< Luka 16 >

1 Yesu anawuza ophunzira ake kuti, “Panali munthu wina wachuma amene kapitawo wake anzake anamuneneza kuti amawononga chuma chakecho.
Jesus el fahk nu sin mwet tumal lutlut, “Oasr sie mwet na kasrup, su filiya sie mwet tutafpo in liyaung ma lal nukewa. Na fwackyang nu sin mwet kasrup sac lah mwet tutafpo se lal ah supoklotina ma lal uh.
2 Choncho anamuyitana ndi kumufunsa kuti, ‘Kodi nʼchiyani chimene ndikumva za iwe? Pereka tsatanetsatane wa ntchito yako, pakuti supitirizanso kukhala kapitawo wanga.’
Ouinge el pangnolma ac fahk nu sel, ‘Mea nga lohng keim inge? Ase nu sik sie pwepu in akkalemye orekmakinyen ma luk uh sum, mweyen kom ac tia sifil karingin ma luk uh.’
3 “Kapitawoyo analingalira kuti, ‘Kodi tsopano ndidzachita chiyani? Bwana wanga andichotsa ntchito. Ine ndilibe mphamvu zokwanira zolimira, komanso ine ndimachita manyazi kupempha.
Ac mwet tutafpo sac sifacna nunku in el, ‘Mea nga ac oru, ke leum luk el akola in sisyula liki orekma luk uh? Nga munas in wi puk laf, ac nga mwekin in ngusr.
4 Ine ndikudziwa chimene ndidzachita kotero kuti, pamene ntchito yanga yatha pano, anthu adzandilandire mʼnyumba zawo.’
Kwal, nga etu lah mea nga ac oru, tuh mwet uh in suliyu nu in lohm selos tukun sisila nga liki orekma luk.’
5 “Choncho iye anayitana aliyense amene anali ndi ngongole kwa bwana wake. Iye anafunsa woyamba, ‘Kodi uli ndi ngongole yotani kwa bwana wanga?’
Ouinge el solama kais sie mwet ma oasr soemoul la nu sin leum sac. El siyuk sin mwet se meet ah, ‘Lupa su soemoul lom nu sin leum luk?’
6 “Iye anayankha kuti, ‘Migolo yamafuta a olivi 800.’ “Kapitawo uja anamuwuza iye, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo, khala pansi msanga ndipo lemba kuti ndi migolo 400.’
Ac el topuk, ‘Barrel siofok ke oil in olive.’ Na mwet tutafpo sac fahk nu sel, ‘Pa inge pwepu in misa lom uh. Muta insacn, simusla ma lumngaul.’
7 “Kenaka iye anafunsa wachiwiri kuti, ‘Nanga iwe uli ndi ngongole yotani?’ “Iye ayankha kuti madengu a tirigu 1,000. “Iye anati, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo ndipo ulembepo 800.’
Na el sifil siyuk sin sie pac, ‘Ac kom, lupa su soemoul lom?’ Ac mwet sac topuk, ‘Sie tausin bushel in wheat.’ Na mwet tutafpo sac fahk ouinge, ‘Pa inge pwepu in misa lom uh. Simusla ma oalfoko.’
8 “Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
Ouinge, leum lun mwet tutafpo kutasrik sac kaksakunul ke inkanek usrnguk ma el oru, mweyen mwet facl se inge arulana yohk usrnguk lalos ke ma elos oru, liki mwet lun kalem uh.” (aiōn g165)
9 Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
Ac Jesus el sifilpa fahk, “Ke ma inge nga fahk nu suwos: orekmakin mwe kasrup lun faclu tuh kowos in konauk mwet kawuk lowos, na ke pacl se lisr, ac fah suliyuk kowos nu in lohm kawil. (aiōnios g166)
10 “Amene akhulupirika pa zinthu zochepa akhoza kukhulupirikanso pa zinthu zambiri, ndipo amene sakhulupirika pa zinthu zochepa adzakhala wosakhulupirika pa zinthu zambiri.
