< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
Przewodnikowi chóru. Psalm Dawida dla przypomnienia. Boże, racz mnie ocalić; PANIE, pospiesz mi na pomoc.
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Niech się zawstydzą i okryją hańbą ci, którzy czyhają na moją duszę; niech się cofną ze wstydem ci, którzy mi źle życzą.
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Niech się cofną wskutek swej hańby ci, którzy mi mówią: Ha, ha!
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Niech się weselą i radują w tobie wszyscy, którzy cię szukają; niech ci, którzy miłują twoje zbawienie, mówią zawsze: Niech Bóg będzie wywyższony!
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
Ja zaś jestem nędzny i ubogi, Boże, pospiesz ku mnie, ty jesteś moją pomocą i wybawicielem; PANIE, nie zwlekaj.

< Masalimo 70 >