< Luka 21 >

1 Yesu atayangʼana, anaona olemera akuyika mphatso zawo mu chosungira ndalama za mʼNyumba ya Mulungu.
A Yeshu bhatendaga kwalolesheyanga matajili bhalitaganga mbepei yabhonji nshibhiko sha ekalu,
2 Iye anaonanso mkazi wamasiye wosauka akuyikamo timakopala tiwiri.
gubhaaweni bhakongwe bhamo bhashitenga na bhaalaga bhalitumbushiya shenti ibhili.
3 Iye anati, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mkazi wamasiye wosaukayu wapereka zambiri kuposa ena onsewa.
Bhai, gubhashite, “Kweli ngunakummalanjilanga, bhene bhakongwe bha shitenga bhaalagabha bhashitaga yaigwinji kupunda bhowenji.
4 Anthu onsewa atapa mphatso zawo kuchokera pa zochuluka zimene ali nazo; koma uyu, mwa umphawi wake, wapereka zonse zimene ali nazo.”
Pabha bhananji bhowe bhashishoyanga mbepei ya indu ipundile pa indu yabhonji ila, ikabheje abha na kulaga kwabho, bhashishoya yowe ibhakulupalilaga nkulamila.”
5 Ena mwa ophunzira ake ankachita ndemanga za mmene Nyumba ya Mulungu anayikongoletsera ndi miyala yokongola ndiponso zinthu zina zomwe anthu anapereka kwa Mulungu. Koma Yesu anati,
Bhaajiganywa bhabho bhatendaga kungulushilanga ga Liekalu shilishite kelengelelwa kwa maganga ga konja na indu ishoshiywe mbepei kwa a Nnungu. Ikabheje a Yeshu gubhashite,
6 “Koma zimene mukuziona panozi, nthawi idzafika pamene ngakhale mwala umodzi omwe sudzakhala pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.”
“Gene gowe gunkugabhonangaga shigaishe mobha nkali liganga limo likalepeka pantundu liganga lina, gwangali kubhomolwa.”
7 Iwo anafunsa kuti, “Aphunzitsi, kodi zonsezi zidzachitika liti? Ndipo tidzaonera chiyani kuti zili pafupi kuchitika?”
Bhai, gubhaabhushiyenje, “Mmajiganya, genego shigakoposhele shakani? Na ilangulo yashi shiikoposhele kulangula genego gali tome na koposhela?”
8 Iye anayankha kuti, “Chenjerani kuti musanyengedwe. Pakuti ambiri adzabwera mʼdzina langa nadzati ‘Ine ndine Iye’ ndi kuti ‘Nthawi yayandikira.’ Musadzawatsate iwo.
A Yeshu gubhaajangwilenje, “Mwiiteiganje nnatembwanga. Pabha bhabhagwinji shibhaikangane bhalikwitembanga kuti nne a Kilishitu Bhaatapula na malanga gala gabhandishile. Ikabheje mmanganya nnaakagulanje!
9 Mukadzamva zankhondo ndi zipolowe, musadzachite mantha. Zinthu izi ziyenera kuchitika poyamba, koma chimaliziro sichidzafika nthawi yomweyo.”
Bhai, pushimpilikananje ga ngondo na tendebhukana, nnajogopanje, pabha yeneyo inapinjikwa ikoposhele oti, ikabheje mpelo gwa gowe, ukanabhe.”
10 Kenaka anawawuza kuti, “Mtundu wa anthu udzawukirana ndi mtundu wina, ndi ufumu kuwukira ufumu wina.
Bhai gubhapundile bheleketa. “Shilambo shimo shishikomane na shilambo shina, na upalume gumo shiukomane na upalume guna.
11 Kudzakhala zivomerezi zazikulu, njala ndi miliri mʼmalo osiyanasiyana, ndi zinthu zoopsa ndi zizindikiro zamphamvu kuchokera kumwamba.
Kupinga koposhela kuungumila kwa litaka kwa punda, na limbukute lya shibhanga na ilwele ya jambushiya mmbali yaigwinji. Kupingabha na indu ya jogoya na ilangulo yaikuluikulu kunnungu.”
