< Miyambo 22 >

1 Mbiri yabwino ndi yofunika kuposa chuma chambiri; kupeza kuyanja nʼkwabwino kuposa siliva kapena golide.
Bolje je ime nego veliko bogatstvo, i milost je bolja nego srebro i zlato.
2 Wolemera ndi wosauka ndi ofanana; onsewa anawalenga ndi Yehova.
Bogat i siromah sretaju se; obojicu je Gospod stvorio.
3 Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala, koma munthu wopusa amangopitirira ndipo amadzanongʼoneza bondo.
Pametan èovjek vidi zlo i skloni se, a ludi idu dalje i plaæaju.
4 Mphotho ya munthu wodzichepetsa ndi woopa Yehova ndi chuma, ulemu ndi moyo.
Smjernosti i strahu Gospodnjemu plata je bogatstvo i slava i život.
5 Mʼnjira za anthu oyipa muli minga ndi misampha, koma amene amasala moyo wake adzazipewa zonsezo.
Trnje i zamke su na putu opakoga; ko èuva dušu svoju, biæe daleko od toga.
6 Mwana muzimuphunzitsa njira yake, ndipo akadzakalamba sadzachokamo.
Uèi dijete prema putu kojim æe iæi, pa neæe otstupiti od njega ni kad ostari.
7 Wolemera amalamulira wosauka, ndipo wokongola zinthu amakhala kapolo wa womukongozayo.
Bogat gospodari nad siromasima, i ko uzima u zajam biva sluga onomu koji daje.
8 Amene amafesa zoyipa amakolola mavuto, ndipo ndodo yaukali wake idzathyoka.
Ko sije bezakonje žeæe muku, i pruta gnjeva njegova nestaæe.
9 Amene ali ndi diso lachifundo adzadalitsika, pakuti iye amagawana chakudya chake ndi anthu osauka.
Blago oko biæe blagosloveno, jer daje hljeba svojega ubogomu.
10 Chotsani munthu wonyoza, ndipo kukangana kudzatha; mapokoso ndi zonyoza zidzaleka.
Otjeraj potsmjevaèa, i otiæi æe raspra i prestaæe svaða i sramota.
11 Amene amakonda kukhala woyera mtima ndi kumayankhula mawu abwino, adzakhala bwenzi la mfumu.
Ko ljubi èisto srce, i èije su usne ljubazne, njemu je car prijatelj.
12 Maso a Yehova amakhala pa anthu odziwa bwino zinthu, koma Iye adzalepheretsa mawu a anthu osakhulupirika.
Oèi Gospodnje èuvaju znanje, a poslove bezakonikove obara.
13 Munthu waulesi amati, “Kunjaku kuli mkango. Ine ndidzaphedwa mʼmisewu!”
Ljenivac govori: lav je napolju; nasred ulice poginuo bih.
14 Pakamwa pa mkazi wachigololo pali ngati dzenje lozama; amene Yehova wamukwiyira adzagwamo.
Usta su tuðih žena jama duboka; na koga se gnjevi Gospod, onamo æe pasti.
15 Uchitsiru umakhala mu mtima mwa mwana, koma ndodo yomulangira mwanayo idzachotsa uchitsiruwo.
Bezumlje je privezano djetetu na srce; prut kojim se kara ukloniæe ga od njega.
16 Amene amapondereza anthu osauka kuti awonjezere chuma chake, ndiponso amene amapereka mphatso kwa anthu olemera onsewa adzasauka.
Ko èini krivo siromahu da umnoži svoje, i ko daje bogatome, zacijelo æe osiromašiti.
17 Utchere khutu lako ndipo umvere mawu anzeru; uyike mtima wako pa zimene ndikukuphunzitsa kuti udziwe.
Prigni uho svoje i slušaj rijeèi mudrijeh ljudi, i srce svoje privij k nauci mojoj.
18 Zidzakhala zokondweretsa ngati uzisunga mu mtima mwako ndi wokonzeka kuziyankhula.
Jer æe ti biti milina ako ih složiš u srce svoje, ako sve budu poreðane na usnama tvojim.
19 Ndakuphunzitsa zimenezi lero koma makamaka uziopa Yehova.
Da bi ti uzdanje bilo u Gospoda, kazujem ti ovo danas, a ti tako èini.
20 Kodi suja ndinakulembera malangizo makumi atatu okuchenjeza ndi okupatsa nzeru,
Nijesam li ti napisao znamenite stvari za savjete i znanje,
21 malangizo okudziwitsa zolungama ndi zoona ndi kuti ukawayankhe zoona amene akutumawo?
Da bih ti pokazao tvrðu istinitijeh rijeèi da bi mogao istinitijem rijeèima odgovarati onima koji pošlju k tebi?
22 Mʼmphawi usamubere chifukwa ndi osauka, ndipo usawapondereze anthu osowa mʼbwalo la milandu,
Ne otimaj siromahu zato što je siromah, i ne zatiri nevoljnoga na vratima.
23 pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo ndipo adzalanda moyo onse amene amawalanda iwo.
Jer æe Gospod braniti njihovu stvar, i oteæe dušu onima koji njima otimaju.
24 Usapalane naye ubwenzi munthu wosachedwa kupsa mtima ndipo usayanjane ndi munthu amene sachedwa kukwiya
Ne druži se s èovjekom gnjevljivijem i ne idi sa žestokim,
25 kuopa kuti iwe ungadzaphunzire njira zake ndi kukodwa mu msampha.
Da se ne bi navikao na putove njegove i metnuo zamke na dušu svoju.
26 Usakhale munthu wopereka chikole kapena kukhala mboni pa ngongole;
Ne budi od onijeh koji ruku daju, koji se jamèe za dugove.
27 ngati ulephera kupeza njira yolipirira adzakulanda ngakhale bedi lako lomwe.
Ako nemaš èim platiti, zašto da se odnese postelja ispod tebe?
28 Usasunthe mwala wamʼmalire akalekale amene anayikidwa ndi makolo ako.
Ne pomièi stare meðe, koju su postavili oci tvoji.
29 Kodi ukumuona munthu waluso pa ntchito yake? Iye adzatumikira mafumu; sadzatumikira anthu wamba.
Jesi li vidio èovjeka ustaoca na poslu? Taki æe pred carevima stajati, a neæe stajati pred prostacima.

< Miyambo 22 >