< 2 Khokhuen 2 >

1 Te phoeiah Solomon loh BOEIPA ming ham im sak ham neh a ram ham im sak hamla cai.
Solomoni anatsimikiza zoti amange Nyumba ya Dzina la Yehova ndi nyumba yake yaufumu.
2 Solomon loh boe a soep vaengah hnophuei hlang thawng sawmrhih, tlang ah lungto aka dae hlang thawng sawmrhet, amih aka mawt te thawng thum neh ya rhuk lo.
Iye analemba ntchito anthu 70,000 onyamula katundu ndi anthu 80,000 okumba miyala ku mapiri ndiponso akapitawo 3,600 oyangʼanira anthuwo.
3 Te phoeiah Solomon loh Tyre manghai Huram taengah ol a tah tih, “A pa David ham na saii dongah amah ham im a sak vaengah a taengla lamphai na thak pah vanbangla a khuiah kho a sak coeng.
Solomoni anatumiza uthenga uwu kwa Hiramu mfumu ya ku Turo: “Munditumizire mitengo ya mkungudza monga munachitira ndi abambo anga pamene munawatumizira mitengo ya mkungudza yomangira nyumba yaufumu yokhalamo.
4 Kai loh im ka sak he ka Pathen BOEIPA ming ham ni. Te te ciim ham neh a mikhmuh ah botui bo-ul phum ham om. Sainoek la rhungkung buh neh hmueihhlutnah tah hlaem ham neh mincang ham khaw, Sabbath vaeng neh hlasae vaengah nawn ham om. He tah kaimih kah Pathen BOEIPA loh Israel soah kumhal hil khoning vaengkah la a khueh.
Tsono ine ndikufuna kumanga Nyumba ya Yehova Mulungu wanga ndi kuyipereka kwa Iye kuti tiziyikamo buledi wopatulika nthawi zonse ndiponso kuperekeramo nsembe zopsereza mmawa uliwonse ndi madzulo ndi pa masabata ndi pa masiku a chikondwerero cha mwezi watsopano ndiponso pa masiku osankhika a chikondwerero cha Yehova Mulungu wathu, monga mwa malamulo a Aisraeli mpaka muyaya.
5 Kaimih kah Pathen tah pathen boeih lakah a len dongah ni im te khaw a len la ka sak.
“Nyumba ya Mulungu imene ndidzamange idzakhala yayikulu, chifukwa Mulungu wathu ndi wamkulu kuposa milungu ina yonse.
6 Tedae a im sak pah ham te u long thadueng a capit eh? Vaan neh vaan phoeikah vaan long pataeng anih te a cangbam uh thai moenih. A mikhmuh ah ka phum uh ham bueng phoeiah tah a im ka sak ham khaw kai he unim?
Koma ndani angathe kumumangira Iye Nyumba, pakuti mlengalenga, ngakhale kumwamba kwenikweni sikungamukwane? Tsono ine ndine yani kuti ndimangire Iyeyo Nyumba, kupatula malo chabe opserezerapo nsembe pamaso pake?
7 Te dongah sui neh, cak neh, rhohum neh, thi neh, daidi neh, aithii neh, a thim neh saii ham te hlang cueih kai taengah han tueih mai. Thingthuk thuk ham aka ming khaw kamah taengkah hlangcueih rhoek neh Judah ah khaw Jerusalem ah khaw om uh saeh. Te rhoek te a pa David loh a sikim sak coeng.
“Tsono tumizireni munthu waluso pa ntchito zagolide ndi siliva, mkuwa ndi chitsulo, nsalu yapepo ndi yofiira ndi yobiriwira ndiponso waluso losema, kuti adzagwire ntchito mu Yuda ndi Yerusalemu pamodzi ndi anthu aluso amene abambo anga Davide anandipatsa.
8 Lebanon lamkah lamphai hmaical thing neh algum te kai hamla ham pat mai. Lebanon thing vung hamla aka ming tah namah kah sal rhoek ni tila ka ming dongah ni. Tedae ka sal rhoek he na sal rhoek taengah om ngawn ne.
“Munditumizirenso mitengo ya mkungudza, payini ndiponso matabwa a mʼbawa wa ku Lebanoni, pakuti ndikudziwa kuti anthu anu ali ndi luso locheka matabwa kumeneko. Antchito anga adzagwira ntchito pamodzi ndi antchito anu
9 Im te a len neh khobaerhambae la ka sak ham dongah thing khaw kamah taengah a cung la a sikim ham om van.
kuti andipatse matabwa ambiri, chifukwa Nyumba imene ndikumanga iyenera kukhala yayikulu ndi yokongola.
