< Luka 15 >

1 Tsopano amisonkho ndi “ochimwa” ankasonkhana kudzamvera mawu ake.
Lani, ke a lonpo gaala leni ya tuonbiiddanba n sieni den kpendi Jesu kani, ki cengi o maama.
2 Koma Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo amangʼungʼudza nati, “Munthu uyu amalandira ochimwa ndi kudya nawo.”
Ke farisieninba leni ti yikodi tundkaaba ji bulni bulni, ki tua “O nilo ne gaani ti biidi danba hali ki di leni ba.”
3 Ndipo Yesu anawawuza fanizo ili:
Ke Jesu pua ba ya makpanjama ne, ki maadi ba
4 “Tiyerekeze kuti mmodzi mwa inu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi yatayika, kodi iye sangasiye 99 zija kutchire ndi kupita kukafuna yotayikayo mpaka atayipeza?
“O laa nilo i siiga nni n baa pia pee kobga, ki biani payendo, ki kan ŋa piiyia n pee yia yeni, ku muagu nni, ki guani ki kpaani ya pia n bodi hali ki ban la o.
5 Ndipo iye akayipeza, amayinyamula pa phewa lake mwachimwemwe
O ya la o, o ba bugi o o buapiadi po, ki mangi o pali boncianla.”
6 ndi kupita kwawo. Kenaka amayitana anzake ndi anansi pamodzi, ndi kuti, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza nkhosa yanga yotayika ija.’
O ya pundi denpo, ba yini o dɔnlinba leni o kuantalieba ki maadi ba, “Mangi mani i pala leni nni, kelima n la n pia yua bi bodi.
7 Ine ndikukuwuzani kuti momwemonso kudzakhala chikondwerero chachikulu kumwamba chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima kusiyana ndi anthu olungama 99 amene ali otembenuka mtima kale.”
Lanyapo, N yedi yi, ke li pamanli baa ye tanpoli kelima biiddanyendo lebdi o pali ki cie niteginkaaba piiyia n biyia yaaba n ki buali pali lebdima.
8 “Kapena tiyeni tifanizire mayi amene anali ndi ndalama zasiliva khumi ndipo imodzi nʼkutayika, kodi sayatsa nyale ndi kusesa mʼnyumba ndi kufuna mosamalitsa mpaka atayipeza?
Bii, o laa pua n baa pia dibala piiga, ki biani dibayenli, ki kan cuoni ki fidsanga, ki tigni li dieli ki fiidi bonŋanla hali ki ban la li?
9 Ndipo pamene wayipeza, amayitana anzake, ndi anansi pamodzi nati, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza ndalama yanga yotayika ija.’
O ya la la, o ba yini o dɔnlinba leni o kuantalieba, ki maadi ba, “Mangi mani i pala leni nni, kelima n la n dibali yaali bi bodi.”
10 Momwemonso, Ine ndikukuwuzani kuti angelo a Mulungu amakondwera kwambiri chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima.”
N yedi yi, biiddanyendo ya lebdi o pali, li tie pamancianli i, U Tienu malekinba po.”
11 Yesu anapitiriza kunena kuti, “Panali munthu amene anali ndi ana aamuna awiri.
Ke Jesu maadi, “Nilo den pia bijaba lie,
12 Wamngʼonoyo anati kwa abambo ake, ‘Abambo, patseni gawo langa la chuma chanu.’ Ndipo iye anawagawira awiriwo chuma chawo.
o bonwaalo po den yedi o báa, “N Báa, bɔgdi n faali biinu ki teni nni mɔlane” Ke o bɔgdi ba o piama.
13 “Pasanapite nthawi, wamngʼonoyo anasonkhanitsa chuma chake chonse, napita ku dziko lakutali ndipo kumeneko anayamba kumwaza chuma chake mʼnjira zachitayiko.
Lan tieni dana waamu, ke o waalo po baani o bonkubkaali ki gedi hali ya dogu n fagi, lan dogu po i, ke o biidi o ligi, ki daa yaali n ki tie o po bonbuakaali mɔno, ki biidi o ligi mi bibiadyema nni.
14 Iye atawononga zonse, kunagwa njala yoopsa mʼdziko lonselo ndipo anayamba kusauka.
Wan dini o ligi ki gbeni, mi konbiadma ń baa li dogu nni, mi koma ń gbadi o.
15 Iye anapita kwa nzika ina ya dzikolo nakakhala naye ndi kumagwira ntchito, amene anamutumiza ku munda kukadyetsa nkhumba.
Ke o gedi ki mia li tuonli li dogtielo bá kani, ke o kaani o o kuanu nni ke wan ya guu i duoli.
16 Iye analakalaka atakhutitsa mimba yake ndi makoko amene nkhumbazo zinkadya, koma panalibe wina amene anamupatsa kanthu.
O den ya baa ti duojiedi, o den ba di leni li pamanli, ama obá nan den ki puni o sanu.
17 “Maganizo ake atabweramo, iye anati, ‘Ndi antchito angati a abambo anga amene ali ndi chakudya chimene amadya nʼkutsalako ndipo ine ndili pano kufa ndi njala!
