< Luka 13 >

1 Nthawi yomweyo panali ena amene analipo omwe amamuwuza Yesu za Agalileya amene magazi awo Pilato anawasakaniza ndi nsembe zawo.
Khunsikhi gugugwa, khwale na vanu avambulile ukhuta avagalatia avu u Pilato avabudile nu khuhanjaniya nu khisa gwavo ne ni vyavupe.
2 Yesu anayankha kuti, “Kodi mukuganiza kuti Agalileya amenewa anali ochimwa kwambiri kuposa Agalileya ena onse chifukwa anavutika mʼnjira iyi?
U Yisu aandile nu khuvavula, “Lino mwita avagalatia avo vale nu vutula nogwa ukhulutilila avagalatia avange voni khe mene vupilile nu vavivi iuwa?
3 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.
Bakho, nikhuvavula, nete mungave samkhute, umwe ayumwiyaga vutevule.
4 Kapena anthu 18 aja amene anafa nsanja ya Siloamu itawagwera, kodi mukuganiza kuti iwo aja anali ochimwa kwambiri kuposa onse amene amakhala mu Yerusalemu?
Upu vale avanu “18” khusiloomu upu unara gwagyile nu khuvabudi pumsaga ukhuta avene vale nuvulula nogwa ukhulutilila khu vanu avange khu Yerusalemu?
5 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.”
Bakho, une ninchova, mungalekhe ukhukhuta, umwe mwivoni punikhwavela.
6 Kenaka Iye anawawuza fanizo kuti, “Munthu wina anali ndi mtengo wamkuyu, umene anadzala mʼmunda wamphesa, ndipo Iye anapita kukayangʼana zipatso, koma sanazipeze.
U Yisu avavulile ikhikhwani ikhi, “Umunu umo ale ne libikhi avyalile khu khyalo khya mwene nu khuluta khulonda isekhe khukya na sapate.
7 Tsono kwa munthu amene amasamalira munda wamphesawo anati, ‘Kwa zaka zitatu tsopano ndakhala ndikubwera kudzafuna chipatso pa mtengo uwu ndipo sindinachipeze. Udule! Nʼchifukwa chiyani ukuwononga nthaka?’
Akhambula uvi alolelaga ikyalo, 'Lola, khu miakha gi datu nainchile nukhugela ukhulonda isekhe khu bikhi ugwa sanapate khinu. Udumule. Ulwa khuva gutela uvuvivi uwa khilunga?
8 “Munthuyo anayankha kuti, ‘Bwana, tawusiyani kwa chaka chimodzi chokha ndipo ine ndikumba ngalande mozungulira ndi kuthira manyowa.
Uvi lolela ikyalo aandile nukhunchova ukhuta, 'Ugulekhe umwakha ugu nilinilile nu khuvikha imbolela, pakyanya.
9 Ngati udzabale zipatso chaka chamawa, zili bwino! Koma ngati sudzabala, pamenepo mudzawudule.’”
Gunguhupe isekhe umwakha ugukhwincha lunovu, pu; gungave saguhupa, ugide!”
10 Pa Sabata Yesu ankaphunzitsa mʼsunagoge ina,
Lino u Yisu ale nu khumanyisya khu vanu vaninye na vasinagogi khusikhi ugwa sabato.
11 ndipo momwemo munali mayi amene anali ndi mzimu woyipa umene unamudwalitsa zaka 18. Iye anali wokhota msana ndipo samatha kuweramuka ndi pangʼono pomwe.
Lola, alepwale ujiu umo uvi ale ne miakha “18” ale ne mumbula inchafu, nu mwene ale abudiwe imbula mbaubo iyave nchaga na khukhwima.
12 Yesu atamuona anamuyitana kutsogolo ndipo anati kwa iye, “Amayi, mwamasulidwa ku mavuto.”
U Yisu vuambwene, akhamwilanga, “akhambula, “Jiu, uvikhwe ukhuva mbulegefu ukhuhuma imbupepe wakho.”
13 Kenaka anasanjika manja ake pa iye, ndipo nthawi yomweyo anawongoka nayamika Mulungu.
Akhambikha amavokho gwa mwene pa kyanya pa mbili ugwa mwene akhimikha amavokho nu khuginiya Unguluve.
