< Levitiko 22 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
OLELO mai la hoi o Iehova ia Mose, i mai la,
2 “Uza Aaroni ndi ana ake kuti azilemekeza zinthu zopatulika zimene Aisraeli azipereka kwa Ine, kuti asayipitse dzina langa loyera. Ine ndine Yehova.
E olelo aku ia Aarona, a i kana mau keiki, e hookaawale lakou ia lakou iho mai na mea hoano o na mamo a Iseraela, i ole ai lakou e hoino mai i ko'u inoa hoano i na mea a lakou i hoano mai ai no'u; owau no Iehova.
3 “Uwawuze kuti ngati wina aliyense mwa zidzukulu zawo mʼmibado yonse imene ikubwera adzayandikira zinthu zopatulika zimene ana a Israeli apereka kwa Yehova, ali wodetsedwa, ameneyo achotsedwe pamaso pa Yehova. Ine ndine Yehova.
E olelo aku ia lakou, O ka mea o ka oukou mau keiki a pau iwaena o ko oukou mau hanauna, e hele i na mea hoano a na mamo a Iseraela i hoolaa aku ai ia Iehova, me kona haumia maluna ona, e okiia'ku oia mai ko'u alo aku: owau no Iehova.
4 “Munthu aliyense mwa zidzukulu za Aaroni amene ali ndi khate kapena amatulutsa zoyipa mʼthupi mwake, asadye zinthu zopatulika mpaka atayeretsedwa. Wansembe angakhale wodetsedwa atakhudzana ndi chinthu chimene chadetsedwa ndi chinthu chakufa kapena kukhudza munthu amene wataya umuna,
O kela kanaka, keia kanaka he keiki a Aarona, he lepero, a he hilo kahe kona; aole ia e ai i na mea hoano a hiki i kona maemae ana. A o ke kanaka hoopa aku i ka mea haumia no ka mea make, a o ke kanaka ua hele aku kona anoano mai ona aku;
5 kapena kukhudza chilichonse chokwawa chomwe chimadetsa munthu, kapena kukhudza munthu amene angamudetse, kapenanso kukhudza kanthu kena kalikonse kodetsedwa.
A o ke kanaka hoopa aku i ka mea kolo e haumia ai, a i ke kanaka paha e haumia ai, o kela haumia keia haumia kona;
6 Tsono ngati wansembe angakhudze chilichonse mwa zimenezi ndiye kuti adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Asadye chopereka chilichonse chopatulika mpaka atasamba thupi lake lonse.
O ke kanaka i pa aku i kekahi o ia mau mea, e haumia no ia a hiki i ke ahiahi, aole ia e ai i na mea hoano, ke holoi ole oia i kona io i ka wai.
7 Munthuyo adzakhala woyeretsedwa pamene dzuwa lalowa, ndipo angathe kudya chopereka chopatulikacho popeza ndi chakudya chake.
A napoo ka la, e maemae no ia, a mahope iho e ai no oia i na mea hoano; no ka mea, o kana ai no ia.
8 Wansembe sayenera kudya chinthu chofa chokha kapena chojiwa ndi chirombo kuopa kuti angadzidetse ndi chakudyacho. Ine ndine Yehova.
O ka mea make wale, a o ka mea i nahaeia, aole oia e ai ia, e hoohauraia'i ia ia iho: owau no Iehova.
9 “‘Choncho ansembe azisunga malamulo angawa kuti asapezeke wolakwa ndi kufa chifukwa chopeputsa malamulowa. Ine ndine Yehova, amene ndimawayeretsa.
E malama hoi lakou i ka'u oihana, o hooili lakou i ka hewa maluna ona, a make, ke hoohaumia Iakou ia mea: na'u ua Iehova lakou e hoano nei.
10 “‘Aliyense amene si wabanja la wansembe, kaya ndi mlendo wa wansembe, kapena wantchito wake, asadye chopereka chopatulika.
Aole e ai ka malihini i ka mea hoano; o ko ke kahuna mea e noho malihini mai, a o ke kauwa hoolimalima, aole no e ai i ka mea hoano.
