< Mateyu 27 >

1 Mmamawa, akulu a ansembe onse ndi akuluakulu anavomerezana kuti aphe Yesu.
Omwanya gwa katondo gwejile gwakinga, abhakulu bhone bha bhagabhisi na abhakaluka bha bhanu nibhalwajila ebhya Yesu bhabhone okumwita.
2 Anamumanga, napita naye kukamupereka kwa bwanamkubwa Pilato.
Nibhamubhoya, nibhamutangasha, na ni bhamukingya kwa liwali Pilato.
3 Yudasi, amene anamupereka Iye, ataona kuti Yesu waweruzidwa kuti akaphedwe, anatsutsika mu mtima mwake nakabweza ndalama zamasiliva makumi atatu zija kwa akulu a ansembe ndi kwa akuluakulu.
Mbe omwanya Yuda unu aliga amulomee iniku, ajile alola ati Yesu amalile kulamulwa, nanega no kusubhya ebhibhutu makumi gasatu ebhya jiela ku mukulu wa abhagabhisi na abhakaluka,
4 Iye anati, “Ndachimwa pakuti ndapereka munthu wosalakwa.” Iwo anayankha nati, “Ife tilibe nazo kanthu izo ndi zako.”
na naika ati, “Nakola echibhibhi kwo kulomela iniku amanyiga ganu gatali na chikayo.” Nawe nibhamusubhya ati, ejichigasa chinuki eswe? Nugalole ago awe omwene.”
5 Pamenepo Yudasi anaponya ndalamazo mʼNyumba ya Mulungu nachoka. Kenaka anapita nakadzimangirira.
Mbe niwo nabhyesa ansi bhiliya ebhibhutu bhya jiela muyekalu nagenda jae no kwinyiga omwene.
6 Akulu a ansembe anatola ndalamazo nati, “Sikololedwa ndi lamulo kuti ndalamazi tiziyike mosungira chuma cha Mulungu, popeza ndi ndalama za magazi.”
Omukulu wa bhagabhisi abhigegele bhilia ebhibhutu bhya jiyela naikati,” jiteile okutula jiyela jinu bhwikilo, kulwokubha nibhugusi bhwa manyinga!
7 Choncho anagwirizana kuti ndalamazo azigwiritse ntchito pogulira munda wa wowumba mbiya kuti ukhale manda alendo.
Nibhalwajila amwi na jiyela nijikola okugulila lisambu lyo mumogi elyokusikamo abhagenyi.
8 Ndi chifukwa chake umatchedwa munda wamagazi mpaka lero lino.
ijuno inu nikwo elibha nilitogwa, “lisambu lyamanyinga” okukinga lelo linu.
9 Pamenepo zimene anayankhula mneneri Yeremiya zinakwaniritsidwa kuti, “Anatenga ndalama zamasiliva makumi atatu mtengo umene anamuyikira Iye anthu a Israeli.
Mbenio ligambo Lilia lyaliga lyaikilwe no mulagi Yelemia lyakumie, okwaikati, “Bhagegele ebhibhutu makumi gasatu ebhya jiyela, obhugusi bhunu bhwalomelwe na bhanu Bhaisiraeli kumwene,
10 Ndipo anazigwiritsa ntchito kugula munda wa wowumba mbiya monga mmene Ambuye anandilamulira ine.”
Nibhakolela kwisambu lyo mumogi, lwa kutyo Latabhugenyi aliga andagilie.”
11 Pa nthawi yomweyo Yesu anayimirira pamaso pa bwanamkubwa ndipo bwanamkubwayo anamufunsa Iye kuti, “Kodi ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Koma Yesu anayankha kuti, “Mwanena ndinu.”
Oli Yesu emeleguyu imbele ya liwali, na liwali namubhusha ati, angu awe nawe Omukama wa bhayaudi? “Yesu amusubhishe ati,”nawe owaika kutyo,”
12 Pamene akulu a ansembe ndi akuluakulu ankamuneneza, sanayankhe kanthu.
Nawe omwanya ogwo asitakibhwe na bhakulu bha bhagabhisi na bhakulu, atasubhishe chona chona.
13 Kenaka Pilato anamufunsa Iye kuti, “Kodi sukumva zinthu zimene akukunenerazi?”
Mbe nio Pilato namubhila ati uchalikungwa amasitako gone kwawe?”