Kutena mwet su oaru in ma srik, ac fah oaru pac ke ma yohk; ac kutena mwet su sesuwos in ma srik ac fah sesuwos pac ke ma yohk.
11 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika pogwiritsa ntchito chuma cha dziko lapansi, ndani amene adzakusungitsani chuma chenicheni?
Kowos fin soaru in karingin mwe kasrup lun faclu, ac ku in lulalfongiyuk kowos fuka in karingin mwe kasrup pwaye uh?
12 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi chuma cha mwini wake, ndani amene adzakupatsani katundu wanuwanu?
Ac kowos fin soaru in karingin ma lun siena mwet, su ac ku in sot ma lowos?
13 “Palibe wantchito amene angatumikire mabwana awiri. Mwina iye adzadana ndi wina ndi kukonda winayo, kapena adzakhala wodzipereka kwa wina ndi kumunyoza winayo. Inu simungathe kutumikira Mulungu komanso ndalama nthawi imodzi.”
“Wangin mwet kulansap ku in kulansapu leum luo. El ac srunga sie, ac lungse el ngia; el ac pwaye nu sin sie, ac kwase el ngia. Kowos koflana kulansupu God ac mani.”
14 Afarisi amene ankakonda ndalama atamva zimenezi anamuseka Yesu.
Ke mwet Pharisee elos lohng ma inge elos isrun Jesus, mweyen elos lungse mani.
15 Yesu anawawuza kuti, “Inu ndi amene mumadzilungamitsa nokha pamaso pa anthu, koma Mulungu amadziwa mitima yanu. Zinthu zimene anthu amaziyesa zopambana, ndi zonyansa pamaso pa Mulungu.
Jesus el fahk nu selos, “Kowos sifacna oru lumowos in suwohs ye mutun mwet uh, tusruk God El etu insiowos. Tuh ma su mwet uh pangon yohk sripa selos, ma inge pilasr ye mutun God.
16 “Malamulo ndi Aneneri zinagwira ntchito mpaka nthawi ya Yohane. Kuyambira nthawi imeneyo, Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ukulalikidwa, ndipo aliyense akuyesetsa mwamphamvu kuti alowemo.
“Ma Sap lal Moses ac ma simusla lun mwet palu uh orekmakinyuk na nwe ke pacl lal John Baptais ah. In pacl sac me, Pweng Wo ke Tokosrai lun God uh fwackyak, ac mwet uh aikusiyak in utyak nu loac.
17 Nʼkwapafupi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zichoke kulekana ndi kuti kalemba kakangʼono kachoke mʼMalamulo.
Tusruktu, fisrasr tuh kusrao ac faclu in wanginla, liki sie akul srisrik ke sie leta ke Ma Sap uh in wanginla.
18 “Aliyense amene asiya mkazi wake ndi kukakwatira mkazi wina akuchita chigololo, ndipo mwamuna amene akwatira mkazi wosiyidwayo akuchitanso chigololo.”
“Kutena mukul su sisla mutan kial ac payuk nu sin sie pacna mutan, el orek kosro; ac sie mukul su payuk nu sin mutan sisila se, el oayapa orek kosro.
19 “Panali munthu wachuma amene ankavala zovala zofiirira za mtengowapatali ndipo ankakhala moyo wachisangalalo tsiku lililonse.
“Oasr sie mwet kasrup su nukum nuknuk na yohk molo, ac el moul in mut len nukewa.
20 Pa khomo la mpanda wake ankagonekapo munthu wopempha wotchedwa Lazaro, wazilonda thupi lonse
Na oasr pac sie mwet sukasrup pangpang Lazarus, su manol nuklana ke ruf, ac kwacna utukla el in muta ke mutunoa in lohm sin mwet kasrup sac,
21 ndipo ankafunitsitsa atadya zomwe zinkagwa pansi kuchokera pamene munthu wolemerayo amadyerapo. Agalu ankabweranso ndi kumanyambita zilonda zake.
mweyen el finsrak na elan ku in kang kutkut in mongo ma ac putatla liki tepu lun mwet kasrup sac. Kosro ngalngul uh ac tuku pac lohi ruf kacl uh.