11 Koma kapolo amene wagulidwa ndi ndalama kapena kubadwira mʼbanja la wansembe angathe kudya chakudya cha wansembeyo.
Aka ina e kuai ke kahuna i ke kanaka me kana kala, e ai no oia ia, a me ka mea i hanau maloko o kona hale; o lakou ke ai i kana ai.
12 Mwana wamkazi wa wansembe amene wakwatiwa ndi munthu amene si wansembe, asadyeko nsembe zopatulikazo.
Ina e mare ke kaikamahine a ke kahuna i ka malihini, aole oia e ai i ka alana o na mea hoano.
13 Koma mwana wamkazi wa wansembe amene ali wamasiye kapena wosudzulidwa, ndipo alibe mwana, komanso anabwerera ku nyumba ya abambo ake monga pa nthawi ya utsikana wake, angathe kudya chakudya cha abambo ake. Mlendo asadye chakudya chopatulika.
Aka ina he wahinekanemake ke kaikamahine a ke kahuna, a ua hemo paha me ke keiki ole, a ua hoi mai i ka hale o kona makuakane, e like me kona wa kamalii, e ai no oia i ka ai a kona makuakane; aka aole ka malihini e ai ia mea.
14 “‘Ngati munthu wina aliyense adya chopereka chopatulika mosadziwa, munthuyo amubwezere wansembe chinthu chopatulikacho ndipo awonjezerepo limodzi la magawo asanu a chinthucho.
A ina e ai ke kanaka i ka mea hoano, me ka ike ole, alaila e hui aku oia i ka hapa lima me ia, a e haawi aku i ke kahuna me ka mea hoano.
15 Choncho ansembe asayipitse zopereka zopatulika za Aisraeli zimene apereka kwa Yehova
Aole lakou e hoohaumia i ka na mamo a Iseraela mau mea hoano a lakou i hoolaa ai ia Iehova:
16 ndipo asachimwitse ndi kupalamulitsa Aisraeli powalola kudya zakudya zawo zopatulika. Ine ndine Yehova amene ndimawayeretsa.’”
Aole hoi e waiho aku maluna o lakou i ka hewa o ka lawehala ana, i ka lakou ai ana i na mea hoano; no ka mea, na'u na Iehova lakou e hoano nei.
17 Yehova anawuza Mose kuti,
Olelo mai la hoi o Iehova ia Mose, penei,
18 “Yankhula ndi Aaroni, ana ake pamodzi ndi Aisraeli onse, ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati wina aliyense wa inu, Mwisraeli kapena mlendo amene akukhala mu Israeli abwera ndi mphatso ya nsembe yopsereza kwa Yehova, kupereka chimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu,
E olelo aku oe ia Aarona, a i kana mau keiki, a i na mamo a pau a Iseraela, a e i aku ia lakou, O kela kanaka keia kanaka o ka ohana o Iseraela, a o na malihini iloko o ka Iseraela, nana e kaumaha i kona mohai no kona hoohiki ana a pau, a no kana mau alana na kona makemake, ka mea a lakou e kaumaha'i ia Iehova, imohaikuni:
19 ndiye kuti abwere ndi ngʼombe yayimuna, nkhosa yayimuna kapena mbuzi yayimuna. Izi zikhale zopanda chilema kuti zilandiridwe.
Na ko oukou makemake iho, i ke kane kina ole o na bipi, o na hipa, a o na kao.
20 Musapereke nyama iliyonse yokhala ndi chilema chifukwa sidzalandiridwa mʼmalo mwanu.
O ka mea kina, aole oukou e kaumaha ia; no ka mea, aole ia e maliuia no oukou.
21 Pamene wina aliyense abweretsa ngʼombe kapena nkhosa kuti ikhale nsembe yachiyanjano kwa Yehova, kukwaniritsa zimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu, nyamayo iyenera kukhala yangwiro ndi yopanda chilema kuti ilandiridwe.
A o ke kanaka nana e kaumaha i ka alana o na mahaihoomalu ia Iehova, e hooko ai i kana i hoohiki ai, a ina he mohai na kona makemake, o na bipi, a o na hipa paha, e hemolele ia e maliuia'i: aole aku kina iloko ona.