14 Koma Yesu sanayankhe ngakhale mawu amodzi mpaka bwanamkubwa anadabwa kwambiri.
Nawe atamusubhishe nolwo musango gumwi, ndijei Liwali nejulwa nechilugulo.
15 Pa nthawiyi chinali chizolowezi cha bwanamkubwa kuti pachikondwerero cha Paska amamasula wamʼndende wosankhidwa ndi anthu.
Nawe musiku ja musikuku yaliga ili tungwa ya Liwali okusulumula umwi unu kasolwa na liijo.
16 Pa nthawiyo anali ndi wamʼndende woyipa kwambiri dzina lake Baraba.
Omwanya ogwo bhaliga no mubhoywa mukumuke lisina lyae Balaba.
17 Gulu la anthu litasonkhana, Pilato anawafunsa kuti, “Ndi ndani amene mufuna kuti ndikumasulireni; Baraba kapena Yesu wotchedwa Khristu?”
Kutyo omwanya ogwo bhaliga bhwekofyanyishe amwi, Pilato abhasubhishe ati, “Niuya omwenda chibhasulumulile kulwemwe?” Baraba angu Yesu unu katogwa Kristo?”
18 Pakuti anadziwa kuti anamupereka Yesu chifukwa cha kaduka.
Okubha amenyele ati bhamalile okumugwatila lwiso.
19 Pamene Pilato anakhala pa mpando woweruza, mkazi wake anamutumizira uthenga uwu, “Musachite kanthu ndi munthuyo, ndi wosalakwa pakuti ndavutika kwambiri lero mʼmaloto chifukwa cha munthuyo.”
Omwanya aliga achenyanjile kuchitebhe chae echo kulamulila, omugasi wae amutumie musango naikati wasiga kukola musango gwone gwone ku munu oyo atali na chikayo okubha nanyasibhwa muno nolwo lelo muchiloto kubhwae.”
20 Koma akulu a ansembe ndi akuluakulu ananyengerera gulu la anthu kuti apemphe Baraba ndi kuti Yesu aphedwe.
Mbe nio abhakulu bha bhagabhisi na bhakaluka nibhabhakongya kongya liijo bhamusabhwe Baraba, na Yesu afwe.
21 Bwanamkubwayo anafunsa kuti, “Ndi ndani mwa awiriwa amene mufuna ine ndikumasulireni?” Iwo anayankha kuti, “Baraba.”
Liwali abhabhusishe ati,” Ni uya omwenda nibhasulumulile kwimwe bhaikile ati,”Baraba.”
22 Pilato anafunsa kuti, “Nanga ndichite chiyani ndi Yesu wotchedwa Khristu?” Onse anayankha kuti “Mpachikeni!”
Pilato nabhabhwila ati kambe nimukolele chinuki Yesu unu katogwa Kristo? Bhone nibhasubya ati,” abhambwe”
23 Pilato anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani? Wachita choyipa chotani?” Koma anachita phokoso nafuwula kwambiri kuti, “Mpachikeni!”
Omwene naika ati, “kubhaki nichikayoki akolele? “Nawe nibeyongesha kusekana obhulaka bhwa ingulu muno, “Abhambwe.”
24 Pilato ataona kuti samaphulapo kanthu, koma mʼmalo mwake chiwawa chimayambika, anatenga madzi nasamba mʼmanja mwake pamaso pa gulu la anthu. Iye anati “Ine ndilibe chifukwa ndi magazi a munthu uyu, ndipo uwu ndi udindo wanu!”
Kutyo omwanya Pilato ejile alola ati, atakutila okukola lyone lyone, nawe obhusambe bwaliga bwambile, agegele amanji nesabha amabhoko gae imbele ya liijo, naika ati, “Anye nitana chikayo ingulu ya manyinga go munu unu atali na chikayo. Mugalole emwe abhwene.”
25 Anthu onse anayankha nati, “Magazi ake akhale pa ife ndi pa ana athu!”
Abhanu bhone nibhaikana ati, “Amanyinga Gaye gabhe ingilu yeswe na bhana bhweswe.”