14 Chifukwa cha kuyipidwa kuti Yesu anachiritsa pa Sabata, wolamulira sunagoge anati kwa anthu, “Pali masiku asanu ndi limodzi ogwira ntchito. Choncho bwerani kuti mudzachiritsidwe masiku amenewo osati pa Sabata.”
Pu umbaha va sinagogi avipile ukhuva u Yisu aponinche umunu isikhu iya sabato. Lino umbaha va khilunga akhanda akhavavula avanyalulundamano, “Khulo isikhu 6 incha khuvomba imbombo. Mwinchage khupokhiwa wonela isikhu iya sabato. '
15 Ambuye anamuyankha kuti, “Iwe wachiphamaso! Kodi nonsenu simumasula pa Sabata ngʼombe zanu kapena bulu kumuchotsa mʼkhola ndi kupita naye kukamupatsa madzi?
Utwa akhanda nu khunchava, “avanyagila vasikhuli nu mo ukhudindula ipunda yakho, isenga ukhuhuma khulipalo nu khwalongoncha ukhulua khwinuwa isikhu iya sabato?
16 Nanga mayiyu, amene ndi mwana wa Abrahamu, ndipo anamangidwa ndi Satana zaka 18, kodi siwoyenera kuti amasulidwe msinga imeneyi pa tsiku la Sabata?”
Lino avahincha va Abrahamu, avuvene undugu akhungile khu miakha “18” lino wanogilwe ikhi khungilwa ikhyo khilekhe ukhudinduliwa isikhu iya sabato?”
17 Atanena izi, onse omutsutsa anachititsidwa manyazi, koma anthu anakondwera ndi zodabwitsa zonse zimene Iye anazichita.
Vu inchova amamenyu ago vala voni avabelile vakhavona soni, pu avanyalulundamano voni na vange valulutile ulwakhuva amambo agakhudega agu avombile.
18 Kenaka Yesu anafunsa kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani? Kodi Ine ndingawufanizire ndi chiyani?
U Yisu akhanchova, “Uvutwa wa Nguluve vukhwanine ne khikhi, vuwesya ukhukhwananincha ne khikhi?
19 Uli ngati mbewu ya mpiru, imene munthu anatenga ndi kudzala mʼmunda mwake. Inakula, nʼkukhala mtengo, ndipo mbalame zamlengalenga zinakhala mʼnthambi zake.”
Nilindi mbegu iya haradai iyiatolile umunu umo nu khuyivyala mukyalo kya mwene nu khumela ukhuva libikhi ilivaha, ni ifidehe ifya khukhyanya vikhajenga uvufumba wavo mumasesi aga bikhi.
20 Iye anafunsanso kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu ndingawufanizire ndi chiyani?
Hange akhanchova, “Nu khukhwananincha nu vutwa uwa Nguluve?
21 Uli ngati yisiti amene mayi anatenga ndi kusakaniza ndi ufa wambiri mpaka anafufumitsa ufawo.”
Yale ukhuta khiluve ikhi udala atolile nu khuhanchaniya khuvigelelo fidatu “3” ifya vutine nu khutoga.”
22 Ndipo Yesu anayendayenda mʼmizinda ndi mʼmidzi, kumaphunzitsa pamene Iye ankapita ku Yerusalemu.
U Yisu agendile imbunchengene vijiji munjila vuiluta khu Yerusalemu nu khuvamanyisya.
23 Wina anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndi anthu ochepa okha amene adzapulumutsidwe?” Iye anawawuza kuti,
Umunu umo avunchehe, “Itwa, vuvale avayakhiva vipokhiwa?” Lino akhavavula,
24 “Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza, chifukwa ndikukuwuzani kuti ambiri adzafuna kulowa koma sadzatha kutero.
“Witange ukhwingila ukhugendela undyango usekhele, ulwakhuva vingi yu vigela nu khusita ukhwingila.
25 Nthawi yomwe mwini nyumba adzayimirira ndi kutseka chitseko, inu mudzayima kunja kugogoda ndi kudandaula kuti, ‘Bwana, tatitsekulirani khomo.’ “Koma Iye adzayankha kuti, ‘Ine sindikukudziwani ndipo sindikudziwanso kumene mwachokera.’
Nu sikhi ugwa undoleli va nyumba ukhima nu khudinda undyango, pu mukhwima khunji nu khugonga ndindulilo nu khunchova, Itwa, Itwa, tudindulile, umwene akhanda nu khuvavula, sanivamanyile umwe nu khuvuhuma.'
