< Masalimo 100 >

1 Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
Raduj se Gospodu, sva zemljo!
2 Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
Služite Gospodu veselo; idite pred lice njegovo pjevajuæi!
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
Poznajte Gospod da je Bog. On nas je stvorio, i mi smo dostojanje njegovo, narod njegov i ovce paše njegove.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
Ulazite na vrata njegova sa slavom, u dvore njegove s hvalom. Slavite ga, i blagosiljajte ime njegovo.
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.
Jer je dobar Gospod; milost je njegova uvijek, i istina njegova od koljena na koljeno.

< Masalimo 100 >