< Luka 16 >

1 Yesu anawuza ophunzira ake kuti, “Panali munthu wina wachuma amene kapitawo wake anzake anamuneneza kuti amawononga chuma chakecho.
Jesu ing a hubatkhqi venawh: “Thlang boei pynoet awm nawh anih a tangka ak khoemkung ing tangka poeih pe kang hy tinawh amik kqawn ce zahy.
2 Choncho anamuyitana ndi kumufunsa kuti, ‘Kodi nʼchiyani chimene ndikumva za iwe? Pereka tsatanetsatane wa ntchito yako, pakuti supitirizanso kukhala kapitawo wanga.’
Cedawngawh a boei ing khy nawh doet hy, ‘Na kawng kang zaak ve ikawmyihna a awmnaak? Tangka na khoem ce nim huh lah, ka tangka ak koemkung na am awm hly voel hyk ti,’ tina hy.
3 “Kapitawoyo analingalira kuti, ‘Kodi tsopano ndidzachita chiyani? Bwana wanga andichotsa ntchito. Ine ndilibe mphamvu zokwanira zolimira, komanso ine ndimachita manyazi kupempha.
Cedawngawh tangka ak khoemkung ing ‘ikawmyihna nu ka ti lah kaw? Ka boeipa ing ka bibi awm ni qoek hly sak hawh hy. Dek deng aham awm kak tha am awm koek, thlang a venawh kut dun aham awm chak koek bai nyng.
4 Ine ndikudziwa chimene ndidzachita kotero kuti, pamene ntchito yanga yatha pano, anthu adzandilandire mʼnyumba zawo.’
Ka sai hly taw sim hawh nyng, cawh ni bibi ani phawh awhtaw thlangkhqi ing kai ve ami im awh ami ni do hly hy,’ tihy.
5 “Choncho iye anayitana aliyense amene anali ndi ngongole kwa bwana wake. Iye anafunsa woyamba, ‘Kodi uli ndi ngongole yotani kwa bwana wanga?’
Cedawngawh a boeipa a ik-oeih ak pukhqi ce khy hy. Lamma cyk awhkaw thlang ce khy nawh, ‘Ka boeipa a koe ik-oeih izah nu nak pu peek? tina hy.
6 “Iye anayankha kuti, ‘Migolo yamafuta a olivi 800.’ “Kapitawo uja anamuwuza iye, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo, khala pansi msanga ndipo lemba kuti ndi migolo 400.’
Anih ing, ‘Olive situi boet zaqeet,’ tina hy. Law lah, ang tawnna ngawi nawhtaw zali na sai mai,’ tina hy.
7 “Kenaka iye anafunsa wachiwiri kuti, ‘Nanga iwe uli ndi ngongole yotani?’ “Iye ayankha kuti madengu a tirigu 1,000. “Iye anati, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo ndipo ulembepo 800.’
Cekcoengawh a pak khihnaak awhkaw thlang ce doet tlaih bai hy, ‘Nang law izah nak pu? tina hy. “Anih ing, ‘Canghum sum thongkhat,’ tina hy. Tangka ak pukung ing, ‘Nak punaak cahawn ce lo nawhtaw sum zaqeet na sai mai,’ tina hy.
8 “Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
Amak thym na bi ak bi tangka ak khoemkung ing cyihnaak ing bi a bi dawngawh a boeipa ing kyih am cah hy. Ve khawmdek thlangkhqi ing a mimah a ik-oeih ami sai awhtaw vangnaak khuiawh ak awmkhqi anglakawh awm cyi ngai uhy. (aiōn g165)
9 Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
Nangmih a venawh ka nik kqawn peek khqi, pyi sainaak aham khawmdek boeinaak ce hawna lah uh, cawh ni ce mihkhqi boeih a boeih coengawh, a mingmih ing kumqui awmnaak hun awh nangmih ce ani do hly khqi hy. (aiōnios g166)
10 “Amene akhulupirika pa zinthu zochepa akhoza kukhulupirikanso pa zinthu zambiri, ndipo amene sakhulupirika pa zinthu zochepa adzakhala wosakhulupirika pa zinthu zambiri.
