< Luka 6 >

1 Tsiku lina la Sabata Yesu ankadutsa mʼminda yatirigu, ndipo ophunzira ake anayamba kubudula ngala zatirigu, namazifikisa mʼmanja mwawo ndi kumadya.
to be then in/on/among Sabbath (second-first *K) to go through it/s/he through/because of (the/this/who *k) grainfield and to pluck the/this/who disciple it/s/he and to eat the/this/who head of grain to rub the/this/who hand
2 Ena mwa Afarisi anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mukuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata?”
one then the/this/who Pharisee to say (it/s/he *k) which? to do/make: do which no be permitted (to do/make: do in/on/among *k) the/this/who Sabbath
3 Yesu anawayankha iwo kuti, “Kodi simunawerenge zimene Davide anachita pamene iye ndi anzake anali ndi njala?
and to answer to/with it/s/he to say the/this/who Jesus nor this/he/she/it to read which to do/make: do David (when *N+kO) to hunger it/s/he and the/this/who with/after it/s/he to be
4 Iye analowa mʼnyumba ya Mulungu ndipo atatenga buledi wopatulika anadya amene ndi ololedwa kudya ansembe okha. Ndipo anaperekanso wina kwa anzake.”
as/when to enter toward the/this/who house: home the/this/who God and the/this/who bread the/this/who purpose (to take *N+kO) (and *k) to eat and to give (and *k) the/this/who with/after it/s/he which no be permitted to eat if: not not alone the/this/who priest
5 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Mwana wa Munthu ndi Ambuye wa Sabata.”
and to say it/s/he (that/since: that *ko) lord: God to be (and *k) the/this/who Sabbath the/this/who son the/this/who a human
6 La Sabata lina Iye analowa mʼsunagoge kukaphunzitsa ndipo mʼmenemo anapeza munthu wadzanja lolumala.
to be then (and *k) in/on/among other Sabbath to enter it/s/he toward the/this/who synagogue and to teach and to be a human there and the/this/who hand it/s/he the/this/who right to be dried up/withered
7 Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo ankamuyangʼana kuti apeze chifukwa Yesu, choncho anamuyangʼanitsitsa kuti aone ngati Iye akanamuchiritsa pa Sabata.
(to observe *N+kO) then it/s/he the/this/who scribe and the/this/who Pharisee if in/on/among the/this/who Sabbath (to serve/heal *N+kO) in order that/to to find/meet (to accuse *N+kO) it/s/he
8 Koma Yesu anadziwa zimene ankaganiza ndipo anati kwa munthu wadzanja lolumalayo, “Tanyamuka ndipo uyime patsogolo pa onsewa.” Choncho iye ananyamuka nayima pamenepo.
it/s/he then to perceive: know the/this/who reasoning it/s/he (and *k) to say (then *no) the/this/who (man *N+kO) the/this/who dried up/withered to have/be the/this/who hand (to arise *N+kO) and to stand toward the/this/who midst (the/this/who *k) (and *N+kO) to arise to stand
9 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Ndikufunseni, kodi chololedwa pa Sabata ndi chiti: kuchita chabwino kapena kuchita choyipa, kupulumutsa moyo kapena kuwononga?”
to say (then *N+kO) the/this/who Jesus to/with it/s/he (to question *N+kO) you (if *N+kO) be permitted (the/this/who Sabbath *N+kO) to do good or to do evil/harm soul: life to save or (to destroy *NK+O)
10 Iye atawayangʼana onsewo, anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye anaterodi, ndipo dzanja lake linachiritsidwa.
and to look around all it/s/he to say (it/s/he *N+KO) to stretch out the/this/who hand you the/this/who then to do/make: do (thus(-ly) *k) and to restore the/this/who hand it/s/he (healthy *K) (as/when the/this/who another *KO)
11 Koma iwo anapsa mtima nayamba kukambirana wina ndi mnzake chomwe akanamuchitira Yesu.
it/s/he then to fill folly and to discuss to/with one another which? if to do/make: do the/this/who Jesus
