< Masalimo 127 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
Ako Gospod neæe graditi doma, uzalud se muèe koji ga grade; ako neæe Gospod èuvati grada, uzalud ne spava stražar.
2 Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
Uzalud ranite, dockan liježete, jedete hljeb umorni; milome svojemu on daje san.
3 Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
Evo našljedstva od Gospoda: djeca, porod je dar od njega.
4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
Što su strijele u ruci jakome, to su sinovi mladi.
5 Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.
Blago èovjeku koji je njima napunio tul svoj! Neæe se osramotiti kad se stanu razgovarati s neprijateljima na vratima.

< Masalimo 127 >