< Luka 6 >

1 Tsiku lina la Sabata Yesu ankadutsa mʼminda yatirigu, ndipo ophunzira ake anayamba kubudula ngala zatirigu, namazifikisa mʼmanja mwawo ndi kumadya.
chikwachitahala kuti ivali lwe Nsabata, mi Jesu avali kuhita muluwa lwa buheke, mi balutiwa vakwe vavali kwa vutola mitwi ya vuheke ni kulya vuheke.
2 Ena mwa Afarisi anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mukuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata?”
Mi vamwi vava Falisi chivawamba kuti. “Chinzi ho chita chisa swaneli kuchitwa luzuva lwe nsavata?”
3 Yesu anawayankha iwo kuti, “Kodi simunawerenge zimene Davide anachita pamene iye ndi anzake anali ndi njala?
Cha kumwitava, Jesu chetava kuti, “kena muvavali chava chiti Davida ha va fwile inzala, iye ni vakwame vavena navo?
4 Iye analowa mʼnyumba ya Mulungu ndipo atatenga buledi wopatulika anadya amene ndi ololedwa kudya ansembe okha. Ndipo anaperekanso wina kwa anzake.”
avayendi mwi nzuvo ye Ireza, avahindi inkonko ivavikitwe muchivaka che Ireza, ni kulya imwi mwateni, nikuhinda imwi chikuha kwateni mane nivavali kwina naye kuti valye kwateni, nihakuva vulyo zivali kuswanelwa kuliwa va Purisita ka mulao”,
5 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Mwana wa Munthu ndi Ambuye wa Sabata.”
Chata kuti mwana muntu simwine mane ni wale Nsavata.
6 La Sabata lina Iye analowa mʼsunagoge kukaphunzitsa ndipo mʼmenemo anapeza munthu wadzanja lolumala.
chikwa chitahala kuti lwensavata lumwi cheza mu ma Sinagoge nikuka luta vantu mwateni, Mukwame mwavali kwina mwateni yavali kwina iyanza lyakwe lyachilyo livanyonyovete.
7 Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo ankamuyangʼana kuti apeze chifukwa Yesu, choncho anamuyangʼanitsitsa kuti aone ngati Iye akanamuchiritsa pa Sabata.
Va ñoli niva Falisi vavali kumulolete chentokomelo kuvona kapa mwahoze muntu lwensavata, kuchitila kuti vawane vushupi bwakumu sumina indava.
8 Koma Yesu anadziwa zimene ankaganiza ndipo anati kwa munthu wadzanja lolumalayo, “Tanyamuka ndipo uyime patsogolo pa onsewa.” Choncho iye ananyamuka nayima pamenepo.
Avezivi zivavali kuhupula, mi chata mukwame yavena iyanza linyonyovele, “Zimane wize aha vakuvone vantu vonse,” Mi mukwame cha zimana haho.
9 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Ndikufunseni, kodi chololedwa pa Sabata ndi chiti: kuchita chabwino kapena kuchita choyipa, kupulumutsa moyo kapena kuwononga?”
Jesu cha wamba, “nimivuza, kana kuzumininwe kuchita vulotu kapa siya zintu lwe Nsavata? Ku chita vuhalo kapa kuvusiya.
10 Iye atawayangʼana onsewo, anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye anaterodi, ndipo dzanja lake linachiritsidwa.
Linu chava lola vonse niku wamba kuyo lwala, “Wolole iyanza lyako” chachita vulyo mi iyanza lyakwe chilya va hande.
11 Koma iwo anapsa mtima nayamba kukambirana wina ndi mnzake chomwe akanamuchitira Yesu.
Kono vavezwile kuvenge mane chivatanga kuli wambila mwete vachitile kaha Jesu.
12 Tsiku lina, masiku amenewo, Yesu anapita ku phiri kukapemphera ndipo anakhala usiku wonse akupemphera kwa Mulungu.
Chikwachitahala kuti mwao mazuva cha yenda kuma lundu nikuka lapela. cha zwila havusu niku lapepa masiku onse kwe Ireza. Haiva
13 Kutacha, anayitana ophunzira ake ndipo anasankha khumi ndi awiri a iwo amene anawayika kukhala atumwi:
musihali, cha sumpa valutiwa vakwe, nikuketa vena makumi nivi vele, vava sumpi va Apostola.
