< Masalimo 3 >

1 Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu. Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira!
Gospode! kako je mnogo neprijatelja mojih! Mnogi ustaju na me.
2 Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” (Sela)
Mnogi govore za dušu moju: nema mu pomoæi od Boga.
3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza, Inu mwandiveka ulemerero ndipo mwanditukula.
Ali ti si, Gospode, štit koji me zaklanja, slava moja; ti podižeš glavu moju.
4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera. (Sela)
Glasom svojim vièem ka Gospodu, i èuje me sa svete gore svoje.
5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo; ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza.
Ja liježem, spavam i ustajem, jer me Gospod èuva.
6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene abwera kulimbana nane kuchokera ku madera onse.
Ne bojim se mnogo tisuæa naroda što sa svijeh strana navaljuje na me.
7 Dzukani, Inu Yehova! Pulumutseni, Inu Mulungu wanga. Akantheni adani anga onse pa msagwada; gululani mano a anthu oyipa.
Ustani, Gospode! pomozi mi, Bože moj! jer ti udaraš po obrazu sve neprijatelje moje; razbijaš zube bezbožnicima.
8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova. Madalitso akhale pa anthu anu. (Sela)
Od Gospoda je spasenje; neka bude na narodu tvom blagoslov tvoj!

< Masalimo 3 >