< Masalimo 37 >

1 Salimo la Davide. Usamavutike chifukwa cha anthu oyipa kapena kuchitira nsanje amene akuchita cholakwa;
Psalm Dawida. Nie oburzaj się z powodu złoczyńców ani nie zazdrość czyniącym nieprawość.
2 pakuti monga udzu iwo adzafota msanga, ngati mbewu zobiriwira adzanyala msanga.
Jak trawa bowiem prędko zostaną podcięci i zwiędną jak świeża zieleń.
3 Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino; khazikika mʼdziko ndi kutsata zokhulupirika.
Ufaj PANU i czyń dobrze; będziesz mieszkał na ziemi i na pewno będziesz nakarmiony.
4 Udzikondweretse wekha mwa Yehova ndipo Iye adzakupatsa zokhumba za mtima wako.
Rozkoszuj się PANEM, a on spełni pragnienia twego serca.
5 Pereka njira yako kwa Yehova; dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:
Powierz PANU swoją drogę i zaufaj mu, a on wszystko wykona;
6 Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha, chiweruzo chako ngati dzuwa la masana.
I wyniesie twoją sprawiedliwość jak światłość, a twoją prawość jak południe.
7 Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa; usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo, pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa.
Poddaj się PANU i oczekuj go; nie oburzaj się na tego, komu powodzi się w drodze, na człowieka, który spełnia swe złe zamiary.
8 Pewa kupsa mtima ndipo tembenuka kuchoka ku ukali, usavutike chifukwa zimenezi zimatsogolera ku zoyipa.
Zaprzestań gniewu i zaniechaj zapalczywości; nie zapalaj się gniewem do czynienia zła.
9 Pakuti anthu oyipa adzachotsedwa, koma iwo amene amayembekeza mwa Yehova adzalandira dziko.
Złoczyńcy bowiem będą wytępieni, a ci, którzy oczekują PANA, odziedziczą ziemię.
10 Kwa kanthawi oyipa sadzapezekanso; ngakhale muwafunefune, sadzapezekanso.
Jeszcze chwila, a nie będzie niegodziwego; spojrzysz na jego miejsce, a już go nie będzie.
11 Koma ofatsa adzalandira dziko ndipo adzasangalala ndi mtendere waukulu.
Lecz pokorni odziedziczą ziemię i będą się rozkoszować obfitością pokoju.
12 Oyipa amakonza chiwembu kutsutsana ndi olungama ndipo amawakukutira mano;
Niegodziwy knuje przeciwko sprawiedliwemu i zgrzyta na niego zębami.
13 koma Ambuye amaseka oyipa pakuti Iye amadziwa kuti tsiku lawo likubwera.
Lecz Pan śmieje się z niego, bo widzi, że nadchodzi jego dzień.
14 Oyipa amasolola lupanga ndi kupinda uta kugwetsa osauka ndi osowa, kupha iwo amene njira zawo ndi zolungama.
Niegodziwi dobyli miecz i napinają swój łuk, aby powalić ubogiego i potrzebującego, aby zgładzić tych, którzy idą prawą drogą;
15 Koma malupanga awo analasa mitima yawo yomwe, ndipo mauta awo anathyoka.
Lecz ich miecz przeszyje ich własne serca, a ich łuki będą złamane.
16 Zabwino zochepa zimene olungama ali nazo ziposa chuma cha anthu oyipa ambiri;
Lepsza jest odrobina, którą ma sprawiedliwy, niż wielkie bogactwa wielu niegodziwych;
17 pakuti mphamvu ya oyipa idzasweka, koma Yehova amasunga olungama.
Ramiona bowiem niegodziwych będą połamane, ale sprawiedliwych PAN podtrzymuje.
18 Masiku a anthu osalakwa amadziwika ndi Yehova, ndipo cholowa chawo chidzakhala mpaka muyaya.
PAN zna dni nienagannych, ich dziedzictwo będzie trwać na wieki.
19 Pa nthawi ya mavuto iwo sadzafota; mʼmasiku a njala adzakhala ndi zinthu zambiri.
W czasie nieszczęścia nie doznają wstydu, a w dniach głodu będą nasyceni.
20 Koma oyipa adzawonongeka; adani a Yehova adzakhala ngati kukongola kwa kuthengo, iwo adzazimirira ngati utsi.
Niegodziwi zaś wyginą, a wrogowie PANA znikną jak tłuszcz barani, jak dym się rozwieją.
21 Oyipa amabwereka ndipo sabweza koma olungama amapereka mowolowamanja.
Niegodziwy pożycza i nie zwraca, a sprawiedliwy lituje się i rozdaje.