22 “Nthawi inafika imene wopemphayo anamwalira ndipo angelo anamunyamula nakamuyika mʼmanja mwa Abrahamu. Munthu wolemerayo anamwaliranso ndipo anayikidwa mʼmanda.
Mwet sukasrup sac misa, ac lipufan uh usalla elan tuh muta siskal Abraham ke kufwa inkusrao uh. Mwet kasrup sac misa ac pukpuki el,
23 Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
ac ke el muta in Hades, yen ma el pulakin keok upa nu sel, el ngetak ac liyal Abraham yen loessula, ac Lazarus el muta siskal. (Hadēs g86)
24 Ndipo anafuwula kwa iye kuti, ‘Abambo Abrahamu, mundimvere chisoni ine ndipo mutumeni Lazaroyo kuti aviyike msonga ya chala chake mʼmadzi kuti aziziritse lilime langa, chifukwa ndikumva ululu mʼmoto muno.’
Na el pangyak ac fahk, ‘Papa Abraham! Pakomutuk, ac supwalma Lazarus elan isongya kufinpaol in kof an ac kahlye mutun louk in akoyohuyauk, tuh nga muta in keok lulap in e se inge!’
25 “Koma Abrahamu anayankha kuti, ‘Mwanawe kumbukira kuti nthawi yamoyo wako unalandira zinthu zako zabwino, pamene Lazaro analandira zinthu zoyipa, koma tsopano akusangalatsidwa kuno ndipo iwe uli mʼmazunzo.
Ac Abraham el fahk, ‘Ma nutik, esam lah pacl kom moul muta fin faclu ma nukewa wo ac fisrasr nu sum, a funu Lazarus el muta in ongoiya ac moul upa. Inge el muta insewowo inse, a kom muta in keok.
26 Ndipo kuwonjezera pa zonsezi, pakati pa inu ndi ife pali chiphompho chachikulu chimene chinayikidwa, kotero kuti amene akufuna kubwera kumeneko sangathe, kapena palibe amene angawoloke kuchokera kumeneko kudzafika kuno.’
Sayen ma inge, oasr luf na lulap se srikutelik, pwanang kutena mwet ma ac ke fahsrot ingewot nu yurum ac tia ku in orala, ac wangin pac mwet ac ku in tuku yurum me nu yorosr.’
27 “Iye anayankha kuti, ‘Ndipo ndikupemphani inu, abambo, mutumeni Lazaro ku nyumba ya abambo anga,
Na mwet kasrup sac fahk, ‘Fin ouingan nga kwafe sum, Papa Abraham, supwalla Lazarus nu in lohm sin papa tumuk,
28 pakuti ine ndili ndi abale asanu. Lolani iye akawachenjeze kotero kuti asadzabwere kumalo ano amazunzo.’
yen tamulel limekosr luk oasr we. Lela elan som ac sensenkunulos, tuh elos in mau tia tuku nu yen waiok se inge.’
29 “Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’
Abraham el fahk, ‘Kas lal Moses ac lun mwet palu uh oasr yorolos. Elos in porongo kas lalos an.’
30 “Iye anati, ‘Ayi, bambo Abrahamu, koma ngati wina ochokera kwa akufa adzapita kwa iwo, adzatembenuka mtima.’
Mwet kasrup sac fahk, ‘Papa Abraham, srakna sufal ma kom fahk ingan! Tuh fin oasr mwet se moulyak liki misa ac som nu yorolos, na elos fah ku in auliyak ac forla liki ma koluk lalos.’
31 “Anati kwa iye, ‘Ngati iwo samvera Mose ndi Aneneri, sadzakhulupirira ngakhale wina atauka kwa akufa.’”
Ac Abraham el fahk, ‘Elos fin tia lohngol Moses ac mwet palu uh, elos ac tia pac lulalfongi finne oasr mwet se moulyak liki misa.’”

< Luka 16 >