U awm ik-oeih a khoehca awh ypawm na ak awm taw ik-oeih khawzah awh awm ypawm na awm hy, cehlai ik-oeih a khoehca awh ypawm na amak awm taw ik-oeih khawzah awh awm upvoet na awm hy.
11 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika pogwiritsa ntchito chuma cha dziko lapansi, ndani amene adzakusungitsani chuma chenicheni?
Khawmdek boeinaak awh zani ama ypawm awhtaw, u ing nu boeimangnaak tang tang ce ani khoem sak kaw?
12 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi chuma cha mwini wake, ndani amene adzakupatsani katundu wanuwanu?
Thlang a ik-oeih awh ypvoet na na awm coengawh taw, u ing nu nang ce ik-oeih a ni peek kaw?
13 “Palibe wantchito amene angatumikire mabwana awiri. Mwina iye adzadana ndi wina ndi kukonda winayo, kapena adzakhala wodzipereka kwa wina ndi kumunyoza winayo. Inu simungathe kutumikira Mulungu komanso ndalama nthawi imodzi.”
Tyihzoeih thlang pynoet ing boei pakkhih a bi pakkhih am bawk thai hy. Pynoet ce sawh na kawmsaw pynoet ce lungna kaw, am awhtaw pynoet ce ypna kawmsaw pynoet taw hep kaw. Khawsa bi ingkaw tangka bi am bawk hly thai qen hyk ti,’ tinak khqi hy.
14 Afarisi amene ankakonda ndalama atamva zimenezi anamuseka Yesu.
Tangka amik thintlawhnaak Farasikhqi ing ce ak awi ce a ming zaak awh Jesu ce qaih na uhy.
15 Yesu anawawuza kuti, “Inu ndi amene mumadzilungamitsa nokha pamaso pa anthu, koma Mulungu amadziwa mitima yanu. Zinthu zimene anthu amaziyesa zopambana, ndi zonyansa pamaso pa Mulungu.
Jesu ing a mingmih a venawh, “Thlang amik huh awh nangmih ing thlakdyng na sa qu uhyk ti, cehlai Khawsa ing nangmih ak kawlung ce sim hy. Thlang ing a phu ak tlo soeih na a taak ce Khawsa mik huh awhtaw tyih cu hy.
16 “Malamulo ndi Aneneri zinagwira ntchito mpaka nthawi ya Yohane. Kuyambira nthawi imeneyo, Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ukulalikidwa, ndipo aliyense akuyesetsa mwamphamvu kuti alowemo.
Johan a khuk dy ni anaa awi ingkaw tangkakhqi ca qee ce amik khypyi hy. Cekcoengawh kawng Khawsa ram awithang ce khypyi hawh uhy, thlang boeih ing ce ak khuiawh kun aham tha lo uhy.
17 Nʼkwapafupi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zichoke kulekana ndi kuti kalemba kakangʼono kachoke mʼMalamulo.
Anaa awi awhkaw a dek zet ce ang qeng anglakawhtaw khawk khan ingkaw khawmdek ang qeng zoei bet kaw.
18 “Aliyense amene asiya mkazi wake ndi kukakwatira mkazi wina akuchita chigololo, ndipo mwamuna amene akwatira mkazi wosiyidwayo akuchitanso chigololo.”
U ingawm a zu thla nawh nuk chang a lawh awhtaw samphaih hy, thlang a zuk thlak ak zunaak awm samphaih toeng toeng hy.
19 “Panali munthu wachuma amene ankavala zovala zofiirira za mtengowapatali ndipo ankakhala moyo wachisangalalo tsiku lililonse.
Kuiqang thlang pynoet awm nawh hik thim ingkaw hi ak leek leek ing myngawi ang thoeihcam qu coengawh awm hly poepa hy.
20 Pa khomo la mpanda wake ankagonekapo munthu wopempha wotchedwa Lazaro, wazilonda thupi lonse
Ak chawmkeng a keng awh Lazaru ak mingnaak kut ak dun thlang pynoet ce awm hy, a pum boeih na phoei ing bawm nawh,
21 ndipo ankafunitsitsa atadya zomwe zinkagwa pansi kuchokera pamene munthu wolemerayo amadyerapo. Agalu ankabweranso ndi kumanyambita zilonda zake.
kuiqang a caboei awhkaw ak tla awkdik aidik ce ai aham ngaih hy. Uikhqi ing ak phoei ce leek pe uhy.
