< Nyimbo ya Solomoni 8 >

1 Ukanakhala kuti ndiwe mlongo wanga, amene anayamwa mawere a amayi anga! Ndikanakumana nawe pa njira, ndikanakupsompsona, ndipo palibe wina aliyense akanandinyoza.
O da bi mi brat bio, da bi sao sise matere moje! našavši te na polju poljubila bih te, i ne bih bila prijekorna.
2 Ndikanakutenga ndi kukulowetsa mʼnyumba ya amayi anga, amayi amene anandiphunzitsa, ndikanakupatsa vinyo wotsekemera kuti umwe, zotsekemera za makangadza.
Povela bih te i dovela bih te u kuæu matere svoje; ti bi me uèio, a ja bih te pojila vinom mirisavijem, sokom od šipaka.
3 Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere ndipo dzanja lake lamanja landikumbatira.
Lijeva je ruka njegova meni pod glavom a desnom me grli.
4 Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani: musachigwedeze chikondi kapena kuchiutsa mpaka pamene chifunire ichocho.
Zaklinjem vas, kæeri Jerusalimske, ne budite ljubavi moje, ne budite je, dokle joj ne bude volja.
5 Kodi ndani uyo akutuluka ku chipululuyo, atatsamira wokondedwa wakeyo? Mkazi Ndinakudzutsa pa tsinde pa mtengo wa apulosi, pamenepo ndi pamene amayi anachirira, pamenepo ndi pamene wokubereka anamva ululu pokubala iweyo.
Ko je ona što ide gore iz pustinje naslanjajuæi se na dragoga svoga? Pod jabukom probudih te, gdje te rodi mati tvoja, gdje te rodi roditeljka tvoja.
6 Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
Metni me kao peèat na srce svoje, kao peèat na mišicu svoju. Jer je ljubav jaka kao smrt, i ljubavna sumnja tvrda kao grob; žar je njezin kao žar ognjen, plamen Božji. (Sheol h7585)
7 Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, mitsinje singachikokolole chikondicho. Ngati wina apereka chuma chonse cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu.
Mnoga voda ne može ugasiti ljubavi, niti je rijeke potopiti. Da ko daje sve imanje doma svojega za tu ljubav, osramotio bi se.
8 Ife tili naye mlongo wathu wamngʼono, koma alibe mawere, kodi tidzamuchitira chiyani mlongo wathuyu pa tsiku limene adzamufunsire?
Imamo sestru malenu, koja još nema dojaka. Šta æemo èiniti sa sestrom svojom kad bude rijeè o njoj?
9 Ngati iye ndi khoma, tidzamumangira nsanja ya siliva. Ngati iye ndi chitseko, tidzamutchinga ndi matabwa a mkungudza.
Ako je zid, sagradiæemo na njemu dvor od srebra; ako li vrata, utvrdiæemo ih daskama kedrovijem.
10 Ine ndili ngati khoma, ndipo mawere anga ndi nsanja zake. Tsono mʼmaso mwa bwenzi langa ndine wobweretsa mtendere.
Ja sam zid i dojke su moje kao kule. Tada postah u oèima njegovijem kao ona koja naðe mir.
11 Solomoni anali ndi munda wampesa ku Baala-Hamoni; iyeyo anabwereketsa munda wamphesawo kwa alimi, aliyense mwa iwo ankayenera kupereka ndalama zasiliva 1,000 mʼmalo mwa zipatso zake.
Vinograd imaše Solomun u Valamonu; dade vinograd èuvarima da svaki donosi za rod njegov po tisuæu srebrnika.
12 Koma munda wanga wampesa ndi wangawanga ndiponso wa ine ndekha. Iwe Solomoni, khala nazo ndalama zasiliva 1,000 ndipo ndalama zasiliva 200 ndi za amene akusamalira mundawo.
Moj vinograd koji ja imam, preda mnom je. Neka tebi, Solomune, tisuæa, i dvije stotine onima koji èuvaju rod njegov.
13 Iwe amene umakhala mʼminda uli pamodzi ndi anzako, ndilole kuti ndimve liwu lako!
Koja nastavaš u vrtovima! drugovi slušaju glas tvoj, daj mi da ga èujem.
14 Fulumira wokondedwa wanga, ndipo ukhale ngati gwape kapena mwana wa mbawala wothamanga mʼmapiri mʼmene mumamera mbewu zokometsera chakudya.
Brže, dragi moj! i budi kao srna ili kao jelenèe na gorama mirisnijem.

< Nyimbo ya Solomoni 8 >