22 Iwo amene Yehova amawadalitsa adzalandira dziko, koma amene Iye amawatemberera adzachotsedwa.
Błogosławieni przez [PANA] odziedziczą ziemię, a przeklęci przez niego zostaną wytępieni.
23 Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu, amakhazikitsa mayendedwe ake;
PAN kieruje krokami [dobrego] człowieka i jego droga mu się podoba.
24 ngakhale atapunthwa sadzagwa, pakuti Yehova amamutchinjiriza ndi dzanja lake.
Choćby upadł, nie zostanie [całkowicie] powalony, bo PAN podtrzymuje [go] swą ręką.
25 Ine ndinali wamngʼono ndipo tsopano ndakalamba koma sindinaonepo olungama akusiyidwa kapena ana awo akupempha chakudya.
Byłem młody i jestem już stary, [lecz] nie widziałem sprawiedliwego, który by był opuszczony, ani żeby jego potomstwo żebrało o chleb.
26 Iwo ndi owolowamanja nthawi zonse ndipo amabwereketsa mwaufulu; ana awo adzadalitsika.
Każdego dnia lituje się i pożycza, a jego potomstwo [jest] błogosławione.
27 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino; pamenepo udzakhazikika mʼdziko kwamuyaya.
Odstąp od złego i czyń dobrze, a będziesz trwał na wieki.
28 Pakuti Yehova amakonda wolungama ndipo sadzasiya okhulupirika ake. Iwo adzatetezedwa kwamuyaya, koma zidzukulu za oyipa zidzachotsedwa;
PAN bowiem miłuje prawość i nie opuszcza swoich świętych, strzeże ich na wieki; a potomstwo niegodziwych będzie wytępione.
29 olungama adzalandira dziko ndipo adzakhazikikamo kwamuyaya.
Sprawiedliwi odziedziczą ziemię i będą na niej mieszkać na wieki.
30 Pakamwa pa munthu wolungama pamayankhula za nzeru, ndipo lilime lake limayankhula zolungama.
Usta sprawiedliwego wypowiadają mądrość, a jego język mówi o sądzie.
31 Lamulo la Mulungu wake lili mu mtima mwake; mapazi ake saterereka.
Prawo jego Boga [jest] w jego sercu, jego kroki się nie zachwieją.
32 Oyipa amabisala kudikira olungama; kufunafuna miyoyo yawoyo;
Niegodziwy czyha na sprawiedliwego i szuka [sposobności], aby go zabić.
33 koma Yehova sadzawasiya pansi pa mphamvu yawo kapena kuti atsutsidwe pamene abweretsedwa pa milandu.
[Lecz] PAN nie zostawi go w jego ręku i nie potępi, gdy będzie sądzony.
34 Khulupirira Yehova, ndipo sunga njira yake; Iye adzakukweza ndipo udzalandira dziko kuti likhale lako; udzaona anthu oyipa akuwonongeka.
Oczekuj PANA i strzeż jego drogi, a on cię wywyższy, abyś odziedziczył ziemię; zobaczysz zatracenie niegodziwych.
35 Ine ndinaona munthu woyipa ndi munthu wopanda chifundo akupeza bwino ngati mtengo wobiriwira pa nthaka ya makolo ake.
Widziałem niegodziwego bardzo wyniosłego i rozpierającego się jak zielone drzewo laurowe;
36 Koma sanachedwe kumwalira ndipo sanaonekenso; ngakhale ndinamuyangʼanayangʼana, sanapezekenso.
Lecz przeminął i oto już go nie było; szukałem go, ale nie mogłem go znaleźć.
37 Ganizira za munthu wosalakwa, yangʼanitsitsa munthu wolungama; udzaona kuti ali ndi tsogolo labwino ndipo ali ndi zidzukulu zambiri.
Spójrz na nienagannego i przypatruj się prawemu, bo ten na końcu osiągnie pokój.
38 Koma anthu ochimwa adzawonongeka; iwowo pamodzi ndi zidzukulu zawo zomwe.
Lecz przestępcy razem zginą, niegodziwi na końcu zostaną wytępieni.
39 Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova; Iye ndiye linga lawo pa nthawi ya masautso.
Zbawienie zaś sprawiedliwych [pochodzi] od PANA; [on jest] ich siłą w czasie utrapienia.
40 Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa; Iye amawalanditsa kwa oyipa ndi kuwapulumutsa, pakuti amathawira kwa Iye.
PAN ich wspomoże i wyzwoli; wyzwoli ich od niegodziwych i wybawi, bo w nim pokładają nadzieję.

< Masalimo 37 >