 'ti nah,” a ti nah.
“‘Tsiku limenelo,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse, ‘ndidzakutenga, iwe mtumiki wanga Zerubabeli mwana wa Sealatieli,’ akutero Yehova, ‘ndipo ndidzakusandutsa kukhala mphete yanga yolamulira, pakuti ndasankha iwe,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.”

< Haggai 2 >