12 “Koma zonsezi zisanachitike, adzakugwirani ndi kukuzunzani. Adzakuperekani ku masunagoge ndi ku ndende, ndipo adzakutengerani pamaso pa mafumu ndi olamulira, ndipo zonsezi zidzachitika chifukwa cha dzina langa.
“Ikabheje yene yoweyo ikanabhe koposhela shibhankamulanje nikumpotekanga na shibhampelekanje Mmashinagogi na kuntabhanga mmagelesha na shimpelekwanje kwa bhakulungwa na kubhakulungwanji kwa ligongo lyangu,
13 Umenewu udzakhala mwayi wanu ochitira umboni.
yeneyo shiikoposhele nkupinga mwaakong'ondelanje ngani jangu.
14 Koma tsimikizani mtima kuti musadzade nkhawa za momwe mudzadzitchinjirizire.
Ikabheje nnakolanje lipamba mmitima jenunji kuti shimmeleketanje nndi sha kuitapula,
15 Pakuti Ine ndidzakupatsani mawu ndi nzeru kotero kuti palibe mmodzi wa adani anu adzathe kuwakana kapena kuwatsutsa.
pabha shinimpanganje malobhe na lunda, gaatenda ashaamagongo ajenunji bhakakombolanga kunkananga wala kuntaukanga.
16 Inu mudzaperekedwa ndi makolo anu, abale, anansi ndi abwenzi anu ndipo ena mwa inu adzakuphani.
Bhankwetenje na ashapwenu na ashalongo ajenunji na ashambwiga ajenunji shibhankananje na mmananji shimmulagwanje.
17 Anthu onse adzakudani chifukwa cha Ine.
Bhandu bhowe shibhampatanje, kwa ligongo lya lina lyangu.
18 Koma palibe tsitsi limodzi la mʼmutu mwanu lidzawonongeke.
Ikabheje, nkali luumbo lumo lwa mmitwe jwenunji lukaobha.
19 Mukadzalimbikira ndiye mudzapeze moyo.
Kwa kwiikakatimila kwenunji shimwitapulanje.”
20 “Mukadzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu ankhondo, inu mudzadziwe kuti kuwonongeka kwake kuli pafupi.
“Pushinshibhonanje shilambo sha Yelushalemu shitimbililwe na makuga ga ashimanjola, bhai mmumanyanje kuti gabhandishile malanga ga shene shilambosho kuangabhanywa.
21 Pamenepo amene ali ku Yudeya adzathawire ku mapiri, amene ali mu mzinda adzatulukemo, ndi amene ali ku midzi asadzalowe mu mzinda.
Penepo bhalinginji ku Yudea bhabhutushilanje mwitumbi, bhalinginji kunnjini bhashokangane, na bhalinginji mmigunda bhanabhujangane kunnjini.
22 Pakuti iyi ndi nthawi yachilango pokwaniritsa zonse zimene zinalembedwa.
Pabha gene mobhago shigabhe ga mboteko ya a Nnungu kubhandu bhabho, nkupinga gowe gajandikwe Mmajandiko gamalile.
23 Zidzakhala zoopsa nthawi imenewo kwa amayi oyembekezera ndi amayi oyamwitsa! Kudzakhala masautso aakulu mʼdziko ndipo anthu onse adzawakwiyira.
Ole gwabhonji bhakwetenje ndumbo na bhajonjeyanga gene mobhago! Pabha shipingapagwa shilaje shapunda nshilambo, na nnjimwa ya a Nnungu shiyajiilanje bhene bhandunjibha.
24 Iwo adzaphedwa ndi lupanga ndi kutengedwa ukapolo kupita ku mayiko wonse. Yerusalemu adzaponderezedwa ndi anthu a mitundu ina mpaka nthawi ya a mitundu ina itakwaniritsidwa.
Bhana shibhabhulagwanje kwa upanga, bhana shibhatolwe ubhanda mwiilambo yowe na shilambo sha Yelushalemu shipinga libhatwa na bhandunji bha ilambo inape mpaka mobha gabhonji pushigatimilile.
