< Luka 24 >

1 Pa tsiku loyamba la Sabata, mmamawa kwambiri, amayi anatenga zonunkhira napita ku manda.
Dănzorja ăn duminikă mujeri apljikat la gruapă ku jarbilje š ku unturilje karje miruasă če lja pripremit.
2 Anaona mwala wa pa manda utagubuduzika
Kănd jalje ažuns, avizut k je buluvanu karje ăvilja ulazu la gruapă runkat ăn partje.
3 ndipo atalowamo sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.
Auntrat ănontru, ali na găsăt tjela alu Domnuluj Isusuluj.
4 Pamene iwo ankadabwa za zimenezi, mwadzidzidzi, amuna awiri ovala zovala zonyezimira kwambiri anayimirira pambali pawo.
Pănd jalje aša astat zbunjitje păntruv aja če sa dogodit, dăturdată pănglă jej sa pojavit doj omurj ăn cualje karje blistjaštje.
5 Ndi mantha, amayiwo anaweramitsa nkhope zawo pansi, koma amunawo anawawuza kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukufuna wamoyo pakati pa akufa?
Mujerilje sa spirjat š sa poklonit ku lica kătri pămănt. Doj omurj lja tribat: “Dăče kătăc p viuv ăntră morc?
6 Iye sali muno ayi. Wauka! Kumbukirani zimene anakuwuzani pamene anali nanu ku Galileya:
Nuje aiča. Auskrăsnit! Dali nu vu găndic če vam zăs još ăn Galileja:
7 ‘Mwana wa Munthu ayenera kuperekedwa mʼmanja mwa anthu ochimwa, napachikidwa ndipo tsiku lachitatu adzaukitsidwanso.’”
‘Jo, Bijatu alu Omuluj, mora s fiuv predajit ăn mănj alu grešnikulor š jej p minje osă m razapnjaskă, ali jo aldă trje zălje osă m skol dăla morc.’”
8 Ndipo anakumbukira mawu ake.
Jalje sa dat d gănd k Isusu aja azăs.
9 Atabwerera kuchokera ku mandako, anafotokoza zinthu zonse kwa khumi ndi mmodziwo ndi kwa ena onse.
Š sa tors dăla gruapă s javjaskă alu unsprjače apostolurj š alu toc alcilor.
10 Amayi anali Mariya Magadalena, Yohana, Mariya amayi a Yakobo, ndi ena anali nawo amene anawuza atumwi.
Irja alja Marija d trg Magdala, Ivana š Marija, mama alu Jakov, š još njeke mujerj. Arubit tot alu apostolilor če sa dogodit,
11 Koma iwo sanawakhulupirire amayiwa, chifukwa mawu awo amaoneka kwa iwo ngati opanda nzeru.
ali alu apostolilor sa spurut k tot aja mujerj aizmislit. Š nu lja krizut alu mujerilor.
12 Komabe Petro anayimirira ndi kuthamangira ku manda. Atasuzumira, anaona nsalu zimene anamukulungira zija zili pa zokha, ndipo iye anachoka, akudabwa ndi zimene zinachitikazo.
Ipak, Petar dă fuga pănla gruapă. Kănd ažuns, s ujtă ănontru ali na vizut nimika osim skumpă albă plahtă ăn karje irja Isusu. Apljikat dăla gruapă š s ăntriba če sa dogodit.
13 Ndipo tsiku lomwelo, awiri a iwo ankapita ku mudzi wotchedwa Emau, pafupifupi makilomita khumi ndi imodzi kuchokera ku Yerusalemu.
Ăn zuvaja doj učenikurj alu Isusuluj pljakă ăn sat Emaus, dăpartje d Jeruzalem njeđe unsprjače kilomjatrje.
14 Iwo ankayankhulana za zonse zimene zinachitikazo.
P drum arubit d tot ča fost.
15 Pamenepo Yesu mwini wake anabwera ndi kuyenda nawo pamodzi;
Pănd jej aša arubit š raspravlja ăntră jej, avinjit Isusu š pljakă ku jej.
16 koma iwo sanamuzindikire.
Ali alu vojki alor irja skuns s l kunaskă.
17 Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukukambirana zotani mʼnjira muno?” Iwo anayima ndi nkhope zakugwa.
Isusu lja antribat: “D čaja aja raspravljic pănd putujic?” Jej astat pljinj d tugă.
18 Mmodzi wa iwo wotchedwa Kaliyopa anamufunsa kuti, “Kodi ndiwe wekha wokhala mu Yerusalemu amene sukudziwa zinthu zimene zachitika mʼmasiku awa?”
Unu dăn jej, karje s kjamă Kleofa, ja odgovorit: “Tu ješt jedini om karje avinjit d praznik ăn Jeruzalem karje nu štije ča fost ăn zuviljaštja.”
19 Iye anafunsa kuti, “Zinthu zotani?” Iwo anayankha nati, “Za Yesu wa ku Nazareti, Iye anali mneneri, wamphamvu mʼmawu ndi mu zochita pamaso pa Mulungu ndi anthu onse.