26 Pamenepo anawamasulira Baraba koma analamula kuti Yesu akakwapulidwe, ndipo anamupereka kuti akapachikidwe.
Nio nabhasulumulila Baraba kwebhwe, nawe amubhumile emijaledi Yesu namukabhiji kwebhwe okuja okumubhamba.
27 Pamenepo asilikali abwanamkubwayo anamutenga nalowa naye ku bwalo la milandu ndipo anasonkhanitsa gulu lonse la asilikali namuzungulira Iye.
Mbe nio abhasilikale abhaliwali nibhamugega Yesu mpaka Praitorio na eiijo lyafu lya bhasilikale bhone nibhamwikofyanyishako.
28 Anamuvula malaya ake namuveka Iye malaya ofiira aufumu.
Nibhamufula emyenda jae nibhamufwafya ikanju ya ilangi imutuku.
29 Ndipo kenaka analuka chipewa chaminga nachiyika pa mutu pake. Anamugwiritsa ndodo mʼdzanja lake lamanja nagwada pamaso pake namuchitira chipongwe nati, “Tikulonjereni Mfumu ya Ayuda.”
Mbe nibhaluka olutenga lwamawa no kuitulila ingulu yo mutwe gwae, na nibhamutulilao lisekeyanda mukubhoko kwae okwebhulyo. Nibhafukama imbele yae nibhamujimya, nibhaika ati, “kasige omukama wa bhayaudi?”
30 Anamuthira malovu ndipo anatenga ndodo namumenya nayo pa mutu mobwerezabwereza.
Na nibhamufubhulila amachwata, na nibhagega lisekeyanda na nibhamubhumila mumutwe.
31 Atamaliza kumuchitira chipongwe, anamuvula malaya aja namuveka malaya ake aja napita naye kokamupachika.
Omwanya gunu bhaliga nibhamujimya, bhamufulile ikanju iliya nibhamufwafya emyenda jae nibhamutagasha okugenda okumubhamba.
32 Pamene gululi linkatuluka ndi Yesu, anakumana ndi munthu wochokera ku Kurene dzina lake Simoni ndipo anamuwumiriza kunyamula mtanda.
Anu bhaliga bhachauluka anja. Nibhamulola omunu okusoka Krene lisina lyae Simoni, oyo nibhamunyasha okugenda nabho koleleki abhone okugega omusalabha gwae.
33 Anafika ku malo wotchedwa Gologota amene atanthauza kuti malo a bade la mutu.
Bhwejile bhakinga anu atogwaga goligota, isonga yacho, olubhala lwo lwanga lwo mutwe.”
34 Pamenepo anamupatsa vinyo wosakaniza ndi ndulu kuti amwe; koma atalawa anakana kumwa.
Nibhamuyana isiki isasibhwemo na idulu anywe.
35 Atamupachika Iye, anagawana zovala zake pochita maere.
Omwanya nibhamala okumubhamba, bagabhene emyenda jae kwo kubhuma ikula.
36 Ndipo anakhala pansi namulonda Iye.
Na nibhwenyaja nibhamulolela.
37 Pamwamba pa mutu wake analembapo mawu osonyeza mlandu wake akuti, “uyu ndi yesu, mfumu ya ayuda.”
Ingulu yo mutwe gwae bhateyeo intambala yae inu yaliga yandikilwe ati unu ni Yesu omukama wa Bhayaudi.”
38 Achifwamba awiri anapachikidwa pamodzi ndi Iye, mmodzi kudzanja lamanja wina kudzanja lamanzere.
Abhasakusi bhabhili bhabhambilwe amwi nage, oumwi olubhala lwebhulyo lyae no undi kubhwebhumosi.
39 Ndipo amene amadutsa anamunenera mawu a chipongwe, akupukusa mitu yawo.
Abhanu bhaliga nibhaiting'ana nibhamufuma nibhasingishaha emitwe jebhwe.
40 Ndipo anati, “Iwe amene ungapasule Nyumba ya Mulungu ndi kuyimanga masiku atatu, dzipulumutse wekha! Tsika pa mtandapo ngati ndiwe Mwana wa Mulungu!”
Nibhaika ati,” awe unu wendaga okufumya iyekalu na nuyumbaka musiku esatu, nuwikishe omwene! Alabha uli mwana wa Nyamuanga, ikaansi usoke kumusalabha!”