22 “Nthawi inafika imene wopemphayo anamwalira ndipo angelo anamunyamula nakamuyika mʼmanja mwa Abrahamu. Munthu wolemerayo anamwaliranso ndipo anayikidwa mʼmanda.
Cawhkaw kut ak dun thlang ce thi nawh khan ceityihkhqi ing Abraham a venna khyn uhy. Kuiqang thlang awm thi lawt nawh pup uhy.
23 Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
Hell khuina khuikha a sim cilh cilh awh ak hla nakawng Abraham ingkaw a venawh Lazaru ak awm ce hu hy. (Hadēs g86)
24 Ndipo anafuwula kwa iye kuti, ‘Abambo Abrahamu, mundimvere chisoni ine ndipo mutumeni Lazaroyo kuti aviyike msonga ya chala chake mʼmadzi kuti aziziritse lilime langa, chifukwa ndikumva ululu mʼmoto muno.’
Ak khy doe na, ‘Ka pa Abraham, qeennaak ing Lazaru ce tyi nawhtaw tui awh a kutply pui seitaw kam lai ve ci law sak lah seh, vawhkaw mai awh ve khuikha cip cip hawh nyng ve,’ tina hy.
25 “Koma Abrahamu anayankha kuti, ‘Mwanawe kumbukira kuti nthawi yamoyo wako unalandira zinthu zako zabwino, pamene Lazaro analandira zinthu zoyipa, koma tsopano akusangalatsidwa kuno ndipo iwe uli mʼmazunzo.
Cehlai Abraham ing, ‘Ka capa, na hqing khui pyt awh ik-oeih ak leek leek hu tiksaw, Lazaru taw ik-oeih che a huh ce poek lah, cehlai tuh awhtaw anih ing ngaihdingnaak hu nawh nang taw khuikha hyk ti.
26 Ndipo kuwonjezera pa zonsezi, pakati pa inu ndi ife pali chiphompho chachikulu chimene chinayikidwa, kotero kuti amene akufuna kubwera kumeneko sangathe, kapena palibe amene angawoloke kuchokera kumeneko kudzafika kuno.’
Vekkhqi boeih coengawh, nang ingkaw kaimih anglakawh lawk-kqawng ak dung soeih awm hy, cedawngawh vawhkawng nang a venna u awm am cet thai hy, nang a venna kawng vena u awm am law thai bai hy,’ tina hy.
27 “Iye anayankha kuti, ‘Ndipo ndikupemphani inu, abambo, mutumeni Lazaro ku nyumba ya abambo anga,
Cawh anih ing, ‘cawhtaw ka pa Abraham, qeennaak thoeh law nyng, Lazaru ce Ka pa im na tyi cang lah,
28 pakuti ine ndili ndi abale asanu. Lolani iye akawachenjeze kotero kuti asadzabwere kumalo ano amazunzo.’
Ka naa thlang pumha awm hyn hy. Vawhkaw khuikha simnaak a hun awh a mami lawnaak thai aham anih ing kqawn law pe cang lah seh nyng,’ tina hy.
29 “Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’
Abraham ing, ‘Mosi ingkaw tawnghakhqi ta hawh usaw ti a; cekkhqi ak awi ce ngai mai u seh,’ tina hy.
30 “Iye anati, ‘Ayi, bambo Abrahamu, koma ngati wina ochokera kwa akufa adzapita kwa iwo, adzatembenuka mtima.’
Anih ing, ‘Amni, ka pa Abraham, thlak thi ak khuiawh kawng thlang pynoet oet a mingmih a venna a ceh mantaw thawlh zut kawm uh,’ tina hy.
31 “Anati kwa iye, ‘Ngati iwo samvera Mose ndi Aneneri, sadzakhulupirira ngakhale wina atauka kwa akufa.’”
Abraham ing a venawh, ‘Mosi ingkaw tawnghakhqi ak awi ce a maming ngai awhtaw, thihnaak ak khuiawh kawng thlang tho nawh kqawn pe bai seiawm am ngai hly uhy,’ tina hy,” tinak khqi hy.

< Luka 16 >