Isusu ăntrijabă: “Če afost?” Azăs: “Pa aja ča fost ku Isusu dăn Nazaret. Jel irja proroku š tuată lumja aputut s vjadă ku vorbilje š ku djela aluj k la trimjes Dimizov.
20 Akulu a ansembe ndi oweruza anamupereka Iye kuti aphedwe, ndipo anamupachika Iye;
Pănglă aja glavni popurlje š alji noštri altje članurlje alu vječe Amarje la predajit s fije osudit p muartje š la dat s l razapnjaskă.
21 koma ife tinkayembekezera kuti Iye ndiye amene akanawombola Israeli. Ndipo kuwonjeza apo, lero ndi tsiku lachitatu chichitikireni izi.
A noj njam nadit k jel ăla karje osă spasaskă p narodu alu Izrael dăla dušmanu aluj, već atrikut trje zălje d kănd je mort.
22 Kuwonjezanso apo, ena mwa amayi athu atidabwitsa ife. Iwo anapita ku manda mmamawa
Ali aja nuje tot k š njeke mujeri karje l pratja ku toc noj, nja zbunjit p noj: čim asvanit zuva jalje apljikat la gruapă,
23 koma sanakapeze mtembo wake. Iwo anabwera ndi kudzatiwuza ife kuti anaona masomphenya a angelo amene anati Yesu ali moyo.
ali ačija na găsăt tjela aluj. Avinjit š azăs k lji sa pokazăt anđelurlje š lja zăs k Isusu viuv.
24 Kenaka ena mwa anzathu anapita ku manda ndipo anakapeza monga momwe amayiwo ananenera, koma Iye sanamuone.”
Njeki dăn noj adat fuga la gruapă š angăsăt k je gruapa guală baš kum azăs mujerilje, ali na vizut p Isusu k je viuv.”
25 Iye anawawuza kuti, “Inu ndinu anthu opusa, osafuna kukhulupirira msanga zonse zimene aneneri ananena!
P aja Isusu lja zăs: “O kum ištjec nerazumni! Dăče vuavă grjev s kridjec ăn aja ča zăs prorokurlje?
26 Kodi Khristu sanayenera kumva zowawa izi ndipo kenaka ndi kulowa mu ulemerero wake?”
Dali nu tribja Kristu s trpjaskă tot majdată njego če s ănčapje s vladjaskă p toc?”
27 Ndipo kuyambira ndi Mose ndi aneneri onse Iye anawafotokozera zimene zinalembedwa mʼmalemba wonse zokhudzana ndi Iye mwini.
Aša Isusu lja objasnit tot če Mojsije š toc prorokurlje azăs ăn Svăntă pismă d jel.
28 Atayandikira mudzi omwe amapitako, Yesu anachita ngati akupitirira.
Kănd avinjit upruapje d sat undje pljakă, Isusu sa fukut k vrja s pljače maj dăpartje.
29 Koma iwo anamupempha Iye kwambiri kuti, “Mukhale ndi ife, popeza kwatsala pangʼono kuda, ndipo dzuwa lili pafupi kulowa.” Ndipo Iye anapita kukakhala nawo.
Ali jej la nagovorit: “Rămăj ku noj! Već je sara. Vinje nuaptja!” Aša auntrat ăn kasă s rămăje ku jej.
30 Iye ali pa tebulo pamodzi nawo, anatenga buledi ndipo anayamika, nanyema nayamba kuwagawira.
Pănd afost ku jej la astal, Isusu alat mălaju, zahvaljit alu Dimizovuluj, la frănt š la dat alor.
31 Kenaka maso awo anatsekuka ndipo anamuzindikira Iye, ndipo anachoka pakati pawo.
Atunča alor sa diškis vojki š jej la kunuskut. Ali jel la vojki alor anistanit.
32 Iwo anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi mitima yathu sinali kutentha mʼkati mwathu pamene Iye ankayankhulana nafe pa njira ndi mmene anatitsekulira malemba?”
A jej azăs unu alu altuluj: “Kum nja fost pljinje inimilje kănd p drum rubja ku noj š nji objasnja Svănta pisma!”
33 Nthawi yomweyo iwo anayimirira ndi kubwerera ku Yerusalemu. Iwo anapeza khumi ndi mmodziwo ndi ena anali nawo nasonkhana pamodzi
Sa skulat š sa tors ăn Jeruzalem. Apljikat la lok undje sa străns unsprjače apostolurj š p alcă sljedbenikurj alu Isusuluj.
34 ndipo anati, “Ndi zoonadi! Ambuye auka ndipo anaonekera kwa Simoni.”
Jej zăče: “Istina je, Domnu Isusu auskrisnit. Sa ukazăt alu Šimunuluj!”
