< Luka 17 >

1 Yesu anati kwa ophunzira ake, “Zinthu zimene zimachimwitsa sizingalephere kubwera, koma tsoka kwa munthu wozibweretsayo.
Yesu akabhajobhela bhanafunzi bha muene, “mambo ghabhisababisha bhanu bhabhombayi dhambi ghilondeka lepi kuhomela, lakini ole wake jha isababisya!
2 Kukanakhala bwino kwa iye kuti aponyedwe mʼnyanja atamangiriridwa mwala wamphero mʼkhosi mwake kusiyana kuti achimwitse mmodzi mwa ana aangʼonowa.
Ngajhijhele heri munu ojhu ngaafungibhu ligenga lya lilopa lya kusyaghila pa n'singu ni kutaghibhwa mu bahari kuliko kumbomba mmonga ghwa abha bhadebe akhetayi dhambi.
3 Nʼchifukwa chake dziyangʼanireni nokha. “Ngati mʼbale wanu achimwa, mudzudzuleni, ndipo ngati alapa, mukhululukireni.
Mukilendayi. Kama ndongo bhu akukosili umwonyayi, na akutubuajhi msameajhi.
4 Ngati iye akulakwira kasanu ndi kawiri pa tsiku, ndipo ngati nʼkubweranso kwa iwe kasanu ndi kawiri nati, ‘Ndalapa,’ umukhululukire.”
Kama akukosili mara saba kwa ligono limonga akahida kwa bhebhe ijobha, 'nitubu,' m'sameajhi!”
5 Atumwiwo anati kwa Ambuye, “Kulitsani chikhulupiriro chathu!”
Mitume bha muene bhakan'jobhela Bwana, “Tujhongeselayi imani jha jhotu.”
6 Yesu anayankha kuti, “Ngati muli ndi chikhulupiriro chachingʼono ngati kambewu kampiru, mukhoza kulamula mtengo wamkuyu uwu kuti, ‘Zulidwa ndi kukadzalidwa mʼnyanja,’ ndipo udzakumverani.
Bwana akajobha, “Kama ngamujha ni imani kama punje jha haradarii, ngamubhwesi kuujobhela libehe e'le lya mkuyu, 'dupukayi na ukamelayi mu bahari,' nibhwene ngaubhatiili.
7 “Tiyerekeze kuti mmodzi mwa inu anali ndi wantchito wolima kapena woweta nkhosa, kodi angawuze wantchitoyo atabwera ku munda kuti, ‘Tsopano bwera kuno khala pansi kuti udye?’
Lakini niani miongoni mwa muenga, ambajhe ajhe ni mtumishi jhailema n'gonda au jhaidima kondoo, ibeta kun'jobhela akerukayi kun'gonda hidayi manyata na utamayi uliajhi kyakulya?
8 Kodi sangamuwuze kuti, ‘Konzere chakudya cha madzulo, iweyo ukonzeke ndipo undidikirire pamene ndikudya ndi kumwa; kenaka ukhoza kudya ndi kumwa?’
Je ibeta lepi kun'jobhela niandalilaiji kyakulya niliajhi, na ukikongayi mkanda na unitumikilayi mpaka panibeta kumala kulya ni kunywa. Baada jha apo wibeta kulya ni kunywa?
9 Kodi iye angathokoze wantchitoyo chifukwa chochita chimene anawuzidwa kuchita?
Ibeta lepi kumbombesya mtumishi ojhu kwandabha atimisi ghala gha an'jobhili?
10 Chimodzimodzi inunso, mukachita zonse zimene munawuzidwa, muzinena kuti, ‘Ndife antchito osayenera; tangogwira ntchito yathu basi.’”
Mebhu ni muenga mkabhombayi gha mlaghisibhu mjobhayi 'Tete twe bhatumishi twetukastahili lepi. Tubhombi tu ghala ghaghalondekeghe kubhombeka.'
11 Tsopano Yesu anayenda mʼmalire a pakati pa Samariya ndi Galileya pa ulendo wake wa ku Yerusalemu.
Jhatokili kwamba bho isafiri kulota Yerusalemu, a'petili mpakani mwa Samaria ni Galilaya.