25 “Padzakhala zizindikiro zodabwitsa pa dzuwa, mwezi ndi nyenyezi. Pa dziko lapansi, mitundu ya anthu idzakhala mʼmasautso ndipo idzathedwa nzeru pakumva mkokomo ndi mafunde a mʼnyanja.
“Kupingabha na ilangulo kulyubha, kumwei, na kundondwa. Ilambo ya pashilambolyo ni ipingabha nshilaje kwa ligongo lya lipamba ga nng'indo gwa mabhimbili ga bhaali.
26 Anthu adzakomoka chifukwa cha mantha, akadzamva za zimene zikubwera pa dziko lapansi, pakuti zinthu zamlengalenga zidzagwedezeka.
Bhandunji shibhaondokanje kwa ligongo lya bhoga, bhalilolelanga indu ipinga koposhela nshilambolyo, pabha mashili ga kunnungu gapinga tikinywa.
27 Nthawi imeneyo adzaona Mwana wa Munthu akubwera ndi mitambo, mphamvu ndi ulemerero waukulu.
Kungai, shibhammonanje Mwana juka Mundu alikwiya mmaunde, ali na mashili na ukonjelo nkulu.
28 Zinthu izi zikadzayamba kuchitika, mudzayimirire ndi kutukula mitu yanu, chifukwa chipulumutso chanu chayandikira.”
Malanga gushigatandubhe genego kukoposhela, nnjimangane, nnjinulanje meyo genunji kunani, pabha kugombolwa kwenunji kubhandishile.”
29 Iye anawawuza fanizo ili, “Taonani mtengo wamkuyu ndi mitengo ina yonse.
Kungai gubhaabhalanjilenje lutango, “Nnolanje ntini na mikongo jina jowe.
30 Ikamatulutsa masamba, mumakhoza kudzionera nokha ndi kudziwa kuti dzinja lili pafupi.
Punkubhonanga jiliipuka maamba, nnakumumanyanga kuti shuku shibhandishile.
31 Chimodzimodzinso, mukadzaona zinthu zonsezi, dziwani kuti ufumu wa Mulungu uli pafupi.
Nneyo peyo, pushimmonanje genego galikoposhela, shimmumanyanje kuti Upalume gwa a Nnungu ubhandishile.”
32 “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mʼbado uno sudzatha mpaka zinthu zonsezi zitachitika.
“Kweli ngunakummalanjilanga, alu lubheleko lwa nnainolu lukapita mpaka gene gowega gamalile.
33 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
Kunnungu na shilambolyo shiipite, ikabheje malobhe gangu gakapita.”
34 “Samalani, kuti mitima yanu ingalemetsedwe ndi maphwando, kuledzera ndi kudera nkhawa za moyo uno, ndi kuti tsiku ilo lingadzakupezeni modzidzimutsa ngati msampha.
“Mwiiteiganje, mitima jenunji jinakwiibhuka nkupoka na kolelwa na kuabhushila ya nndamo jino. Lyene lyubhalyo linakunng'imananga shiimushila mbuti kutanjila kwa nnukonji.
35 Pakuti lidzafika pa onse okhala pa dziko lonse lapansi.
Nneyo ni shiipinga koposhela, kubhandu bhowe bhaatamangana pa shilambolyo.
36 Khalani tcheru nthawi zonse ndi kupemphera kuti inu mudzathe kuthawa zonse zimene zili pafupi kuchitika, ndi kuti mudzathe kuyima pamaso pa Mwana wa Munthu.”
Bhai nsheyanje, nkwaajuga a Nnungu mobha gowe, kupinga mpatanje mashili ga kwiitapula pushigakoposhele genego na jima mmujo jika Mwana juka Mundu.”
37 Tsiku lililonse Yesu amaphunzitsa ku Nyumba ya Mulungu, ndi madzulo ali wonse Iye amachoka kukakhala pa phiri la Olivi usiku wonse.
Kila mui a Yeshu bhatendaga jiganya Nniekalu, ikabheje shilo bhatendaga tama kushitumbi sha Misheituni.
38 Ndipo anthu onse amabwera mmamawa kudzamumva Iye ku Nyumba ya Mulungu.
Bhandu bhowe bhatendaga labhanga lyamba, kwenda ku Liekalu kukwaapilikanishiya.

< Luka 21 >