12 Tsiku lina, masiku amenewo, Yesu anapita ku phiri kukapemphera ndipo anakhala usiku wonse akupemphera kwa Mulungu.
to be then in/on/among the/this/who day this/he/she/it (to go out *N+kO) (it/s/he *no) toward the/this/who mountain to pray and to be to spend the night in/on/among the/this/who prayer the/this/who God
13 Kutacha, anayitana ophunzira ake ndipo anasankha khumi ndi awiri a iwo amene anawayika kukhala atumwi:
and when to be day to call to/summon the/this/who disciple it/s/he and to select away from it/s/he twelve which and apostle to name
14 Simoni (amene anamutcha Petro), mʼbale wake wa Andreya, Yakobo, Yohane, Filipo, Bartumeyu,
Simon which and to name Peter and Andrew the/this/who brother it/s/he (and *no) James and John (and *no) Philip and Bartholomew
15 Mateyu, Tomasi, Yakobo mwana wa Alufeyo, Simoni amene amatchedwa Zaleti,
(and *no) Matthew and Thomas (and *no) James (the/this/who the/this/who *k) Alphaeus and Simon the/this/who to call: call Zealot
16 Yudasi mwana wa Yakobo ndi Yudasi Isikarioti amene anamupereka.
(and *no) Judas James and Judas Iscariot which (and *ko) to be traitor
17 Iye anatsika pamodzi ndi atumwiwo ndipo anayima pamalo athyathyathya. Gulu lalikulu la ophunzira ake, gulu lalikulu la anthu ochokera ku Yudeya konse, ku Yerusalemu ndi ochokera mʼmphepete mwa nyanja ya Turo ndi Sidoni anali pomwepo.
and to come/go down with/after it/s/he to stand upon/to/against place level and crowd (much *NO) disciple it/s/he and multitude much the/this/who a people away from all the/this/who Judea and Jerusalem and the/this/who seaside Tyre and Sidon which to come/go to hear it/s/he and to heal away from the/this/who illness it/s/he
18 Iwo anabwera kudzamvetsera ndi kuchiritsidwa ku matenda awo. Osautsidwa ndi mizimu yoyipa anachiritsidwa,
and the/this/who (to trouble away from *N+kO) spirit/breath: spirit unclean (and *k) to serve/heal
19 ndipo anthu ankayesetsa kuti amukhudze chifukwa mphamvu imatuluka mwa Iye ndi kuchiritsa onse.
and all the/this/who crowd (to seek *N+kO) to touch it/s/he that/since: since power from/with/beside it/s/he to go out and to heal all
20 Akuyangʼana ophunzira ake, Iye anati, “Odala ndinu amene ndi osauka, chifukwa ufumu wa Mulungu ndi wanu.
and it/s/he to lift up the/this/who eye it/s/he toward the/this/who disciple it/s/he to say blessed the/this/who poor that/since: since you to be the/this/who kingdom the/this/who God
21 Inu amene mukumva njala tsopano, ndinu odala chifukwa mudzakhutitsidwa. Inu amene mukulira tsopano, ndinu odala chifukwa mudzasekerera.
blessed the/this/who to hunger now that/since: since to feed blessed the/this/who to weep now that/since: since to laugh
22 Ndinu odala, anthu akamakudani, kukusalani ndi kukunyozani ndi kumayipitsa dzina lanu chifukwa cha Mwana wa Munthu.
blessed to be when(-ever) to hate you the/this/who a human and when(-ever) to separate you and to revile and to expel the/this/who name you as/when evil/bad because of the/this/who son the/this/who a human
23 “Nthawi imeneyo sangalalani ndipo lumphani ndi chimwemwe chifukwa mphotho yanu ndi yayikulu kumwamba. Pakuti ndi zomwezonso zimene makolo awo anachitira aneneri.
(to rejoice *N+kO) in/on/among that the/this/who day and to leap look! for the/this/who wage you much in/on/among the/this/who heaven according to (the/this/who *N+KO) (it/s/he *N+kO) for to do/make: do the/this/who prophet the/this/who father it/s/he
24 “Ndinu atsoka, anthu olemera, popeza mwalandiriratu zokusangalatsani.
but/however woe! you the/this/who rich that/since: since to have in full the/this/who encouragement you
25 Tsoka inu amene mukudya bwino tsopano, chifukwa mudzakhala ndi njala. Ndinu atsoka, amene mukusekerera tsopano, chifukwa mudzabuma ndi kulira.