41 Chimodzimodzinso akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anamuchitira chipongwe.
Nyabhuliko one abhakulu abhabhagabhisi bhaliga Ni bhamugombelesha amwi na bhandiki na bhakaluka nibhaika ati,
42 Iwo anati, “Anapulumutsa ena koma sangathe kudzipulumutsa yekha! Ndi mfumu ya Israeli! Mulekeni atsike pa mtanda ndipo tidzamukhulupirira Iye.
Akishaga abhandi, nawe atakutula okwikisha omwenene. Omwene ni mukama wa Bhayaudi. Natuke ansi okusoka kumusalabha, nio jechimwikilishe.
43 Amadalira Mulungu, mulekeni Mulunguyo amupulumutse tsopano ngati akumufuna pakuti anati, ‘Ndine Mwana wa Mulungu.’”
Eikanyishe Nyamuanga siga Nyamuanga amukishe olyanu labha Kenda, okubha aikile ati,' Anye nili mwana wa Nyamuanga.”
44 Momwemonso mbala zimene zinapachikidwa naye pamodzi zinamuneneranso zachipongwe.
Na bhalia abhasakusi abho bhaliga babhambilwe amwi nage one bhaikile emisango jokumufuma.
45 Kuyambira 12 koloko masana mpaka 3 koloko, kunachita mdima pa dziko lonse.
Oli kusoka saa mukaga chabheyeo echisute kuchalo chone okukinga saa mwenda.
46 Ndipo nthawi ili ngati 3 koloko, Yesu analira mofuwula nati, “Eloi, Eloi, lama sabakitani!” Kutanthauza kuti, “Mulungu Wanga, Mulungu Wanga, mwandisiyiranji Ine?”
Yejile yakinga saa mwenda Yesu nalila kwo bhulaka bhwa ingulu, “Eloi, Eloi lama Saba kitani?” Isonga ati, “Nyamuanga wani, Nyamuanga wani. Ni kulwaki wasiga?”
47 Ena a oyimirira pamalopo atamva izi anati, “Akuyitana Eliya.”
Omwanya ogwo abhandi bhabhili bhanu bhaliga bhemeleguyu ao bhoguywe, nibhaika ati kabhilikila Eliya.”
48 Mmodzi wa iwo anathamanga natenga chinkhupule. Anachidzaza ndi vinyo wosasa, nachizika ku mtengo namupatsa Yesu kuti amwe.
Ao nao oumwi wabho abhilimile nagega isifongo naijusha ebhyokunywa bhilulu, naitula ingulu ya liti namuyana abhone okunywa.
49 Koma ena onse anati, “Mulekeni tiyeni tione ngati Eliyayo abwere kudzamupulutsa.”
Ka bhanu bhasigae nibhaika ati mumusige enyele ela musige chilole labha Eliya kaja okumukisha.”
50 Ndipo pamene Yesu analiranso mofuwula, anapereka mzimu wake.
Mbe nio Yesu nalila lindi kwo bhulaka bhunene nasosha omwoyo gwae.
51 Pa nthawi imeneyo chinsalu chotchinga cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati kuyambira pamwamba mpaka pansi. Dziko linagwedezeka ndipo miyala inangʼambika.
Lola, lipajia lya iyekalu lyatikilemo mabhala gabhili okusokelela ingulu kukinga emwalo. Na Insi niyalala na amatale nigatika bhibhala.
52 Manda anatsekuka ndipo mitembo yambiri ya anthu oyera mtima amene anafa inaukitsidwa.
Jifwa nijiguka, ne mibhili eja bhelu bhafu bhanu bhaliga bhamamile jitilo nibhasululwa.
53 Anatuluka mʼmanda mwawo, ndipo chitachitika chiukitso cha Yesu, anapita mu mzinda woyera naonekera kwa anthu ambiri.
Bhasokele munfwa kwo kumala okusuluka kwae, bhengie mumusi omwelu na bhabhonekene bhafu.
54 Mkulu wa asilikali ndi amene ankalondera Yesu ataona chivomerezi ndi zonse zinachitika, anachita mantha, ndipo anati, “Zoonadi, uyu anali Mwana wa Mulungu!”