12 Akulowa mʼmudzi wina, amuna khumi amene anali ndi khate anakumana naye. Iwo anayima patali
Bhoijhingili mu kijiji kimonga, okhu abhonene ni bhanu kumi bhabhajhele ni ukoma. Bhakajhema patali
13 ndipo anafuwula ndi mawu okweza kuti, “Yesu, Ambuye, tichitireni chifundo!”
Bhakapwesya sauti bhakajobha “Yesu, Bwana tuhurumilayi.”
14 Iye atawaona, anati, “Pitani kadzionetseni nokha kwa ansembe.” Ndipo pamene iwo ankapita, anachiritsidwa.
Bho abhabhwene akabhajobhela, “Mulolayi mkakilesiajhi kwa makuhani.” na bhene bho bhilota bhatakasiki.
15 Mmodzi wa iwo, ataona kuti wachiritsidwa, anabwerera, nayamika Mulungu ndi mawu okweza.
Mmonga ghwa bhene bho ambwene aponili, akakerebhuka kwa sauti mbaha akan'sifu K'yara.
16 Anagwetsa nkhope yake nagwa pa mapazi a Yesu ndi kumuthokoza. Ndipo iye anali Msamariya.
Akapiga magoti mu magolo gha Yesu akan'shukuru. Muene ajhele Msamaria.
17 Yesu anafunsa kuti, “Kodi amene anachiritsidwa sanalipo khumi? Nanga asanu ndi anayi ena ali kuti?
Yesu ajibili, akajobha, “Je bhatakasikilepi bhoha kumi? bhajhendaku bhala bhamana tisa?
18 Kodi palibe mmodzi mwa iwo amene anabwerera kudzalemekeza Mulungu kupatula mlendoyu?”
Ajhelepi hata mmonga jhaabhonekene kukerebhuka ili kun'tukusya k'yara, isipokujha ojho n'hesya?”
19 Pamenepo anati kwa iye, “Imirira ndipo pita; chikhulupiriro chako chakuchiritsa iwe.”
Akan'jobhela, “Jhinukayi na alotayi imani jha jhobhi jhikuponyisi.”
20 Ndipo Afarisi atamufunsa Iye kuti, ufumu wa Mulungu udzabwera liti, Yesu anayankha kuti, “Mulungu sakhazikitsa ufumu wake mooneka ndi maso,
Bho akotibhu ni Mafarisayo kujha ufalme bhwa K'yara bhwihida ndali, Yesu akabhajibu akajobha, “Ufalme bhwa K'yara sio khenu ambakyo kibhwesya kubhonekana.
21 kapenanso kuti anthu adzati, ‘Uwu uli apa,’ kapena ‘Uwo uli apo,’ Pakuti taonani ufumu wa Mulungu uli pakati panu.”
Wala bhanu bhibeta lepi kujobha, 'Langayi apa!' au, 'Langayi khola!' kwandabha ufalme bhwa K'yara ajhele mugati mwa jhomo.”
22 Kenaka Iye anati kwa ophunzira ake, “Masiku akubwera pamene inu mudzalakalaka mutaona tsiku limodzi la masiku a Mwana wa Munthu, koma simudzaliona.
Yesu akabhajobhela bhanafunzi bha muene, “Wakati wibeta kufika ambapo mwibeta kunoghela kujhibhona moja jha magono gha mwana ghwa Adamu, lakini mwibeta lepi kujhibhona.
23 Anthu adzakuwuzani kuti, ‘Uyo ali apoyo!’ kapena ‘Uyu ali apa!’ Musawathamangire iwo.
Bhibeta kubhajobhela, 'Langayi, khola! Langayi apa!' Lakini msil'oti kulanga, wala kubhakhesya,
24 Pakuti monga mphenzi ingʼanima ndi kuwala kuchokera mbali ina ya thambo kufikira inzake, koteronso adzakhala ali Mwana wa Munthu pa tsiku lake.