woe! you the/this/who to fill up (now *no) that/since: since to hunger woe! (you *k) the/this/who to laugh now that/since: since to mourn and to weep
26 Ndinu atsoka, anthu akamakuyamikirani, popeza makolo anu anawachitira aneneri onama zomwezi.”
woe! (you *k) when(-ever) you well to say all the/this/who a human according to (the/this/who *N+KO) (it/s/he *N+kO) for to do/make: do the/this/who false prophet the/this/who father it/s/he
27 “Koma Ine ndikuwuza inu amene mukundimva: Kondani adani anu, chitirani zabwino amene amakudani.
but you to say the/this/who to hear to love the/this/who enemy you well to do/make: do the/this/who to hate you
28 Dalitsani amene amakutembererani, apempherereni amene amakusautsani.
to praise/bless the/this/who to curse (you *N+kO) (and *k) to pray (about *N+kO) the/this/who to mistreat you
29 Ngati wina akumenyani patsaya limodzi mupatseninso tsaya linalo. Ngati wina akulanda mwinjiro wako, umulole atenge ndi mkanjo omwe.
the/this/who to strike you upon/to/against the/this/who cheek to furnish occasion and the/this/who another and away from the/this/who to take up you the/this/who clothing and the/this/who tunic not to prevent
30 Mupatseni aliyense amene akupemphani kanthu ndipo ngati wina atenga chinthu chanu, musamulamule kuti akubwezereni.
all (then the/this/who *ko) to ask you to give and away from the/this/who to take up the/this/who you not to demand
31 Inu muwachitire anthu ena, zomwe mukanafuna kuti iwo akuchitireni.
and as/just as to will/desire in order that/to to do/make: do you the/this/who a human (and you *ko) to do/make: do it/s/he similarly
32 “Ngati mukonda okhawo amene amakukondani, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amakonda amene amawakondanso.
and if to love the/this/who to love you what? you grace to be and for the/this/who sinful the/this/who to love it/s/he to love
33 Ndipo ngati muchita zabwino kwa amene ndi abwino kwa inu, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amachita izi.
and (for *no) if to do good the/this/who to do good you what? you grace to be and (for *ko) the/this/who sinful the/this/who it/s/he to do/make: do
34 Ndipo ngati mukongoza amene mukuyembekeza kuti abweza, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amabwereketsa kwa ochimwa anzawo, ndipo amayembekezera kubwezeredwa zonse.
and if (to lend/borrow *N+k+o) from/with/beside which to hope/expect (to take *N+kO) what? you grace to be and (for *ko) (the/this/who *k) sinful sinful to lend/borrow in order that/to to get back the/this/who equal
35 Koma kondani adani anu, achitireni zabwino, akongozeni koma osayembekezera kulandira kanthu. Pamenepo mphotho yanu idzakhala yayikulu ndipo inu mudzakhala ana a Wammwambamwamba, chifukwa ndi wokoma mtima kwa anthu osayamika ndi oyipa.
but/however to love the/this/who enemy you and to do good and to lend/borrow nothing to despair and to be the/this/who wage you much and to be son (the/this/who *k) Highest that/since: since it/s/he good/kind to be upon/to/against the/this/who ungrateful and evil/bad
36 Khalani achifundo, monga momwe Atate anu ali achifundo.”
to be (therefore/then *K) compassionate as/just as and the/this/who father you compassionate to be
37 “Musaweruze, ndipo inu simudzaweruzidwa. Musatsutse ndipo inu simudzatsutsidwa. Khululukirani ena ndipo mudzakhululukidwa.
and not to judge and no not to judge (and *no) not to condemn and no not to condemn to release: release and to release: release
38 Perekani ndipo mudzapatsidwa. Adzakupatsani mʼthumba mwanu muyeso wabwino, wotsenderezeka, wokhutchumuka ndi wosefukira. Pakuti muyeso umene mumagwiritsa ntchito, ndi omwewo adzakuyeserani.”
to give and to give you measure good to press down (and *k) to shake (and *k) to overflow to give toward the/this/who bosom you which (the/this/who *k) for (it/s/he *k) measure to measure to return you
39 Iye anawawuzanso fanizo ili, “Kodi munthu wakhungu angatsogolere munthu wakhungu mnzake? Kodi onse sadzagwera mʼdzenje?