Nawe uliya Akida na bhalia abho bhaliga nibhamulola Yesu bhalolele echiyalalo namamagambo ganu gabhonekene, bhejuwe no bhubha muno nibhaikana ati, “Nichimali unu ali Mwana wa Nyamuanga.”
55 Amayi ambirimbiri amene ankasamalira Yesu ankaonerera ali patali. Iwo anamutsatira Yesu kuchokera ku Galileya.
Abhagasi bhafu bhanu bhaliga nibhamulubhilisha Yesu okusoka Galilaya bhanu bhamufulubhendelaga bhaliga bhalio aliya nibhalolaga okusoka kula.
56 Pakati pawo panali Mariya wa ku Magadala, Mariya amayi ake Yakobo ndi Yosefe ndi amayi a ana a Zebedayo.
Mwabho aliga alimo Mariamu Magdarena, Mariamu nyilamwene Yakobho na Josefu na nyilamwene abhana bha Jebhedayo.
57 Pamene kumada, kunabwera munthu wolemera wa ku Arimateyu dzina lake Yosefe amene anali wophunzira wa Yesu.
Yejile yakinga kegolo, ejile munu munibhi okusoka Alimataya, unu atogwaga Yusufu, unu one aliga mwiigisibhwa wa Yesu.
58 Anapita kwa Pilato kukapempha mtembo wa Yesu, ndipo Pilato analamula kuti uperekedwe kwa iye.
Agendelee ku Pilato nagusabhwa omubhili gwa Yesu. Mbe niwo Pilato nalagilila abhone okumuyana.
59 Yosefe anatenga mtembowo, nawukulunga nsalu yabafuta.
Yusufu agegele omubhili nagubhoya no mwenda gwa isufu ya kisi,
60 Ndipo anawuyika mʼmanda ake atsopano amene anasema mu thanthwe, natsekapo ndi mwala waukulu pa khomo la mandawo nachokapo.
na nagumamya munfwa inyaya ya inu aliga asimbile kulutale, niwo nasilingisha libhui enene niliswikila omulyango gwa infwa nagenda jae.
61 Mariya wa Magadala ndi Mariya wina anakhala pansi moyangʼanizana ndi mandawo.
Mariamu magdarena na Mariamu oundi bhaliga bhalio alia bhenyanjile bhasomekene na infwa.
62 Litapita tsiku lokonzekera Sabata, mmawa mwake, akulu a ansembe ndi Afarisi anapita kwa Pilato.
Olusiku olwo lwalubhie olwo lwaliga lusiku olwo kwilabha, abhakulu bha bhagabhisi na abhafarisayo nibhekofyanyisha amwi ewa pilato.
63 Iwo anati, “Bwana takumbukira kuti munthu wonyenga uja akanali ndi moyo anati, ‘Pakatha masiku atatu ndidzauka.’
Nibhamubhwila ati, “Mukulu echijuka ati omwanya gulia omubhei aliga achali muanga, aikile ati, alibha jatulao nsiku esatu ndisuka lindi.'
64 Choncho lamulirani kuti manda ake atetezedwe mpaka pa tsiku lachitatu. Chifukwa tikapanda kutero, ophunzira ake angabwere kudzaba mtembo wake ndipo angawuze anthu kuti waukitsidwa kwa akufa. Ndipo chinyengo chomalizachi chidzakhala choyipa kwambiri kusiyana ndi choyamba chija.”
Mbe kulwejo lagilila ati infwa ilindwe kata kukinga ku lusiku lwa kasatu. Bhindi nebyo, abheigisibhwa bhae abhatula okuja okumwibha na nibhaikana ku bhanu, 'Asulukile okusoka mu bhafuye' na okubheya kwa kubhutelo obhubha bhubhibhi okukila bhulia obho kwamba.”
65 Pilato anayankha kuti, “Tengani mlonda kalondereni monga mudziwira.”
Pilato nabhabhwila ati, “Mugege abhalisi. Mugende mukole iyali yo mulembe lwa kutyo omutula.
66 Tsono anapita nakatseka manda kolimba ndi kuyikapo chizindikiro ndipo anayikapo mlonda.
Kutyo bhagendele na nibhakola infwa kubha mulembe, libhui lyabhumilwe echibhalikisho no kutulako abhalisi.

< Mateyu 27 >