< Masalimo 41 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka; Yehova amamuwombola pa nthawi yamsautso.
Blago onome koji razumije ništemu! Gospod æe ga izbaviti u zli dan.
2 Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake; Yehova adzamudalitsa iye mʼdziko ndipo sadzamupereka ku zofuna za adani ake.
Gospod æe ga saèuvati i poživiæe ga; biæe blažen na zemlji. Neæeš ga dati na volju neprijateljima njegovijem.
3 Yehova adzamuthandiza pamene akudwala ndipo adzamuchiritsa pa bedi lake la matenda.
Gospod æe ga ukrijepiti bolna na odru. Sasvijem mijenjaš postelju njegovu u bolesti njegovoj.
4 Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo; chiritseni pakuti ndakuchimwirani.”
Ja vièem: Gospode! smiluj se na me, iscijeli dušu moju, sagriješih ti.
5 Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti, “Kodi munthu ameneyu adzafa liti kuti ayiwalike?”
Neprijatelji moji govore zlobno za mene: “kad æe umrijeti, i ime njegovo poginuti?”
6 Pamene wina abwera kudzandiona, amayankhula mwachinyengo, pomwe mtima wake ukusonkhanitsa zachipongwe; kenaka iye amatuluka ndi kukalengeza kunja.
I ako ko doðe da me vidi, laska; srce njegovo slaže u sebi nepravdu, i otišavši kazuje.
7 Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane, iwo amalingalira zoyipa kwambiri za ine, ponena kuti,
Šapæu o meni meðu sobom neprijatelji moji, i misle mi zlo:
8 “Matenda owopsa amugwira; sadzaukapo pamalo pamene wagona.”
“Zla stvar doðe na njega, legao je; neæe više ustati.”
9 Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira, iye amene amadya pamodzi ndi ine watukula chidendene chake kulimbana nane.
I èovjek mira mojega, u kojega se uzdah, koji jeðaše hljeb moj, podiže na me petu.
10 Koma Yehova mundichititre chifundo, dzutseni kuti ndiwabwezere.
Ali ti, Gospode, smiluj se na me, i podigni me; a ja æu im vratiti.
11 Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane, pakuti mdani wanga sandigonjetsa.
Po tome æu poznati da sam ti mio, ako se ne uzraduje neprijatelj moj nada mnom.
12 Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga ndi kundiyimika pamaso panu kwamuyaya.
A mene cijela saèuvaj, i daj mi da stojim pred licem tvojim dovijeka.
13 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli kuchokera muyaya mpaka muyaya. Ameni ndi Ameni.
Blagosloven Bog Izrailjev od vijeka do vijeka. Amin, amin.

< Masalimo 41 >