Kama umeme bhwa radi kya bhwimulika mu anga kubhwanjila lubhafu l'ongi hadi l'ongi. Mebhu hata mwana ghwa Adamu ibeta kujha mebhu mu ligono lya muene.
25 Koma poyamba ayenera kuzunzika mu zambiri ndi kukanidwa ndi mʼbado uno.
Lakini hoti jhibeta kulondeka kutesibhwa mu mambo ghamehele ni kubelibhwa ni kizazi ekhe.
26 “Monga mmene zinkachitikira nthawi ya Nowa, momwemonso zidzachitikanso nthawi ya Mwana wa Munthu.
Kama kyajhikajhele magono gha Nuhu, ndo kyajhibetakujha mu magono gha mwana ghwa Adamu.
27 Anthu ankadya, kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa mpaka tsiku limene Nowa analowa mʼchombo. Pomwepo chigumula chinafika ndi kuwawononga onsewo.
Bhalili, bhanywili, bhakagega ni kugegikibhwa mpaka ligono lela ambalyo Nuhu bho ajhingili mu safina ni gharika ikahida ni kubhaangamisya bhoha.
28 “Zinalinso chimodzimodzi nthawi ya Loti. Anthu ankadya ndi kumwa, kugula ndi kugulitsa, kudzala ndi kumanga.
Ndo kyajhikajhele mu magono gha Lutu, bhalili, kunywa, bhagolili ni kuhemelesya, kulema na bhajengili.
29 Koma tsiku limene Loti anachoka ku Sodomu, moto ndi sulufule zinavumbwa kuchokera kumwamba ndi kuwawononga onsewo.
Lakini ligono lela Lutu bho abhokili Sodoma, jhatonyili fula jha muoto ni kiberiti kuhoma kumbinguni jhabhaangamisi bhoha.
30 “Zidzakhalanso choncho Mwana wa Munthu akadzaonekera.
Mebhu ndo kyajhibetakujha mu ligono lela lya mwana ghwa Adamu paibetakufunulibhwa.
31 Tsiku limenelo munthu amene ali pa denga la nyumba yake, ndi katundu wake ali mʼnyumbamo, asadzatsike kukatenga. Chimodzimodzinso, munthu amene adzakhale ali ku munda asadzabwerere kukatenga chilichonse.
Ligono e'lu, usinduhusu jha ajhele padari jha nyumba aseleleyi kutola bidhaa sya muene mugati munyumba. Na usinduhusu jha ajhele kun'gonda kukerebhuka kunyumba.
32 Kumbukirani mkazi wa Loti!
Mkhombokajhi ghwa Lutu.
33 Aliyense amene ayesetsa kusunga moyo wake adzawutaya, ndipo aliyense amene ataya moyo wake adzawusunga.
Jhejhioha jha ijaribu kughaokola maisha gha muene ibeta kughajhasya, lakini jhejhioha jha ibeta kujhesya maisha gha muene ibeta kughaokola.
34 Ine ndikukuwuzani inu, usiku umenewo anthu awiri adzagona pa mphasa imodzi; wina adzatengedwa ndipo wina adzasiyidwa.
Nikabhajobhela, kiru ekhu kibeta kujha ni bhanu bhabhele pa kitanda kimonga. Mmonga ibeta kujha ni jhongi ilekibhwa.
35 Amayi awiri adzakhala pamodzi akusinja; wina adzatengedwa ndi wina adzasiyidwa.
Kubetakujha ni bhadala bhabhele bhisyagha nafaka pamonga,
36 Amuna awiri adzakhala akulima mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzasiyidwa.”
mmonga itolibhwa ni jhongi ilekibhwa.”
37 Iwo anafunsa kuti, “Ambuye, kodi zimenezi zidzachitikira kuti?” Iye anayankha kuti, “Kumene kuli mtembo, nʼkumene makwangwala amasonkhanako.”
Wakamwuliza, “Wapi, Mungu?” akabhajobhela, “Pale ulipo mzoga, ndipo tai hukusanyika kwa pamoja.”

< Luka 17 >