14 Simoni (amene anamutcha Petro), mʼbale wake wa Andreya, Yakobo, Yohane, Filipo, Bartumeyu,
Mazina ava Apositola ivali nji Simon (wava sumpi Pitorosi), ni mwance, Andulu, Jakovo ni Johani, Filipi, Bartholome,
15 Mateyu, Tomasi, Yakobo mwana wa Alufeyo, Simoni amene amatchedwa Zaleti,
Mateu, Tomasi, Jakovo mwana wa Alufeya, Simone yavali kusupwa Zealote,
16 Yudasi mwana wa Yakobo ndi Yudasi Isikarioti amene anamupereka.
Judas mwana Jacobo, Ni Judasi Isikariyote, yava vi muveteki.
17 Iye anatsika pamodzi ndi atumwiwo ndipo anayima pamalo athyathyathya. Gulu lalikulu la ophunzira ake, gulu lalikulu la anthu ochokera ku Yudeya konse, ku Yerusalemu ndi ochokera mʼmphepete mwa nyanja ya Turo ndi Sidoni anali pomwepo.
Linu Jesu chakav0la navo kuzwa he lundu navo, cheza kuzimana ha pateme ni chikwata cha valuti vakwe ni vantu vangi vavali kuzwila kwa Judeya, ni Jerusalema ni Tire ni Sidoni.
18 Iwo anabwera kudzamvetsera ndi kuchiritsidwa ku matenda awo. Osautsidwa ndi mizimu yoyipa anachiritsidwa,
Vavakezi kwiza kuteka kwali ni kwiza kuhozwa matuku avo onse. Vantu vavali kukatazwa luhuho luvi vava hozwa navo.
19 ndipo anthu ankayesetsa kuti amukhudze chifukwa mphamvu imatuluka mwa Iye ndi kuchiritsa onse.
Vantu vonse vavena muchisi vava kulika kumu kwata kakuti ziho zakuhoza zivali kuzwa kwali, mi avava hozi vonse.
20 Akuyangʼana ophunzira ake, Iye anati, “Odala ndinu amene ndi osauka, chifukwa ufumu wa Mulungu ndi wanu.
Chalola kuva lutiwa vakwe, nikuti, mwina imbuyoti inwe musena chenu, kakuti chenu muvuso wa kwi wilu we Ireza.
21 Inu amene mukumva njala tsopano, ndinu odala chifukwa mudzakhutitsidwa. Inu amene mukulira tsopano, ndinu odala chifukwa mudzasekerera.
Imbuyoti njiyenu mufwa inzala hanu, kakuti kamwi kutiswe. mufuyaulitwe inwe mulila hanu kakuti kamu seke.
22 Ndinu odala, anthu akamakudani, kukusalani ndi kukunyozani ndi kumayipitsa dzina lanu chifukwa cha Mwana wa Munthu.
mwina imbuyoti vantu hava mi toya, havasamivali ni kumi tukola, chevaka lya mwana a muntu.
23 “Nthawi imeneyo sangalalani ndipo lumphani ndi chimwemwe chifukwa mphotho yanu ndi yayikulu kumwamba. Pakuti ndi zomwezonso zimene makolo awo anachitira aneneri.
Mutabe mwelina izuva mi mulotoke che ntavo. Kakuti kamuve ni mupuzo mukando mwi wulu. Kakuti vakukwavo muvava chitili va Polofita vamwi mwinzila iswana.
24 “Ndinu atsoka, anthu olemera, popeza mwalandiriratu zokusangalatsani.
Kono woo kwenu mufumite, kakuti chiva tambuli inkavelo yenu.
25 Tsoka inu amene mukudya bwino tsopano, chifukwa mudzakhala ndi njala. Ndinu atsoka, amene mukusekerera tsopano, chifukwa mudzabuma ndi kulira.
Woo kwenu mwi kusi hanu kakuti kamu fwenzala mazuva akeza. Woo kwenu museka hanu, kakuti kamulile ni kuswava kuvusu.
26 Ndinu atsoka, anthu akamakuyamikirani, popeza makolo anu anawachitira aneneri onama zomwezi.”
woo kwenu vantu hava mitemba, kakuti muvava chitili kuva Polofita va mapa.
