< Masalimo 13 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
Dokle æeš me, Gospode, sasvijem zaboravljati? dokle æeš odvraæati lice svoje od mene?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
Dokle æu se domišljati u duši svojoj, mutiti se u srcu svom dan i noæ? dokle æe se neprijatelj moj podizati nada mnom?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
Pogledaj, usliši me, Gospode, Bože moj! Prosvijetli oèi moje da ne zaspim na smrt.
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
Da ne reèe neprijatelj moj: nadvladao sam ga; da se ne raduju koji me gone, ako posrnem.
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
A ja se uzdam u milost tvoju; radovaæe se srce moje za spasenje tvoje.
6 Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.
Pjevaæu Gospodu, koji mi dobro èini.

< Masalimo 13 >