to say then (and *no) parable it/s/he surely not be able blind blind to guide not! both toward pit (to fall into *N+kO)
40 Wophunzira sangapose mphunzitsi wake, koma yense amene waphunzitsidwa bwinobwino adzakhala ngati mphunzitsi wake.
no to be disciple above/for the/this/who teacher (it/s/he *k) to complete then all to be as/when the/this/who teacher it/s/he
41 “Kodi ndi chifukwa chiyani mumaona kachitsotso mʼdiso la mʼbale wanu ndi kusasamala mtengo uli mʼdiso mwanu?
which? then to see the/this/who speck the/this/who in/on/among the/this/who eye the/this/who brother you the/this/who then plank the/this/who in/on/among the/this/who one's own/private eye no to observe
42 Kodi munganene bwanji kwa mʼbale wanu kuti, ‘Mʼbale nʼtakuchotsa kachitsotso mʼdiso mwako,’ pamene inu eni ake mukulephera kuona mtengo uli mʼdiso mwanu? Inu achiphamaso, yambani mwachotsa mtengo uli mʼdiso mwanu, ndipo kenaka mudzaona bwinobwino ndi kuchotsa kachitsotso mʼdiso la mʼbale wanu.”
(or *ko) how! be able to say the/this/who brother you brother to release: permit to expel the/this/who speck the/this/who in/on/among the/this/who eye you it/s/he the/this/who in/on/among the/this/who eye you plank no to see hypocrite to expel first the/this/who plank out from the/this/who eye you and then to see clearly the/this/who speck the/this/who in/on/among the/this/who eye the/this/who brother you to expel
43 Palibe mtengo wabwino umene umabala chipatso choyipa, kapena mtengo oyipa umene umabala chipatso chabwino.
no for to be tree good to do/make: do fruit rotten nor (again *no) tree rotten to do/make: do fruit good
44 Mtengo uliwonse umadziwika ndi chipatso chake. Anthu sathyola nkhuyu pa mtengo waminga, kapena mphesa pa nthungwi.
each for tree out from the/this/who one's own/private fruit to know no for out from a thorn to collect fig nor out from thorn bush grapes to harvest
45 Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zosungidwa mu mtima mwake, koma munthu oyipa amatulutsa zinthu zoyipa zosungidwa mu mtima mwake. Pakamwa pake pamayankhula zimene zadzaza mu mtima mwake.
the/this/who good a human out from the/this/who good treasure the/this/who heart (it/s/he *ko) to bring out the/this/who good and the/this/who evil/bad (a human *k) out from the/this/who evil/bad (treasure the/this/who heart themself *K) to bring out the/this/who evil/bad out from for (the/this/who *k) overflow (the/this/who *k) heart to speak the/this/who mouth it/s/he
46 “Kodi nʼchifukwa chiyani munditchula kuti, ‘Ambuye, Ambuye’ koma simuchita zimene Ine ndinena?
which? then me to call: call lord: God lord: God and no to do/make: do which to say
47 Ine ndidzakuonetsani mmene alili munthu amene amabwera kwa Ine ndi kumva mawu anga ndi kuwachita.
all the/this/who to come/go to/with me and to hear me the/this/who word and to do/make: do it/s/he to show you which? to be like
48 Iye ali ngati munthu womanga nyumba, amene anakumba mozama nayika maziko ake pa mwala. Madzi osefukira atabwera ndi mphamvu, nawomba nyumbayo koma sinagwedezeka, chifukwa anayimanga bwino.
like to be a human to build home which to dig and to dig deep and to place foundation upon/to/against the/this/who rock flood then to be to strike the/this/who river the/this/who home that and no be strong to shake it/s/he (through/because of *N+kO) (the/this/who *no) (well *NO) (to build *N+KO) (it/s/he *no) (upon/to/against the/this/who rock *k)
49 Koma amene amamva mawu anga koma osawachita, akufanana ndi munthu amene anamanga nyumba yake koma yopanda maziko. Nthawi yomwe madziwo anawomba nyumbayo, inagwa ndipo inawonongekeratu.”
the/this/who then to hear and not to do/make: do like to be a human to build home upon/to/against the/this/who earth: soil without foundation which to strike the/this/who river and immediately (be downcast *N+kO) and to be the/this/who destruction the/this/who home that great

< Luka 6 >