Ama ki bonjaga yeni yama ń den guani, ke o maadi o pali nni, “N báa pia naacenba biŋa i, ke bi di ke jiema ki muani ba, ke mini nan ba kpe leni mi koma nekanba!
18 Ine ndinyamuka ndi kubwerera kwa abambo anga ndipo ndikati kwa iwo: abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi kwa inu.
“N ba siedi ne, ki guani ki kuni n báa po, ki ban maadi o, “N Báa, n biidi U Tienu po leni a nunga nni.
19 Ndine wosayeneranso kutchedwa mwana wanu; munditenge ngati mmodzi wa antchito anu.’
N ji ki dagdi min ya tie a biga, ga nni min tua a naacenba nni yendo.
20 Ndipo iye ananyamuka ndi kupita kwa abambo ake. “Koma iye akanali patali, abambo ake anamuona ndipo anamvera chisoni; anathamangira mwanayo, namukumbatira ndi kupsompsona.
Ke ki bonjaga yeni siedi ki kuni o báa po. Wan dá den paa hali fagma, o báa den la o, ke ti niñipadi cuo o, ke o sani ki wobi o, ki muadi o tankpina po.
21 “Mwanayo anati, ‘Abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi inunso. Ine sindiyenera konse kutchedwa mwana wanu.’
Ke ki biga maadi o, “N Báa, n biidi U Tienu po leni a nunga nni. N ji ki dagdi ŋan yini nni a biga.
22 “Koma abambowo anati kwa antchito ake, ‘Fulumirani! Bweretsani mkanjo wabwino kwambiri ndipo mumuveke. Muvekeni mphete ndi nsapato.
Bibáa ń maadi o naacenba, “Cua mani leni liadŋanli, ki lani o, ki pilini o li nubiñinli leni ti taacaadi.
23 Bweretsani mwana wangʼombe wonenepa ndipo iphani. Tiyeni tikhale ndi phwando ndi kukondwerera.
Diidi mani natonbikpanbili, ki kpa, ke tin tieni mi jaanma, ki mangi ti pala.
24 Pakuti mwana wangayu anali wakufa, ndipo ali ndi moyonso; iye anatayika ndipo wapezeka.’ Chomwecho anayamba kukondwerera.
Kelima, n biga den kpe, ki ji pia li miali, o den bodi, ke n guani ki la o. Ke bi ji cili mi jaanma.
25 “Nthawi imeneyi, mwana wake wamkulu uja anali ku munda. Iye atafika pafupi ndi nyumba, anamva anthu akuyimba ndi kuvina.
Li sua ke o kpelo bi ye u kuanu po. Wan kpendi, ki nagi deni, ke o gbadi ki ciaga yani leni ku jeligu.
26 Ndipo iye anayitana mmodzi wa antchito, namufunsa chimene chimachitika.
Wan yini naacenyendo ki buali lanya bona niima nni.
27 Iye anayankha kuti, ‘Mʼbale wako wabwera ndipo abambo ako apha mwana wangʼombe wonenepa chifukwa wabwera wamoyo ndipo ali bwino.’
O naaciemo ń maadi o, “A waalo n kpeni, ke a báa kpaá li nakpanbili ki tieni mi jaanma kelima o guani ki kpeni leni laafia.”
28 “Mwana wamkulu anakwiya ndipo anakana kulowa. Chomwecho abambo ake anatuluka ndi kumudandaulira.
ki bikpelga pali ń be, wan yie ke o kan kua deni, o báa ń ña ki baagi o.
29 Koma iye anayankha abambo ake kuti, ‘Taonani! Zaka zonsezi ndakhala ndikukutumikirani kugwira ntchito yowawa ndipo palibe pamene sindinamvere malamulo anu. Koma inu simunandipatse ngakhale mwana wambuzi kuti ine ndichite phwando ndi anzanga.
Ama o kpelo ń jiini ki maadi o báa, “Diidi, bina ŋa n yeni, ke n tuuni a po a tuona, n nan ki kpeli ki tudi a nunga nni, Ama a nan ki kpeli ki puni nni bá ŋɔtonpanli, ke min tieni mi jaanma leni n dɔnlinba,
30 Koma pamene mwana wanu uyu amene wawononga chuma chanu ndi achiwerewere wabwera ku nyumba, inu mwamuphera mwana wangʼombe wonenepa.’”
Ama A bijua yua n biidi a ŋalmani yeni a poconcona ń kpeni, ke a nan kpaá o po naatonkpanbili.
31 Abambowo anati, “Mwana wanga, iwe umakhala ndi ine nthawi zonse ndipo zonse ndili nazo ndi zako.
O báa ń maadi o, “N bijua, fini li ye leni nni daali kuli, ke min die yaali kuli tie a yaali i.
32 Koma tinayenera kukondwera ndi kusangalala, chifukwa mʼbale wako uyu anali wakufa ndipo ali ndi moyonso; iye anali wotayika ndipo wapezeka.”
Ama, li bi dagdi leni tin tieni mi jaanma, ki mangi ti pala, kelima a waalo ne den kpe, ki ji pia li miali mɔla, O den bodi ke ti guani ki la o.

< Luka 15 >