10 Thing aka vung tih aka top ham khaw na sal rhoek te cang yen kore thawng kul, cangtun kore thawng kul, misurtui bath thawng kul, situi bath thawng kul ka paek bitni ne,” a ti nah.
Ine ndidzalipira antchito anu amene adzacheke matabwa matani 1,000 a tirigu wopunthapuntha, matani 2,000 a barele, malita 440,000 a vinyo, ndiponso malita 440,000 a mafuta a olivi.”
11 Te dongah Tyre manghai Huram loh ca neh a voek tih, Solomon taengah, “BOEIPA loh a pilnam te a lungnah dongah nang te amih soah manghai la n'khueh,” tila a pat.
Hiramu, mfumu ya ku Turo, anamuyankha Solomoni pomulembera kalata kuti, “Chifukwa Yehova amakonda anthu ake, wayika iwe kukhala mfumu yawo.”
12 Te vaengah Huram loh, “Israel Pathen BOEIPA tah a yoethen pai. Amah loh vaan neh diklai a saii. Amah loh manghai David taengah lungmingnah neh yakmingnah aka ming capa hlangcueih te a paek. Te long te BOEIPA ham im neh a ram ham im a sak ni.
Ndipo Hiramu anawonjezera kunena kuti, “Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli, amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi! Iye wamupatsa Davide mwana wanzeru, wodzaza ndi luntha ndi wozindikira, amene adzamanga Nyumba ya Mulungu ndi kudzimangira yekha nyumba yaufumu.
13 Te dongah yakmingnah aka ming, hlang cueih Huramabi te kan tueih coeng.
“Ine ndikukutumizira Hiramu Abi, munthu wa luso lalikulu,
14 Anih he Dan nu lamkah huta pakhat kah a capa tih a napa he Tyre hlang ni. Anih tah sui neh, cak neh, rhohum neh, thi neh, lungto neh, thing neh, daidi la, a thim la, baibok la, aithii la saii ham, thingthuk cungkuem a thuk ham khaw, a taengah a paek kopoek boeih te ngai ham khaw a ming. Nang kah hlangcueih rhoek neh na pa David, ka boeipa kah hlangcueih taengah om bitni.
amene amayi ake anali wochokera ku Dani ndipo abambo ake anali a ku Turo. Iye anaphunzitsidwa kugwira ntchito zagolide ndi siliva, mkuwa ndi chitsulo, miyala yokongola ndi matabwa, ndiponso nsalu zofewa zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Alinso ndi luso la zosemasema ndipo atha kupanga chilichonse chimene wapatsidwa. Iye adzagwira ntchito ndi amisiri anu ndi a mbuye wanga, Davide abambo anu.
15 Te dongah cang neh cangtun khaw, situi neh misurtui khaw ka boeipa kah a thui bangla a sal rhoek taengah pat laeh saeh.
“Tsono mbuye wanga tumizirani antchito anu tirigu ndi barele, mafuta a olivi ndi vinyo zimene mwalonjeza,
16 Na ngoengaihnah boeih tarhing ah Lebanon lamkah thing te kaimih loh kam vung vetih Joppa tuipuei lamloh nang taengah pan kan thak uh bitni. Te te namah loh Jerusalem la khuen,” a ti nah.
ndipo ife tidzadula mitengo yonse imene mukuyifuna kuchokera ku Lebanoni ndipo tidzayimanga pamodzi ndi kuyiyadamitsa pa madzi mpaka ku Yopa. Ndipo inu mudzatha kuyitenga mpaka ku Yerusalemu.”
17 A napa David loh mingsoepnah a soep hnukah Solomon loh Israel khohmuen kah yinlai hlang te boeih a soep tih thawng yakhat neh thawng sawmnga neh thawng thum ya rhuk a hmuh.
Solomoni anawerenga alendo onse amene anali mu Israeli, potsatira chiwerengero chimene abambo ake Davide anachita ndipo panapezeka kuti analipo anthu 153,600.
18 Amih khuiah thawng sawmrhih te hnophuei la, thawng sawmrhet te tlang ah lungto aka dae la, thawng thum ya rhuk te pilnam kah a thohtat aka mawt la a khueh.
Iye anayika anthu 70,000 kuti akhale onyamula katundu ndi anthu 80,000 kuti akhale ophwanya miyala mʼmapiri, anthu 3,600 anawayika kukhala akapitawo oyangʼanira anthu pa ntchitoyo.

< 2 Khokhuen 2 >