< Malaki 3 >

1 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga amene adzakonza njira pamaso panga. Kenaka mwadzidzidzi Ambuye amene mukumufunafuna adzafika ku Nyumba yake. Mthenga wapangano amene mukumuyembekezera adzabwera.”
Oto posyłam mego posłańca, który przygotuje drogę przed moim obliczem. I nagle przybędzie do swojej świątyni Pan, którego wy szukacie, Posłaniec przymierza, którego wy pragniecie. Oto przyjdzie, mówi PAN zastępów.
2 Koma ndani adzatha kupirira pa tsiku la kubwera kwake? Ndani adzatha kuyima pamene Iye wafika? Pakuti adzakhala ngati moto wa mmisiri wa pa ngʼanjo, kapenanso ngati sopo wa munthu wochapa.
Lecz któż będzie mógł znieść dzień jego przyjścia? I kto się ostanie, gdy on się ukaże? [Jest] bowiem jak ogień złotnika i jak mydło foluszników.
3 Iye adzachita kukhalira pansi ngati mmisiri woyenga ndi woyeretsa siliva. Iye adzayeretsa Alevi ndi kuwayenga ngati golide ndi siliva. Pamenepo Yehova adzakhala ndi anthu amene azidzabweretsa zopereka mwachilungamo,
I zasiądzie jako ten, kto roztapia i oczyszcza srebro: oczyści synów Lewiego, oczyści ich jak złoto i srebro i będą składać PANU ofiarę w sprawiedliwości.
4 ndipo Yehova adzalandira zopereka za Yuda ndi Yerusalemu, ngati masiku akale, masiku amakedzana.
Wtedy ofiara Judy i Jerozolimy będzie miła PANU, jak za dawnych dni i jak za lat minionych.
5 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Tsono ndidzakuyandikirani kuti ndikuweruzeni. Mosataya nthawi ndidzanena mawu otsutsa mfiti, achigololo, a umboni wonama, amene salipira bwino antchito awo, amene amazunza akazi ndi ana amasiye, amene saweruza alendo mwachilungamo, komanso amene sandiopa Ine.”
I zbliżę się do was na sąd, i będę rychłym świadkiem przeciwko czarownikom, przeciwko cudzołożnikom, przeciwko krzywoprzysięzcom, przeciwko tym, którzy uciskają najemników przy ich zapłatach oraz wdowy i sieroty i krzywdzą cudzoziemca, a nie boją się mnie, mówi PAN zastępów.
6 “Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe.
Gdyż ja, PAN, nie zmieniam się, dlatego wy, synowie Jakuba, nie zostaliście zniszczeni.
7 Kuyambira nthawi ya makolo anu mwakhala mukuphwanya malamulo anga ndipo simunawatsatire. Bwererani kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Tibwerere motani kwa Yehova?’
Od dni waszych ojców odstępowaliście od moich ustaw i nie przestrzegaliście [ich]. Zawróćcie do mnie, a ja zawrócę do was, mówi PAN zastępów. Ale wy mówicie: Pod jakim względem mamy zawrócić?
8 “Kodi munthu angathe kuba za Mulungu? Komatu inu mumandibera. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi timakuberani motani?’ “Pa zakhumi ndi pa zopereka.
Czy człowiek okradnie Boga? Wy jednak mnie okradacie. Lecz mówicie: Z czego cię okradamy? Z dziesięcin i ofiar.
9 Mtundu wanu wonse ndinu otembereredwa, chifukwa mukundibera.
Jesteście zupełnie przeklęci, ponieważ mnie okradacie, wy [i] cały wasz naród.
10 Bweretsani chakhumi chathunthu ku nyumba yosungira, kuti mukhale chakudya mʼnyumba mwanga.” Akutero Yehova Wamphamvuzonse, “Tandiyesani, ndipo muone ngati sindidzatsekula zipata zakumwamba, ndi kukugwetserani madalitso ochuluka amene mudzasowe malo owayikamo.
Przynieście całą dziesięcinę do spichlerza, aby żywność była w moim domu, a doświadczcie mnie teraz w tym, mówi PAN zastępów, czy wam nie otworzę okien niebios i nie wyleję na was błogosławieństwa, tak że nie będziecie mieli gdzie go podziać;
11 Ndidzaletsa tizirombo kuti tisawononge mbewu zanu, ndipo mpesa wa mʼminda mwanu zipatso zake sizidzayoyoka,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
I zgromię ze względu na was tego, który pożera, a nie popsuje wam plonu ziemi i winorośl nie będzie pozbawiona owocu na polu, mówi PAN zastępów.
12 “Motero anthu amitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
I wszystkie narody będą was nazywać błogosławionymi, bo będziecie ziemią rozkoszną, mówi PAN zastępów.
13 Yehova akuti, “Mwayankhula mawu owawa onena za Ine. “Komabe inu mukufunsa kuti, ‘Kodi tanena chiyani chotsutsana nanu?’
Zuchwałe są wasze słowa przeciwko mnie, mówi PAN. Wy jednak mówicie: Cóż powiedzieliśmy przeciwko tobie?
14 “Mwanena kuti, ‘Kutumikira Mulungu nʼkosapindulitsa. Kodi timapindulanji pochita zofuna zake, ndi kumayenda ngati anamfedwa pamaso pa Yehova Wamphamvuzonse?
Mówiliście: Na próżno służyć Bogu. Co za pożytek z tego, że przestrzegaliśmy jego przykazań i chodziliśmy smutni przed PANEM zastępów?
15 Koma tsono ife timati anthu odzikuza ndiye odalitsika. Kunena zoona anthu oyipa ndiye amapeza bwino, ngakhale amene amanyoza Mulungu amapulumuka.’”
A teraz pysznych mamy za błogosławionych, ponieważ ci się budują, którzy czynią niegodziwość, a ci, którzy kuszą Boga, są wybawieni.
16 Ndipo woopa Yehova anayamba kukambirana, ndipo Yehova anamvetsera. Buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, lonena za amene amaopa Yehova ndi kulemekeza dzina lake.
Wtedy rozmawiali [o tym] między sobą ci, którzy się bali PANA. PAN zobaczył [to] i usłyszał, i napisano księgę wspomnień przed nim [z powodu] tych, którzy się boją PANA i rozmyślają o jego imieniu.
17 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu amenewo adzakhala anga, tsiku limene Ine ndidzachita izi, adzakhala angaanga. Ndidzawaleka osawalanga monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira.
Oni będą moimi, mówi PAN zastępów, w dniu, kiedy uczynię ich moją własnością. Zlituję się nad nimi, jak się lituje ojciec nad swoim synem, który mu służy.
18 Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.”
Wtedy zawrócicie i zobaczycie różnicę między sprawiedliwym i bezbożnym, między tym, który służy Bogu, [i] tym, który mu nie służy.

< Malaki 3 >