27 “Koma Ine ndikuwuza inu amene mukundimva: Kondani adani anu, chitirani zabwino amene amakudani.
Kono niwamba kwenu mutekeleze, musake zila zenu mane muchite hande vami toyete.
28 Dalitsani amene amakutembererani, apempherereni amene amakusautsani.
mufuyole vami kuta mi mufuyole vaminyandisa.
29 Ngati wina akumenyani patsaya limodzi mupatseninso tsaya linalo. Ngati wina akulanda mwinjiro wako, umulole atenge ndi mkanjo omwe.
Yokuwopa kulimi tama, mumu he ni limwi a wope kwateni. Haiva zumwi nahinda chi Jansi chako, muhe ni vulukwe.
30 Mupatseni aliyense amene akupemphani kanthu ndipo ngati wina atenga chinthu chanu, musamulamule kuti akubwezereni.
He kuvonse vakumbila. haiva zumwi nahinda chintu kwako, Zanzi umuwambili kuti achivize.
31 Inu muwachitire anthu ena, zomwe mukanafuna kuti iwo akuchitireni.
Mosakila kuti vantu vaku chitile, upange vulyo kuvantu.
32 “Ngati mukonda okhawo amene amakukondani, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amakonda amene amawakondanso.
Haiva usaka vulyo vakusaka, cho wana mwateni iwe chinzi. Ni vaezalivi vasaka vava
33 Ndipo ngati muchita zabwino kwa amene ndi abwino kwa inu, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amachita izi.
saka. Haiva uchita vulotu kuvaku chita hande, cho volelwa chi? esi ni va ezalivi vachita ziswana,
34 Ndipo ngati mukongoza amene mukuyembekeza kuti abweza, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amabwereketsa kwa ochimwa anzawo, ndipo amayembekezera kubwezeredwa zonse.
linu ho kalima vulyo vana vowizi kuti vawola kuku vozekeza, chovolelwa chi, niva eza livi vakolotisa va eza livi kuti vavolelwe zi swana.
35 Koma kondani adani anu, achitireni zabwino, akongozeni koma osayembekezera kulandira kanthu. Pamenepo mphotho yanu idzakhala yayikulu ndipo inu mudzakhala ana a Wammwambamwamba, chifukwa ndi wokoma mtima kwa anthu osayamika ndi oyipa.
Kono usake zila zako mi uvachite hande. Kolotise nosalindili kutambula chimwi mi mupuzo wako kauve mi kamuve mu vaana va Simwine mukandomukando kakuti iye ushiyeme kuvali tumuli niku vantu vavi.
36 Khalani achifundo, monga momwe Atate anu ali achifundo.”
Muve ni chisemo kakuti ishenu wina chisemo.
37 “Musaweruze, ndipo inu simudzaweruzidwa. Musatsutse ndipo inu simudzatsutsidwa. Khululukirani ena ndipo mudzakhululukidwa.
Sanzi u atuli, mi nawe kete u atulwe. Sanzi unyazi mi nawe kete unyaswe. Swalele, mi nawe ko swalelwe.
38 Perekani ndipo mudzapatsidwa. Adzakupatsani mʼthumba mwanu muyeso wabwino, wotsenderezeka, wokhutchumuka ndi wosefukira. Pakuti muyeso umene mumagwiritsa ntchito, ndi omwewo adzakuyeserani.”
Uhe nawe ko hewe. cha vungi luti, vukakatele, zinyungitwe hamwina, niku hasanywa, kasi tikile muchivikilo chako. kakuti vulemi votendesa, muvuseveliswe kwako.
39 Iye anawawuzanso fanizo ili, “Kodi munthu wakhungu angatsogolere munthu wakhungu mnzake? Kodi onse sadzagwera mʼdzenje?
linu chaba wambila linu ihuko. “kana muntu yasa voni uwola ku etelela zumwi yasa voni? Haiva nachita vulyo, vuvele bwavo muva wile mwi lindi. kapa kaku oleki?