22 Musapereke kwa Yehova nyama zakhungu, zovulala kapena zolumala, kapena nyama zimene zikutulutsa mafinya mʼthupi mwake, kapena zimene zili ndi nthenda yonyerenyetsa, kapena zimene zili ndi mphere. Nyama zotere musaziyike pa guwa kuti zikhale nsembe yopsereza kwa Yehova.
O ka makapaa, o ka oopa, a he puu kona, he puupuu, he kakio, aole oukou e kaumaha ia mau mea ia Iehova, aole hoi e hoolilo ia mau mea i mohai e kaumahaia ma ke ahi maluna o ke kuahu ia Iehova.
23 Koma mungathe kupereka ngʼombe yayimuna kapena nkhosa imene ili ndi chiwalo chachitali kapena chachifupi kukhala nsembe yaufulu. Koma simungayipereke ngati nsembe yoperekera zimene munalumbirira chifukwa sidzalandiridwa.
O ka bipikane, a o ka hipakeiki, he oi aku ko ka lala ona, he hemahema paha, e hiki no ke kaumaha oe ia i mohai na kou makemake no; aka no ka hoohiki ana aole e maliuia'ku ia.
24 Nyama iliyonse imene mavalo ake ndi onyuka kapena ophwanyika, ongʼambika kapena oduka, musamayipereke kwa Yehova mʼdziko lanu.
O ka mea i pepeia, a i paopaoia, a uhaeia, a i poaia, aole oukou e kaumaha ia mea ia Iehova, aole oukou e hana ma ko oukou aina.
25 Ndipo musalandire nyama zotere kuchokera kwa mlendo ndi kuzipereka kukhala zakudya za Mulungu wanu. Zimenezi sizidzalandiridwa mʼmalo mwanu chifukwa zili ndi chilema ndipo ndi zolumala.’”
Aole hoi noloko mai a ko ka malihini lima, e kaumaha ai oukou i ka berena a ko oukou Akua, no keia mau mea; no ka mea, iloko o lakou ko lakou popopo, he mau kina iloko o lakou; aole e maliuia no oukou.
26 Yehova anawuza Mose kuti,
Olelo mai la hoi o Iehova ia Mose, i mai la,
27 “Pamene mwana wangʼombe, mwana wankhosa kapena mwana wambuzi wabadwa, akhale ndi make kwa masiku asanu ndi awiri. Kuyambira tsiku lachisanu ndi chitatu mpaka mʼtsogolo mwake, angathe kulandiridwa kuti akhale nsembe yopsereza ya kwa Yehova.
Aia hanau ka bipikane, a he hipa paha, a he kao paha, alaila e noho ia malalo iho o ka makua, i na la ehiku; a mai ka walu o ka la, a mahope aku e maliuia'i ia i mohai puhi no Iehova.
28 Musaphe ngʼombe kapena nkhosa pamodzi ndi mwana wake tsiku limodzi. Muyidye pa tsiku lomwelo; musasiyeko ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
Ina he bipiwahine, a he hipawahine paha, aole oukou e pepehi pu ia mea me kana keiki i ka la hookahi.
29 “Pamene mupereka nsembe yoyamika kwa Yehova, muyipereke mwakufuna kwanu mu njira yoti ilandiridwe mʼmalo mwanu.
Aia kaumaha aku oukou i ka mohai aloha ia Iehova, e kaumaha oukou ia ua ko oukou makemake no.
30 Muyidye pa tsiku lomwelo, wosasiyako ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
Ia la hookahi no, e aiia ia, aole e hookoe oukou i kauwahi ona a ao ae: owau no Iehova.
31 “Choncho sungani malamulo anga ndi kuwatsatira. Ine ndine Yehova.
Nolaila e malama oukou i ka'u mau kauoha, a e hana ma ia mau mea: owau no Iehova.
32 Musanyoze dzina langa loyera. Koma lilemekezedwe pakati pa Aisraeli. Ine ndine Yehova amene ndimakuyeretsani
Aole hoi oukou e hoino i ko'u inoa hoano; e hoanoia no wau iwaena o na mamo a Iseraela; owau no Iehova nana oukou e hoano nei,
33 ndipo ndine amene ndinakutulutsani mu Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Ine ndine Yehova.”
Nana hoi oukoa i lawe mai mai ka aina o Aigupita mai i Akua au no oukou: owau no Iehova.

< Levitiko 22 >