35 Kenaka awiriwo anawawuza zimene zinachitika pa njira, ndi mmene iwo anamudziwira Yesu, Iye atanyema buledi.
Atunča š ăštja alji doj rubja če sa dogodit p drum š kum akunuskut p Isusu pănd jel afrănt mălaju.
36 Akufotokoza zimenezi, Yesu mwini wake anayimirira pakati pawo ndipo anati, “Mukhale ndi mtendere.”
Pănd jej doj rubja, Isusu dăturdată astat ăntră jej toc. Lji zăče: “Mir vuavă!”
37 Koma chifukwa choti anathedwa nzeru ndi kuchita mantha, ankaganiza kuti akuona mzukwa.
Ali lja afost frikă daja če găndit k vjadje măroj.
38 Iye anawafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukuvutika? Nʼchifukwa chiyani mukukayika mu mtima mwanu?
Š Isusu lji zăče: “Dăče vu frikă? Dăče ăn voj s fače sumnje ăn inimă?”
39 Taonani manja anga ndi mapazi anga. Ine ndine amene! Khudzeni kuti muone. Mzukwa ulibe mnofu ndi mafupa monga mukuonera ndili nazo.”
Atunča lja arătat mănjilje š pičuarilje š azăs: “Ujtacăvă la rănj! Jo sănt aja! Punjec mănilje p minje š osă vidjec! Măroji narje karnje š vuasă kašă če lji am jo!”
40 Iye atanena izi anawaonetsa manja ake ndi mapazi ake.
41 Ndipo pamene iwo samakhulupirirabe, chifukwa cha chimwemwe ndi kudabwa, Iye anawafunsa kuti, “Kodi muli ndi chakudya chilichonse pano?”
A jej d radost na putut s krjadă alu vojki alor, njego sa mirat. Jel ăntrijabă: “Avjec čiva d mănkat?”
42 Iwo anamupatsa Iye kachidutswa ka nsomba yophika.
Ja dat krod d pjaštje pržăt,
43 Iye anakatenga ndi kukadya iwo akuona.
a jel l ja š mălănk pănglă jej.
44 Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene ndinakuwuzani pamene ndinali nanu: chilichonse chiyenera kukwaniritsidwa chimene chinalembedwa cha Ine mʼbuku la Malamulo a Mose, Aneneri ndi Masalimo.”
Atunča zăče: “Asta če sa dogodit upravo aja če vam zăs k osă dogodjaskă. Pănd majdată amfost ku voj, vam zăs: atribut s s ispunjaskă tot če skrije d minje ăn zakonu alu Mojsije, ăn knjige d prorokurj š ăn Psalmi.”
45 Kenaka anawatsekula maganizo kuti azindikire Malemba.
Atunča lja žutat s razumjaskă čije skris ăn Svăntă pismă.
46 Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene zinalembedwa: Khristu adzazunzika ndipo adzauka kwa akufa tsiku lachitatu.
Kănd azavršăt jel azăs: “Kašă kum vidjec, aša skrije ăn Svăntă pismă k jo, Kristu, trjebje s trpjesk š s mor š aldă trje zălje s m skol dăla morc
47 Ndipo kutembenuka mtima ndi kukhululukidwa kwa machimo zidzalalikidwa mu dzina lake kwa anthu amitundu yonse kuyambira mu Yerusalemu.
š ku autoritetu alu mjov s rubjaskă alu tuată lumja k trjebje s s okrinjaskă dăla grešală š Dimizov osă lji oprostjaskă grešala. Osă ănčipjec ăn Jeruzalem
48 Inu ndinu mboni za zimenezi.
s zăčec alu alcilor aja če voj auzăt š avizut dăla minje.
49 Ine ndidzakutumizirani chimene Atate anga analonjeza. Koma khalani mu mzinda muno mpaka mutavekedwa mphamvu yochokera kumwamba.”
A jo osă vu trimjet p Sufljetu alu Svăntuluj, p karje Tatimjov ăn čerj aobečit k vuavă osă vije. Răminjec ăn trg Jeruzalem pănd Dimizov nu trimjatje p voj săla d sus!”
50 Iye atawatengera kunja kwa mzindawo mpaka ku Betaniya, anakweza manja ake ndi kuwadalitsa.
Isusu atunča askos p učenikurlje aluj d trg Jeruzalem pănla lok upruapje d sat Betanija. Ănklo adrikat mănilje š sa rugat s lji blagoslovjaskă Dimizov.
51 Iye akuwadalitsa, anawasiya ndipo anatengedwa kupita kumwamba.
Pănd lja blagoslovit, Isusu afost drikat p čerj tot pănd nu lja nistanit dăn vojk.
52 Pamenepo anamulambira Iye ndipo anabwerera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu.
Učenikurlje sa poklonit la Isusu, a atunča jej sa tors ku marje radost ăn Jeruzalem.
53 Ndipo iwo anakhalabe ku Nyumba ya Mulungu, akulemekeza Mulungu.
Atunča irja stalno ăn Hram š slavja p Dimizov.

< Luka 24 >