< Nehemiya 10 >

1 Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
Un uz tā apzieģelētā stāvēja: Nehemija, tas zemes soģis, Hakalijas dēls, un Cedeķija,
2 Seraya, Azariya, Yeremiya
Seraja, Azarija, Jeremija,
3 Pasuri, Amariya, Malikiya,
Pašhurs, Amarija, Malhija,
4 Hatusi, Sebaniya, Maluki,
Hatus, Šebanija, Maluks,
5 Harimu, Meremoti, Obadiya,
Harims, Merimots, Obadija,
6 Danieli, Ginetoni, Baruki,
Daniēls, Ģintuns, Bāruks,
7 Mesulamu, Abiya, Miyamini
Mešulams, Abija, Mejamins,
8 Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
Maāzgus, Bilgajus, Šemaja: šie bija priesteri.
9 Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
Un leviti: Ješuūs, Azanijas dēls, Binujus no EnHadada bērniem, Kadmiēls,
10 ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
Un viņu brāļi Šebanija, Hodija, Kelitus, Pelaja, Hanans,
11 Mika, Rehobu, Hasabiya,
Miha, Reūbs, Hašabija,
12 Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
Zakurs, Šerebija. Šebanija,
13 Hodiya, Bani ndi Beninu.
Hodija, Banus, Beninus.
14 Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
Tie ļaužu virsnieki: Pareūs, PaātMoabs, Elams, Zatus, Banus.
15 Buni, Azigadi, Bebai,
Bunus, Azgads, Bebajus.
16 Adoniya, Bigivai, Adini,
Adonija, Bigvājus, Adins,
17 Ateri, Hezekiya, Azuri,
Aters, Hizkija, Azurs,
18 Hodiya, Hasumu, Bezayi
Hodija, Hašums, Becajus,
19 Harifu, Anatoti, Nebayi,
Harips, Anatots, Nebajus,
20 Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
Magpijas, Mešulams, Hezirs,
21 Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
Mešezabeēls, Cadoks, Jaduūs,
22 Pelatiya, Hanani, Ananiya,
Platija, Hanans, Anaja,
23 Hoseya, Hananiya, Hasubu
Hošeja, Hananija, Hašubs,
24 Halohesi, Piliha, Sobeki,
Haloūs, Pilka, Šobeks,
25 Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
Rehums, Hašabnus, Maāseja.
26 Ahiya, Hanani, Anani,
Un Ahija, Hanans, Anans,
27 Maluki, Harimu ndi Baana.
Maluks, Harims, Baēnus.
28 Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
Un tie citi ļaudis, priesteri, leviti, vārtu sargi, dziedātāji, Dieva nama kalpotāji un visi, kas bija atšķīrušies no tiem pagāniem tanīs zemēs uz Dieva bauslības pusi, viņu dēli un viņu meitas, visi prātīgie un mācītie ļaudis,
29 tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
Šie turējās pie saviem brāļiem, tiem virsniekiem, un svēti apsolījās un zvērēja, staigāt Dieva bauslībā, kas caur Mozu, Dieva kalpu, dota, un turēt un darīt Tā Kunga, mūsu Dieva, baušļus un Viņa tiesas un Viņa likumus.
30 “Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
Un ka mēs negribam dot savas meitas tiem zemes ļaudīm, nedz ņemt viņu meitas saviem dēliem.
31 “Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
Un kad tie zemes ļaudis preces un visādu labību atvedīs svētā dienā pārdot, ka mēs no tiem negribam ņemt svētā dienā vai kādos citos svētkos, un ka mēs septīto gadu gribam turēt par vaļas gadu un atlaist visādu nastu.
32 “Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
Un tad mēs iecēlām sev bausli, ka ik gadus gribam dot viena sēķeļa trešo daļu sava Dieva nama kalpošanai,
33 Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
Tām priekšliekamām maizēm un tam nemitējamam ēdamam upurim un tam nemitējamam dedzināmam upurim svētdienās, jaunos mēnešos un svētkos, tām svētām dāvanām un tiem grēku upuriem, Israēli salīdzināt, un visiem darbiem mūsu Dieva namā.
34 “Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
Un mēs, priesteri, leviti un tie ļaudis metām meslus par malkas došanu, kas bija pievedama pie mūsu Dieva nama, pēc mūsu tēvu namiem ik gadus savā laikā, dedzināt uz Tā Kunga, mūsu Dieva, altāra, kā tas bauslībā rakstīts;
35 “Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
Un ka arī savas zemes pirmajus un visu augļu pirmajus no visādiem kokiem gribam ik gadus nest uz Tā Kunga namu,
36 “Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
Un savus pirmdzimušos dēlus un lopus, tā kā tas bauslībā rakstīts; un ka mēs savus pirmdzimušos vēršus un sīkos lopus gribam novest uz sava Dieva namu tiem priesteriem, kas mūsu Dieva namā kalpo;
37 “Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
Un ka tos pirmajus no savas mīklas un no saviem cilājamiem upuriem un visādu koku augļus, vīnu un eļļu gribam nest tiem priesteriem sava Dieva nama kambaros, un desmito tiesu no savas zemes tiem levitiem, un ka šie leviti to desmito tiesu dabū visās pilsētās, kur zemi kopjam.
38 Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
Un ka priesterim no Ārona bērniem būs būt pie tiem levitiem, kad leviti to desmito tiesu dabū, un levitiem būs to desmito tiesu no (saviem) desmitiem nest augšām mūsu Dieva nama mantu kambaros.
39 Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”
Jo Israēla bērniem un Levja bērniem cilājamo upuri, labību, vīnu un eļļu būs nest tanīs kambaros, kur arī svētās vietas trauki ir un tie priesteri, kas tur kalpo, un vārtu sargi un dziedātāji, ka mēs sava Dieva nama neatstājam.

< Nehemiya 10 >