40 Wophunzira sangapose mphunzitsi wake, koma yense amene waphunzitsidwa bwinobwino adzakhala ngati mphunzitsi wake.
Mulutiwa kena muku lwana ku muluti wakwe, kono zumwi ni zumwi hamana ku lutiwa chakwizula, uswana ni muluti wakwe.
41 “Kodi ndi chifukwa chiyani mumaona kachitsotso mʼdiso la mʼbale wanu ndi kusasamala mtengo uli mʼdiso mwanu?
Chinzi holola haka chiti kanini kena mulinso lya mwako, Mi kolemuhi chikando chikutoweze.
42 Kodi munganene bwanji kwa mʼbale wanu kuti, ‘Mʼbale nʼtakuchotsa kachitsotso mʼdiso mwako,’ pamene inu eni ake mukulephera kuona mtengo uli mʼdiso mwanu? Inu achiphamaso, yambani mwachotsa mtengo uli mʼdiso mwanu, ndipo kenaka mudzaona bwinobwino ndi kuchotsa kachitsotso mʼdiso la mʼbale wanu.”
U wola kw u wamba vule kwa mwako, mwangu nikuzwise chikutoweze, mi nikwina kuti iwe umwine kovonwe chikutoweze mulinso lyako. Inwe mulihele, Tange pili uzwise chikutoweze mulinso lyako, mi mo wole kuvona hande, linu njete uwole kuzwisa china mulinso lya mwako.
43 Palibe mtengo wabwino umene umabala chipatso choyipa, kapena mtengo oyipa umene umabala chipatso chabwino.
kakuti kakwina isamu ilotu livika zihantu zi volete, nandi isamu livolete kaliwoli kuvika zihantu zi lotu.
44 Mtengo uliwonse umadziwika ndi chipatso chake. Anthu sathyola nkhuyu pa mtengo waminga, kapena mphesa pa nthungwi.
Isamu ni isamu lizivahala cha zihanto lyalyo lili vika. Vantu kavawoli kukunganya ma Feiga kwi samu lya miya, kapa manjembere kuzi chachani.
45 Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zosungidwa mu mtima mwake, koma munthu oyipa amatulutsa zinthu zoyipa zosungidwa mu mtima mwake. Pakamwa pake pamayankhula zimene zadzaza mu mtima mwake.
Muntu mulotu kuzwilila kuvulotu bwa vuhumi bwina mwinkulo yakwe, uzwisa vulotu, ni muntu muvi ku zwilila ku vuhumi bwa vuvi bwina mwinkulo yakwe, uswisa sivi, kuzwilila ku vuhumi bwina mwinkulo yakwe muntu, uzwisa mwinkulo yakwe cha kaholo.
46 “Kodi nʼchifukwa chiyani munditchula kuti, ‘Ambuye, Ambuye’ koma simuchita zimene Ine ndinena?
Chinzi hamuni sumpa kuti simwine simwinwe, kono kamu mameli zini mi wambila.
47 Ine ndidzakuonetsani mmene alili munthu amene amabwera kwa Ine ndi kumva mawu anga ndi kuwachita.
Muntu ni muntu wiza kwangu ni ku zuwa manzi angu ni kua mamela. Muni mi wambile mwe kalile.
48 Iye ali ngati munthu womanga nyumba, amene anakumba mozama nayika maziko ake pa mwala. Madzi osefukira atabwera ndi mphamvu, nawomba nyumbayo koma sinagwedezeka, chifukwa anayimanga bwino.
Ukola sina muntu yo zaka inzuvo, ya va shii chaku tunga mwivu, ni kuzaka musumo we nzuvo hebwe likolete. Mi muunda haukeza, ni menzi mangi kuvuvila he mota lyenzuvo, Kono kana abai nyanganisi, kakuti iva zakwa hande.
49 Koma amene amamva mawu anga koma osawachita, akufanana ndi munthu amene anamanga nyumba yake koma yopanda maziko. Nthawi yomwe madziwo anawomba nyumbayo, inagwa ndipo inawonongekeratu.”
Kono muntu yo zuwa manzi angu kono ka amameli, ukola sina muntu yo zaka inzuvo yakwe he wulu lyevu kusena musumo. Mi menzi ha vuvila he nzuvo, chiya wa kapilpili, Mi kusinyeha kwe nzuvo kuva mani.

< Luka 6 >