26 “Ndipo inu mudzati, tinkadya ndi kumwa ndi inu ndipo munkaphunzitsa mʼmisewu yathu.
Pu yumwinchova, Twalile nu khunywa khuvulongoo khu vene, wa manyisye khuvunchenge uweto.”
27 “Koma Iye adzayankha kuti, ‘Ine sindikukudziwani ndipo sindikudziwanso kumene mwachokera. Chokereni inu nonse ochita zoyipa!’
Pu umwene akhavanda, sanivamanyile ukhumwihuma, hega khulyune, umwe mwivavomba imbivi!'
28 “Mudzalira ndi kukuta mano mukadzaona Abrahamu, Isake ndi Yakobo ndi aneneri onse ali mu ufumu wa Mulungu koma inuyo mutaponyedwa kunja.
Khulova nu khulila nu khuheveta amino khusikhi ugulava mkhuvavona u Abrahamu, Isaka, Yakobo na avanyaalago voni khu vutwa u wa Nguluve, nu umwe yumwe mutagiwe khunji.
29 Anthu adzachokera kummawa ndi kumadzulo, kumpoto ndi kummwera, kudzakhala pa phwando mu ufumu wa Mulungu.
Valincha ukhuhua khu vuhumo, na khuvusemo, khunena na khusikha, nu khugatalukha khu khisancha iya khya khulya ikya pa khimihe khu vutwa uwa Nguluve.
30 Ndithudi otsirizira ndiye adzakhale oyambirira, ndipo oyambirira ndiye adzakhale otsirizira.”
Ne lumanyile ukhuta uva khuvumalilo iva vakhuvumalilo.”
31 Pa nthawi imeneyo Afarisi anabwera kwa Yesu ndipo anati kwa Iye, “Chokani malo ano ndipo pitani kumalo ena aliwonse. Herode akufuna kukuphani.”
Usikhiusupi, pongela gwiva gwaMafarisayo vainchilenu khumbula, “Luta nu khuhega apa ulwakhuva u Herode inogwa ukhubuda.”
32 Iye anayankha kuti, “Pitani kawuzeni nkhandweyo, Ine ndikutulutsa ziwanda ndi kuchiritsa anthu lero ndi mawa ndipo tsiku lachitatu ndidzakwaniritsa cholinga changa.”
U Yisu akhanchova, “Mulutage mukhambule imbweha yila, 'Lola, nikhugavinga amanguluve nu khuvomba ukhuponiya ilelo na khilavo ne isikhu iya datu yu nivomba uvigane wango.
33 Mʼnjira ina iliyonse, Ine ndiyenera kupitirira ulendo wanga lero, mawa ndi mkuja. Zoona nʼzakuti mneneri sangafere kunja kwa Yerusalemu.
Pu usikhi ugwa venchaga unonu khu khuvunogwe wango ukhuluta ilelo, khilavo na khusikhu iyikhongile khuvala avasavisayiwa ukhubuda unyamalago khutali ne Yerusalemu.
34 Iwe Yerusalemu, Yerusalemu! Umapha aneneri ndi kuwagenda miyala anthu amene atumizidwa kwa iwe. Nthawi zambiri ndakhala ndikufuna kusonkhanitsa ana ako pamodzi, monga nkhuku imasonkhanitsira anapiye pansi pa mapiko ake, koma iwe sunafune!
Yerusalemu, Yerusalemu, veni uvibuda avanyamalago nu khuvatova na mawe vala avasuhiwa khulimwe, khalikhalingi nenogilwe ukhuvalunde maniya avana avadebe khulyu mwe ndi hukhu vuyilundamaniye inyamahukhu ifya pasi mumapapalilo aga hukhu, ingawa samwa nogwe ili.
35 Taona, nyumba yako yasanduka bwinja. Ine ndikukuwuza kuti, sudzandionanso mpaka pamene udzati, “Wodala amene akubwera mʼdzina la Ambuye!”
Lola, uvunjenge wakho vulekhiwe. Nune nikhuvavula, samukhawesye ukhumbona nu muyakhiva mwinchova 'Asayiwe uvikhincha khulitawa ilya ITWA.'”

< Luka 13 >